< Aroma 8 >
1 Choncho, tsopano amene ali mwa Khristu Yesu alibe mlandu owatsutsa
Vinu kwahera utoza kwa wantu yawalikala kwa kulikolerana pamuhera na Kristu Yesu.
2 chifukwa mwa Khristu Yesu, lamulo la Mzimu Woyera amene amapereka moyo, lawamasula ku lamulo la tchimo ndi la imfa.
Toziya malagaliru ga Rohu yagajega ukomu kwa kulikolerana pamuhera na Yesu Kristu ganekeziya kulawa mumalagaliru ga vidoda yagajega kuhowa.
3 Pakuti zimene Malamulo sanathe kuzichita, popeza anali ofowoka chifukwa cha khalidwe lathu la uchimo, Mulungu anazichita potumiza Mwana wake mʼchifanizo cha munthu ochimwa kuti akhale nsembe yauchimo. Ndipo Iye anagonjetsa tchimo mʼthupi la munthu,
Mlungu kashitenda shitwatira ashi, malagaliru geni gaweza ndiri kutenda toziya uzotopa wa muntu. Mlungu kamtumiti Mwana gwakuwi pakawera na nshimba teratera na nshimba zyetu twenga yatuwera na vidoda kuvitoza vidoda.
4 ndi cholinga chakuti chilungamo chofunikira cha lamulo chikwaniritsidwe kwathunthu mwa ife amene sitikhala monga mwachikhalidwe chathu cha uchimo koma mwa Mzimu.
Mlungu katenditi hangu su mafiliru gaherepa ga Malagaliru yagatendaga kwa ukamilika mngati mwa twenga yatulikala ntambu yakafira Rohu na tulema mafiliru ga nshimba.
5 Pakuti anthu amene amakhala monga mwa makhalidwe oyipa a thupi amayika malingaliro awo pa zinthu zathupi. Koma amene amakhala monga mwa Mzimu amayika malingaliro awo pa zinthu za Mzimu.
Wantu walii yawalikala kugenderana ntambu yazifira nshimba, walongoziwa na mahala ga nshimba zyawu. Kumbiti walii yawalikala kugenderana ntambu yakafira Rohu, walongoziwa na Rohu ntambu yakafira.
6 Kuyika mtima pa zathupi ndi imfa koma kuyika mtima pa za Mzimu ndi moyo ndi mtendere.
Kulonguziwa na nshimba kujega kuhowa, kumbiti kulonguziwa na Rohu kujega ukomu na ponga.
7 Pakuti mtima umene wakhazikika pa zathupi ndi wodana ndi Mulungu. Sunagonjere lamulo la Mulungu ndipo sungathe kutero.
Su wantu yawalongoziwa na mafiliru ga nshimba ndo wankondu wa Mlungu, womberi hapeni wagajimiri Malagaliru ga Mlungu, nakaka hapeni wawezi kugajimira.
8 Ndipo anthu amene amalamulidwa ndi khalidwe lauchimo sangathe kukondweretsa Mulungu.
Wantu walii yawajimira mafiliru ga nshimba hapeni wamfiriziyi Mlungu.
9 Koma inu simulamulidwanso ndi khalidwe lanu lauchimo koma ndi Mzimu ngati Mzimu wa Mulungu akhaladi mwa inu. Koma ngati munthu aliyense alibe Mzimu wa Khristu, iyeyu si wa Khristu.
Kumbiti mwenga mulikala ndiri kugenderana na mafiliru ga nshimba, ira mulikala kugenderana na mafiliru ga Rohu, payiwera Rohu gwa Mlungu kalikala mngati mwenu. Yoseri yakawera ndiri na Rohu gwa Kristu, yomberi ndo gwa Kristu ndiri.
10 Ndipo ngati Khristu ali mwa inu, thupi lanu ndi lakufa chifukwa cha uchimo, koma mzimu wanu ndi wamoyo chifukwa cha chilungamo.
Kumbiti handa Kristu kamungati mwenu, Rohu ndo makaliru kwa mwenga toziya mtendwa waheri kulongolu kwa Mlungu, kumbiti nshimba zyamwenga pazigenda kuhowa toziya ya vidoda.
