< Nyimbo ya Solomoni 5 >
1 Ndalowa mʼmunda mwanga, iwe mlongo wanga, iwe mkwatibwi wanga; ndasonkhanitsa mure wanga ndi zokometsera zakudya zanga. Ndadya uchi wanga pamodzi ndi zisa zake zomwe; ndamwa vinyo wanga ndi mkaka wanga. Abwenzi Idyani abwenzi anga, imwani; Inu okondana, imwani kwambiri.
Dunu da amane sia: i, “Na dogolegei amola na uda! Na da na ifabia golili sa: i dagoi. Na da na hedama: ne fodole nasu amola na gabusiga: ‘me’ amo da gagadolala. Na da na agime hano amola agime hano diasu nana. Na da na waini hano amola gebo dodo maga: me nana.” Uda da amane sia: i, “Sasagesu dabe dilia! Ha: i moma! Amola waini hano naleawane, sasagesu hou amoga feloama: ma!”
2 Ndinagona tulo koma mtima wanga unali maso. Tamverani, bwenzi langa akugogoda: “Nditsekulire, mlongo wanga, bwenzi langa, nkhunda yanga, wangwiro wanga. Mutu wanga wanyowa ndi mame, tsitsi langa lanyowa chifukwa cha nkhungu ya usiku.”
“Na da golai dialoba, na dogo da nedigi dialu. Na sasagesu da logoa lulu fugilaloba, na da golaia ba: lu.” Dunu da amane sia: i, “Na dogolegei! Na ‘dafe’ sio! Na misa: ma! Na dialuma da oubi mogele amoga nanegai gala.” Uda da amane sia: i,
3 Ndavula kale zovala zanga, kodi ndizivalenso? Ndasamba kale mapazi anga kodi ndiwadetsenso?
“Na da na abula gisa: i dagoi. Na da abuliba: le amo bu gasisa: lima: bela: ? Na da na emo dodofei dagoi. Na da laluba: le na emo bu nigima: ma: bela: ?
4 Bwenzi langa anapisa dzanja lake pa chibowo cha pa chitseko; mtima wanga unagunda chifukwa cha iye.
Na sasagesu dunu da logo ga: suga lobo ligisi. E da na gadenene esalebe, amo na dawa: loba, nodoi.
5 Ndinanyamuka kukamutsekulira wachikondi wangayo, ndipo manja anga anali noninoni ndi mure, zala zanga zinali mure chuchuchu, pa zogwirira za chotsekera.
Na da e ganodini misa: ne momagei dagoi ba: i. Na lobo da ‘me’ gabusiga: hano amoga dedeboi ba: i. Na da logo ga: su geda gagui.
6 Ndinamutsekulira wachikondi wanga, koma nʼkuti wachikondi wangayo atachoka; iye anali atapita. Mtima wanga unafumuka chifukwa cha kuchoka kwake. Ndinamuyangʼanayangʼana koma sindinamupeze. Ndinamuyitana koma sanandiyankhe.
Na da na sasagesu dunu misa: ne logo doasi. Be e da asi dagoi ba: i. Na da ea sia: nabimusa: bagadewane hanai. Na da e hogoi be hame ba: i. Na da e wei be alofebe hame nabi.
7 Alonda anandipeza pamene ankayendera mzindawo. Anandimenya ndipo anandipweteka; iwo anandilanda mwinjiro wanga, alonda a pa khoma aja!
Sosodo aligisu dunu amo da moilai bai bagade sisiga: ha lala, na ba: i. Ilia da na fane, fofonomagia: i. Moilai bai bagade gagoi sosodo aligisu dunu ilia da na abula sawa: figi houga: le fasi.
8 Inu akazi a ku Yerusalemu ndithu ndikukupemphani, mukapeza wokondedwa wangayo, kodi mudzamuwuza chiyani? Muwuzeni kuti ine ndadwala nacho chikondi.
Yelusaleme uda, dilia! Nama sia: ilegema! Dilia na sasagesu dunu ba: sea, ema na da sasagesu hou ha: giwane hamobeba: le gasa hame gala adoma: ne, sia: ilegema.” Yelusaleme uda ilia amane sia: i,
9 Iwe wokongola kuposa akazi onsewa, kodi wokondedwa wakoyo ndi wopambana wina aliyense bwanji? Kodi wokondedwa wakoyo ndi wopambana ena onse chotani kuti uzichita kutipempha motere?
“Saga! Dia noga: idafa ba: su da eno uda huluane baligisa. Be dia sasagesu dunu da eno dunu huluane baligisala: ? E da baligili noga: idafala: ? Ninia da abuliba: le dima ilegele sia: ma: bela: ?” Uda da amane sia: i,
10 Wokondedwa wangayo ndi wowala kwambiri ndi wathanzi pakati pa anthu 1,000.
“Na sasagesu dunu da noga: idafa ba: sa amola e da gasa bagade gala. E da dunu 10,000 gilisisu ganodini baligili noga: idafa ba: sa.
11 Mutu wake ndi golide woyengeka bwino; tsitsi lake ndi lopotanapotana, ndiponso lakuda bwino ngati khwangwala.
Ea odagi gadofo da osoboya: i amola hohona: boi. Ea dialuma hinabo da helo amola balega sio defele, bunumai gala.
12 Maso ake ali ngati nkhunda mʼmbali mwa mitsinje ya madzi, ngati nkhunda zitasamba mu mkaka, zitayima ngati miyala yamtengowapatali.
Ea si da ‘dafe’ sio amo da dodo maga: mega dodofei amola hano yogo dalebe ea bega: esala, amo defele, noga: idafa ba: sa.
13 Masaya ake ali ngati timinda ta mbewu zokometsera zakudya zopatsa fungo lokoma. Milomo yake ili ngati maluwa okongola amene akuchucha mure.
Ea ba: da ifabi amo da hedama: ne fodole nasu bugi amoga nabai defele, noga: idafa ba: sa. Ea lafi gadofo da ‘lili’ mosoi amo ‘me’ hano amoga nanegai agoane ba: sa.
14 Manja ake ali ngati ndodo zagolide zokongoletsedwa ndi miyala yamtengowapatali. Thupi lake ndi losalala ngati mnyanga wanjovu woyikamo miyala ya safiro.
Ea lobo da noga: le hamoi ba: sa amola ea lobo sogo gasisalasu amo da igi noga: idafa amoga nina: hamoi. Ea da: i da hohona: boi ‘aifoli’ amo da ‘sa: faia’ igi noga: i amoga nina: hamoi, agoane ba: sa.
15 Miyendo yake ili ngati mizati yamwala, yokhazikika pa maziko a golide. Maonekedwe ake ali ngati Lebanoni, abwino kwambiri ngati mkungudza.
Ea masele da ‘a: laba: sade’ ganumu amo da gouli bai amoga sali agoane ba: sa. E da Lebanone Goumi alelaloi (amo da: iya da dolo ifa sedadedafa) amo agoane baligili noga: idafa ba: sa.
16 Milomo yake ndi yosangalatsa kwambiri; munthuyo ndi wokongola kwambiri! Uyu ndiye wachikondi wanga ndi bwenzi langa, inu akazi a ku Yerusalemu.
Ea lafi da nonogosea hedasa. Na da ea hou huluane ba: sea, nodosa. Dilia, Yelusaleme uda! Na sasagesu dunu da agoaiwane gala.”