< Nyimbo ya Solomoni 1 >
1 Nyimbo ya Solomoni, nyimbo yoposa nyimbo zonse.
Pa inge on ma kato emeet, ma Solomon el orala.
2 Undipsompsone ndi milomo yako chifukwa chikondi chako nʼchokoma kuposa vinyo.
Nga ke kom in arulana ngokla mutuk; Lungse lom uh los liki na wain uh.
3 Mafuta ako odzola ndi onunkhira bwino; dzina lako lili ngati mafuta onunkhira otsanulidwa. Nʼchifukwa chake atsikana amakukonda!
Oasr foul na keng se keim; Ke pacl inem ac fwack uh, nga sifil pacna esamak foul keng sac. Wangin mutan ku in kutongya lungse la nu sum.
4 Nditenge ndipo ndizikutsata, tiye tifulumire! Mfumu indilowetse mʼchipinda chake. Abwenzi Ife timasangalala ndi kukondwera nawe, tidzatamanda chikondi chako kupambana vinyo. Mkazi Amachita bwinotu potamanda iwe!
Usyu nga in wi kom, ac kut ac fah kaingla; Kom in tokosra luk ac pwenyuwot nu infukil sum. Kut ac fah tukeni ac arulana engan, Nga yukin lungse lom uh yohk liki kutena ma. Pwaye sin mutan uh in lungse kom!
5 Ndine wakuda, komatu ndine wokongola, inu akazi a ku Yerusalemu, ine ndine wakuda ngati tenti ya ku Kedara, ngati makatani a tenti ya Solomoni.
Mutan Jerusalem, nga ne sroalsroal tuh nga oasku. Nga sroalsroal oana lohm nuknuk in acn mwesis Kedar, Tuh nga kato oana lisrlisr inkul fulat sel Solomon.
6 Musandiyangʼane monyoza chifukwa ndine wakuda, ndine wakuda chifukwa cha dzuwa. Alongo anga anandikwiyira ndipo anandigwiritsa ntchito mʼminda ya mpesa; munda wangawanga sindinawusamalire.
Nimet pilesreyu mu nga sroalsroal, Mweyen faht uh pa tuhneyula uh. Tamulel luk elos tuh kasrkusrak sik Ac sap nga orekma ke ima in grape. Na wangin pacl luk in karinginyu sifacna.
7 Ndiwuze iwe, amene ndimakukonda, kumene umadyetsa ziweto zako ndi kumene umagoneka nkhosa zako nthawi yamasana. Ndikhalirenji ngati mkazi wachiwerewere pambali pa ziweto za abwenzi ako?
Kom su nga lungse yohk, fahkma nu sik, Kom ac pwen un sheep nutum an in mongo oya? Elos ac mongla ya ke pacl faht uh fol ke infulwen len uh? Efu ku ngan suk kom Inmasrlon un sheep nutin mwet shepherd ngia?
8 Ngati sukudziwa iwe wokongola kwambiri kuposa akazi ena, ngati sukudziwa, tsatira makwalala a nkhosa ndipo udyetse ana ambuzi pambali pa matenti a abusa.
Ya kom tia etu acn sac, kom su oasku liki mutan nukewa? Fahla ukweot na un sheep uh Twe konauk acn nani nutum an in mongo we Apkuran nu ke lohm nuknuk sin mwet shepherd ngia.
9 Iwe bwenzi langa, uli ngati kavalo wamkazi ku magaleta a Farao.
Kom su nga lungse na pwaye, lumom arulana kato Oana horse mutan ma amakin chariot okoal Tokosra Egypt.
10 Masaya ako ndi okongola ndi ndolo zamʼmakutuzo, khosi lako likukongola ndi mikanda yamiyala yamtengowapatali.
Aunsifom oaskulana ke oan likintupom uh, Ac putati sisken kwawom oana wek saok uh.
11 Tidzakupangira ndolo zagolide zokongoletsedwa ndi mikanda yasiliva.
Kut ac fah orala soko sein gold ah lom, Ac nawela ke mwe yun silver.
12 Pamene mfumu inali pa malo ake odyera, mafuta anga onunkhira anamveka fungo lake.
Ke tokosra luk el oan infukil sel, Ono keng keik uh nwakla in lohm uh ke foul wo.
13 Wokondedwa wanga ali ngati kathumba ka mure kwa ine, kamene kamakhala pakati pa mawere angawa.
Ke mukul kawuk luk el elongak iniwuk, El oana sie nwana keng orekla ke myrrh.
14 Wokondedwa wanga ali ngati mpukutu wa maluwa ofiira, ochokera ku minda ya mpesa ya ku Eni-Gedi.
El su saok sik el oana sie ros inima uh Su farngelik inima grape in acn Engedi.
15 Iwe wokondedwa wanga, ndiwe wokongoladi! Ndithu, ndiwe chiphadzuwa, maso ako ali ngati nkhunda.
Mutan saok sik, kom arulana oasku, Motom saromrom ke ngetnget in lungse lom!
16 Iwe bwenzi langa, ndiwe wokongoladi! Ndithu, ndiwe wokongoladi kwambiri! Ndipo malo athu ogonapo ndi msipu wobiriwira.
Mukul kawuk luk, kom kato na pwaye sik, Nga arulana pwar sum! Mah folfol uh pa ac fah mwe oan kiuktal.
17 Mitanda ya nyumba yathu ndi ya mkungudza, phaso lake ndi la mtengo wa payini.
Sak cedar pa srulun loaloa nu ke lohm sesr, Ac sak cypress pa ac srulun siling lasr uh.