11 Ndipo ngati Mzimu wa Mulungu amene anaukitsa Yesu kwa akufa akhala mwa inu, Iyeyo amene anaukitsa Khristu kwa akufa adzapatsanso moyo matupi anu amene amafa kudzera mwa Mzimu wake amene amakhala mwa inu.
Payiwera Rohu gwa Mlungu yakamzyukisiyiti Yesu kalikala mngati mwenu, su ayu yakamzyukisiyiti Kristu Yesu hakazipanani ukomu nshimba zyenu zyazifira kuhowa, hakatendi hangu kupitira Rohu yakalikala mngati mwenu.
12 Kotero abale, ife tili ndi zoti tikwaniritse, koma osati za khalidwe lathu lauchimo, kumachita zofuna zake.
Su waganja wangu twana uwanda, kumbiti wa kulikala ndiri kugenderana na mafiliru ga nshimba.
13 Pakuti ngati inu mukhala monga mwa khalidwe lauchimo, mudzafa. Koma ngati mwa Mzimu mupha ntchito zoyipa zathupi, mudzakhala ndi moyo.
Toziya handa pamulikala kugenderana na mafiliru ga nshimba, nakaka mgenda kuhowa, kumbiti handa kupitira Rohu mwankugalaga matendu genu gadoda, nakaka hamlikali.
14 Onse amene amatsogozedwa ndi Mzimu wa Mulungu ndi ana a Mulungu.
Woseri yawalongoziwa na Rohu gwa Mlungu ndo wana wa Mlungu.
15 Mzimu amene inu munalandira samakusandutsani akapolo, kuti muzikhalanso amantha, koma Mzimu amakusandutsani ana. Ndipo mwa Iye ife timafuwula kuti, “Abba, Atate.”
Kwa Rohu yakawapanani Mlungu kawatenda ndiri mwenga wamanda na kuwatenda muweri na lyoga, kumbiti Rohu kawatenda mwenga muweri wana wa Mlungu na kwa makakala ga Rohu, twenga tumshema Mlungu, “Tati! Tati gwangu!”
16 Mzimu mwini amavomerezana ndi mzimu wathu kuti ife ndife ana a Mulungu.
Rohu gwa Mlungu mweni kankulaviya ukapitawu na rohu zya twenga kuwera twenga ndo wana wa Mlungu.
17 Tsono ngati tili ana ake, ndiye kuti ndife olowa mʼmalo a Mulungu ndi olowa mʼmalo pamodzi ndi Khristu. Ngati ife timva zowawa pamodzi ndi Khristu, tidzalandiranso ndi ulemerero womwe pamodzi naye.
Toziya twenga twawana wa Mlungu, hatuwanki tekeleru zoseri Mlungu zyakawatuliriti wantu wakuwi na hatuwanki pamuhera na Kristu vilii Mlungu vyakamtuliriti. Handa patuwera pamuhera na Kristu muntabika yakuwi, hatuweri pamuhera nayomberi viraa muukwisa wakuwi.
18 Ine ndiganiza kuti masautso amene tikuwamva nthawi ino, sakufanana ndi ulemerero umene udzaonetsedwa mwa ife.
Mona kuwera ntabika zya shipindi sha vinu hapeni gawezi kulifana na ukwisa ulii waugenda kugubutulwa kwa twenga.
19 Pakuti chilengedwe chikudikira ndi chiyembekezo kuonetsedwa poyera kwa ana a Mulungu.
Vyoseri vyaviumbitwi vyankuhepera kwa lumatamata kwa Mlungu kuwagubutulira wana wakuwi.
