< Rute 3 >
1 Tsiku lina Naomi anafunsa mpongozi wake Rute kuti, “Mwana wanga, kodi si kwabwino kuti ndikupezere kokhala kuti zinthu zizikuyendera bwino?
Ruth te a mani Naomi loh, “Ka canu aw, nang ham ngolbuel khaw ka tlap mapawt a? te ni nang ham a voelphoeng eh.
2 Bowazi amene adzakazi ake wakhala nawo nthawi yonseyi, si wachibale wathu kodi? Usiku uno akhala akupeta barele ku malo opunthira.
A lopai na balak puei Boaz te mah kah huiko moenih a? Anih te khoyin ah cangtilhmuen kah cangtun a cop lah ko te.
3 Samba ndi kudzola mafuta onunkhira, ndipo uvale zovala zako zabwino kwambiri. Kenaka upite ku malo opunthirako tirigu ndi barele koma munthuyo asakakuzindikire kufikira atamaliza kudya ndi kumwa.
Te dongah sil uh lamtah situi hluk. Te phoeiah na himbai te na pum dongah bai lamtah cangtilhmuen la suntla thuk. A caak a ok a coeng duela hlang taengah moe boeh.
4 Akamakagona, iwe ukaonetsetse malo amene wagonawo. Kenaka upite ndi kuvundukula chofunda ku mapazi ake ndi kugona. Iyeyo akakuwuza zoti uchite.”
Tedae a yalh tue om bitni. Te vaengah a yalh nah hmuen te phatuem lamtah pahoi paan. Te phoeiah a kho te khawn pah lamtah yalh pah. Te vaengah na saii ham te amah loh nang taengah a thui bitni,” a ti nah.
5 Rute anayankha kuti, “Ndichita zonse zimene mwanena.”
Te dongah amani te, “Kai taengah na thui boeih te saii bitni,” a ti nah.
6 Choncho Rute anapita ku malo opunthirawo ndipo anachita monga momwe apongozi ake anamuwuza.
Te dongah cangtilhmuen la suntla tih a mani loh anih a uen bangla boeih a saii.
7 Atamaliza kudya ndi kumwa, Bowazi anakhala wosangalala, ndipo anakagona pa mbali pa mulu wa barele. Tsono Rute anapita mwa kachetechete, navundukula chofunda ku mapazi ake ndi kugona.
Boaz khaw a caak a ok tih a lungbuei a voelphoeng nen tah yalh hamla canghlom hmatoeng te a paan. Te vaengah a muel la a paan tih a kho a khawn pah phoeiah a yalh pah.
8 Tsono pakati pa usiku Bowazi anadzidzimuka, natembenuka, ndipo anangoona mkazi akugona ku mapazi ake.
Khoyin boengli ah tah tongpa te lakueng tih a hoi uh hatah a kho taengah huta tarha ana yalh pah.
9 Iye anafunsa kuti, “Ndiwe yani?” Ndipo anayankha kuti, “Ndine mdzakazi wanu Rute. Popeza ndinu wachibale amene muyenera kundiwombola, ndiye mundilowe chokolo.”
Te dongah, “Nang ulae?” a ti nah hatah, “Na salnu kai, Ruth ni, nan tlan coeng dongah na salnu he na himbai hmoi neh aka ng'khuk thil laeh,” a ti nah.
10 Ndipo Bowazi anati, “Mwana wanga, Yehova akudalitse popeza kukoma mtima kumene wasonyeza panoku kwaposa koyamba kaja. Iwe sunathamangire anyamata olemera kapena osauka.
Te dongah, “Ka canu, BOEIPA dongah na yoethen coeng. Hlanglen mai khaw, tattloel mai cakhaw tongpang hnukah na caeh pawt dongah lamhma kah lakah a hnuk lam ni na sitlohnah neh na voelphoeng pueng.
11 Ndipo tsopano mwana wanga usaope. Ine ndidzakuchitira chilichonse udzapemphe popeza anzanga onse amʼmudzi muno akudziwa kuti ndiwe mkazi wa khalidwe labwino.
Te dongah ka canu na hoe boeih te rhih boeh, nang tah tatthai nu tila ka pilnam kah vongka tom m'ming coeng dongah nang ham kan saii bitni.
12 Ngakhale kuti ndinedi wachibale woyenera kukusamala, koma alipo wachibale weniweni kuposa ine.
Kai loh kan tlan ham khaw tueng ngawn coeng dae aka tlan ham te kai lakah aka yoei rhep om pueng.
13 Gona konkuno usiku uno mpaka mmawa. Tsono ngati iyeyu adzakulowa chokolo, chabwino alowe. Koma ngati safuna kutero, ine ndikulumbira pamaso pa Yehova Wamoyo kuti ndidzakulowa chokolo. Ugone kuno mpaka mmawa.”
Khoyin ah rhaeh lamtah mincang ah ni nang aka tlan te a om atah a then la n'tlan saeh. Tedae nang te tlan ham a ngaih pawt atah BOEIPA kah hingnah dongah nang te kamah loh kan tlan bitni, mincang duela yalh mai dae,” a ti nah.
14 Choncho Rute anagona ku mapazi ake mpaka mmawa, koma anadzuka mmamawa kusanayere chifukwa Bowazi anati, “Aliyense asadziwe kuti kopondera barele kunabwera mkazi.”
Te dongah mincang duela a kho tang, a kho tang ah a yalh pah. Tedae a hui te kah hlang a hmat hlan ah vawl thoo coeng. Te vaengah Boaz longtah, “Cangtilhmuen huta ha pawk he a ming uh moenih,” a ti.
15 Bowazi anati kwa Rute, “Bwera nacho kuno chofunda wavalacho ndipo uchiyale pansi.” Ndipo atayala, Bowazi anathira makilogalamu makumi awiri a barele ndi kumusenzetsa Rute. Rute anapita nakalowa mu mzinda.
Te vaengah, “Na pum dongkah te himbai hang khuen lamtah duen lah,” a ti nah. Te dongah himbai te a tuuk doela cangtun khoi rhuk a loeng pah phoeiah Ruth a phueih sak tih kho khuila cet.
16 Rute atafika kwa apongozi ake anamufunsa kuti, “Zinayenda bwanji mwana wanga?” Kenaka iye anafotokoza zonse zimene Bowazi anamuchitira.
A mani taengla a pawk vaengah, “Ka canu nang u taengah lae na caeh,” a ti nah hatah Hlang loh anih ham a saii pah te boeih a thui.
17 Ndipo anati, “Munthuyo anandipatsa makilogalamu makumi awiri awa a barele, nandiwuza kuti usapite kwa apongozi ako wopanda kanthu.”
Te dongah, “Cangtun khoi rhuk he kai ham ham poep tih, 'Na mani te kuttling la paan boeh,’ a ti,” a ti nah.
18 Kenaka Naomi anati, “Mwana wanga, dikira mpaka titaona mmene zinthu zikhalire chifukwa munthuyu salekera pomwepo, mpaka zinthuzi zitakonzeka lero.”
Te vaengah, “Ka canu tihnin kah olka he a khah uh hlan atah hlang te mong mahpawh, metlamlae olka a dip eh tite na ming duela ngol,” a ti nah.