20 Pakuti chilengedwe sichinasankhe kugonjera zopanda pake, koma mwachifuniro cha Iye amene analola kuti chigonjere. Koma chili ndi chiyembekezo
Su, viumbitwi kwa jimilirwa, muntambu ya kuligangamaziya ndiri. Ayi ndo ntambu ndiri ya mafiliru ga viumbitwi, kumbiti toziya ya mafiliru ga Mlungu. Pamuhera na hangu kwana matumbiru
21 chakuti chidzamasulidwa ku ukapolo wa chivundi ndi kulandiranso ufulu ndi ulemerero wa ana a Mulungu.
kuwera vyaviumbitwi avi viraa na vyeni havilopoziwi kulawa muwumanda wa kuhalabisiya na haviweri pamuhera muukwisa wa ulekeru wa wana wa Mlungu.
22 Ife tikudziwa kuti chilengedwe chonse chakhala chikubuwula ndi ululu ngati ululu wa nthawi yobereka mwana mpaka tsopano lino.
Toziya tuvimana kuwera mpaka vinu, viumbi vyoseri vyankulira kwa kutama gambira utama wa mdala wa kulera.
23 Si zokhazo ayi, ngakhale ife tomwe, amene tili ndi zipatso zoyamba za Mzimu, tikubuwulira mʼkati mwathu pomwe tikudikira mwachidwi kusankhidwa kwathu ngati ana, kuwomboledwa kwa matupi athu.
Viumbi avi vya gweka yawu ndiri, viraa virii twenga yatuwera Rohu, Rohu ndo yakawera lifupu lya kwanja lya Mlungu, twenga viraa tuwera na utama mngati mwetu, patuhepera tutendwi wana wa Mlungu na nshimba zya twenga zilekeziwi.
24 Pakuti ife tinapulumutsidwa mʼchiyembekezo ichi. Koma chiyembekezo chimene chimaoneka si chiyembekezo ayi. Kodi ndani amene amayembekezera chimene ali nacho kale?
Kwa matumbiru aga twenga tulopoziwitwi. Kumbiti litumbiru lyahera mana payiwera twankushiwona shilii shatushitumbira. Hashi, gaa kankushitumbira shilii shakashiwona kala?
25 Koma ngati ife tiyembekeza chimene tikanalibe, ndiye kuti tikuyembekeza modekha mtima.
Handa patushitumbira shilii hatwenishiwoni, su twankushihepera kwa hepeleru.
26 Momwemonso, Mzimu amatithandiza ife mʼkufowoka kwathu. Ife sitidziwa momwe tiyenera kupempherera koma Mzimu mwini amatipempherera mobuwula ndi mawu osafotokozedwa.
Ntambu iraa ayi Rohu kiza kututanga uzotopa yatuwera nawu. Twenga tuvimana ndiri vyavifiruwa kumluwa Mlungu, kumbiti Rohu mweni kankutuluwira kwa Mlungu kwa visoweru hapeni guvitakuli.
27 Koma Iye amene amasanthula mitima yathu amadziwa maganizo a Mzimu, chifukwa Mzimu amapempherera oyera mtima molingana ndi chifuniro cha Mulungu.
Na Mlungu yakawona mpaka mngati mwa mumyoyu ya twenga, kavimana maholu ga Rohu ayu, toziya Rohu ayu kankuwaluwira wantu wa Mlungu kugenderana na mafiliru ga Mlungu.
28 Ndipo ife tikudziwa kuti zinthu zonse zimathandizana kuwachitira ubwino amene amakonda Mulungu, amene anayitanidwa monga mwa cholinga chake.
Tuvimana kuwera muvitwatira vyoseri, Mlungu kankutenda viherepa kwa walii yawamfira mweni, walii yakawashemiti kulawirana na mpangu gwakuwi.
29 Pakuti amene Mulungu anawadziwiratu, anawasankhiratunso kuti akonzedwe mʼchifanizo cha Mwana wake, kuti Iye akhale Mwana woyamba kubadwa mwa abale ambiri.
Woseri walii yawamanitwi kala na Mlungu viraa wasyagulitwi kala su wapati kulifana na Mwana gwakuwi, su Mwana gwakuwi kaweri kifungua mimba pakati pa waumini wavuwa.
30 Iwo amene anawasankhiratu, anawayitananso. Amene Iye anawayitana anawalungamitsanso ndipo amene anawalungamitsa anawapatsanso ulemerero.
Su walii yawasyagulitwi kala na Mlungu, viraa Mlungu ndo yakawashemiti. Walii yakawashemiti ndo walii kawatenditi kumfiriziya Mlungu. Walii yakawatenditi kumfiriziya Mlungu, viraa kawapananiti ukwisa wakuwi.
31 Nanga tsono tidzanena chiyani pa izi? Ngati Mulungu ali mbali yathu, adzatitsutsa ife ndani?
Kulawirana na aga, twenga tutakuli hashi? Hashi, payiwera Mlungu kauwega wa twenga, gaa yakaweza kuwera mngondu gwa twenga? Kwahera ata yumu!
32 Iye amene sanatimane Mwana wake wa Iye yekha, koma anamupereka chifukwa cha ife tonse. Iye adzalekeranjinso pamodzi naye kutipatsa ife zinthu zonse mwaulere?
Mlungu kamwonera ndiri lusungu ata Mwana gwakuwi gwa gweka, kumbiti kamlaviyiti tambiku kwa twenga woseri! Yomberi katupananiti Mwana gwakuwi. Hashi, Mlungu na Mwana gwakuwi watushera ndiri twenga pamuhera na vitwatira vyoseri vyawatupananiti?
33 Ndani amene adzabweretsa mlandu kutsutsa amene Mulungu anawasankha? Ndi Mulungu amene amalungamitsa.
Hashi, gaa hakawatozi wantu yawasyagulitwi na Mlungu? Ndala! Mlungu mweni ndo yakawawusilira ukondola!
34 Ndani amene angatipeze ife olakwa? Palibe. Khristu Yesu amene anafa, kuposera pamenepo, amene anaukitsidwa ndi moyo, amene ali kudzanja lamanja la Mulungu ndiye amene akutipempherera.
Hashi, gaa hakawatozi mwenga? Ndala! Kristu Yesu ndo yakahowiti, kayi kazyukiti na kankulivaga uwega wa kumliwu wa Mlungu. Mweni kankutuluwira!
35 Ndani amene adzatilekanitsa ife ndi chikondi cha Khristu? Kodi ndi masautso, kapena zowawa, kapena mazunzo, kapena njala, kapena umaliseche, kapena choopsa, kapena lupanga?
Hashi, gaa yakaweza kutulekaniziya mumafiliru ga Kristu? Hashi, tabu ama uhushu ama ntabiku ama njala, ama kuwera shivula ama hatali ama kuhowa?
36 Monga kwalembedwa: “Chifukwa cha inu, ife tikuphedwa tsiku lonse: ife tikutengedwa ngati nkhosa zoti zikaphedwe.”
Malembu Mananagala ntambu yagalembwa, “Toziya ya gwenga, twenga twamuhatari ya kuhowa vipindi vyoseri, Tutenderwa gambira wakondolu yawagenda kulikitulwa.”
37 Ayi, mu zonsezi ife ndife oposa agonjetsi mwa Iye amene anatikonda.
Kumbiti muvitwatira avi vyoseri, tupata ukanga mkulu kupitira Yesu yakatufiriti twenga!
38 Pakuti ine ndatsimikiza ndi mtima wonse kuti ngakhale imfa, kapena moyo, ngakhale angelo, kapena ziwanda, ngakhale zinthu zilipo, kapena zili mʼtsogolo, kapena mphamvu zina,
Toziya nuvimana nakaka kwahera shintu shashiweza kutulekaniziya na mafiliru gakuwi ama kuhowa, ama ukomu ama wantumintumi wa kumpindi, ama washamshera ama yagalawira vinu, ama yagalawira kulongolu ama makakala,
39 ngakhale kutalika, kapena kuya, kapena chilichonse mʼchilengedwe chonse, sizingathe kutisiyanitsa ndi chikondi cha Mulungu chimene chili mwa Khristu Yesu Ambuye athu.
ama kumpindi, ama kumambi. Kwahera shiumbi shoseri shashiweza kutulekaniziya na mafiliru ga Mlungu mu Mtuwa gwetu Yesu Kristu.