< Aroma 4 >
1 Nanga tsono tidzati chiyani za Abrahamu kholo lathu, iyeyu anapezana ndi zotani pa nkhani imeneyi?
Hanchu, taksa tieng ei richibul Abraham hah i angin mo ei misîr rang ani zoi? Inmo a sinthona a lei intem?
2 Kunena zoona, Abrahamu akanalungamitsidwa ndi ntchito zake, akanakhala nako kanthu kodzitamandira, koma osati pamaso pa Mulungu.
Sintho sika thei intum nirese chu, Abraham'n song rang imini chu a dôn rang kêng, hannirese Pathien mitmua chu ni mak.
3 Kodi Malemba akuti chiyani? “Abrahamu anakhulupirira Mulungu, ndipo ichi chinamuchititsa kukhala wolungama.”
Pathien lekhabu'n imo ati? “Abraham'n Pathien a iema, a taksônna sika han Pathien'n midikin a pom ani,” ati.
4 Tsopano munthu amene wagwira ntchito, malipiro ake satengedwa kukhala ngati mphatso koma zimene anayenera kulandira.
Sinthopu rathaman chu lungkham pêk niloiin lâkâi anga be ani uol, an sinthona an man kêng ani.
5 Koma kwa munthu amene sanagwire ntchito ndipo akhulupirira Mulungu amene amalungamitsa ochimwa, chikhulupiriro chakecho chimatengedwa kukhala chilungamo.
Aniatachu mingei hah an sintho han midika tel nimak ngeia nunsiengei ngâidampu Pathien taksônna sikin kêng ani.
6 Davide ponena zomwezi pamene anayankhula za kudala kwa munthu amene Mulungu amulungamitsa osati chifukwa cha ntchito zake akuti,
Mi Sintho sika niloia Pathien'n dikna a minchang ngei satvur anni tie, David khom hi anghin a ril:
7 “Odala ndi amene zoyipa zawo zakhululukidwa; amene machimo awo afafanizidwa.
“An tho minchâinangei ngâidamin a oma, an sietnangei mukhua aom ngei chu, satvur an ni!
8 Ngodala munthu amene machimo ake Ambuye sadzawakumbukiranso.”
Pumapa'n sietna dôn a be loi ngei chu satvur an ni!”
9 Kodi madalitso amenewa ali kwa ochita mdulidwe okha kapena kwa amene sanachitepo mdulidwe? Ife takhala tikunena kuti chikhulupiriro cha Abrahamu chinamuchititsa kukhala wolungama.
Ha satvurna hah sertan ngei rang vai mo? Sertanloi ngei rang khom mo? Abraham'n taksônna sikin dikna achang ei tia.
10 Kodi chinatengedwa bwanji? Kodi nʼkuti iye atachita mdulidwe kapena asanachite? Osati atachita mdulidwe koma asanachite!
A sertan mâna chong mo, a tan suole mo? nimak, sertan suole nimaka, sertan mân ani.
11 Ndipo iye anachita mdulidwe ngati chizindikiro ndi chitsimikizo cha kulungama kumene anali nako mwachikhulupiriro pomwe anali asanachite mdulidwe. Choncho, iye ndi kholo la onse amene akhulupirira koma sanachite mdulidwe, ndi cholinga chakuti alungamitsidwe.
A sertan mâna a taksônna sika, Pathien'n thei a minchang minenna ranga sertan kêng ani. Hanchu sertan khom no rese iemna sika Pathien'n thei a minchang ngei ta rangin chu Abraham chu an rathatienga pa ani.
12 Ndipo iyenso ndiyenso kholo la ochita mdulidwe osati amene anangochita mdulidwe kokha koma amene amatsata chitsanzo cha chikhulupiriro chimene kholo lathu Abrahamu anali nacho asanachite mdulidwe.
Sertan ngei pa khom ani, sertan anni vai sika niloiin ei pa Abraham'n a sertan mâna an taksôn angdêna iemna an nei sika ani.
13 Abrahamu ndi zidzukulu zake sanalandire lonjezano lakuti adzalandira dziko lapansi kudzera mu Malamulo, koma kudzera mu chilungamo chimene chimabwera ndi chikhulupiriro.
Balam jôm sik niloiin, iemna sika thei minchang a lei ni, Pathien'n Abraham kôm, ama le a jâisuon ngeiin rammuol hih la luo an tih, ti a khâm ani.
14 Pakuti ngati amene amadalira Malamulo ndiye olowa mʼmalo, ndiye kuti chikhulupiriro nʼchopanda pake ndipo lonjezano ndi lopanda phindu
Balam jôm hih rochon luona anînchu, taksônna hih akorong nîng ata, chongkhâm khom hah kâmomloi ani, tina nîng a tih.
15 chifukwa Malamulo anabweretsa chilango. Ndipo kumene kulibe Malamulo kulibenso kuwalakwitsa.
Balam han Pathien taksina a minsuok ngâi balam boina hanchu minchâina khom om ngâi mak.
16 Motero, timalandira lonjezo mwachikhulupiriro. Laperekedwa mwachisomo kuti patsimikizidwe kuti lonjezolo liperekedwa kwa ana ndi zidzukulu zonse za Abrahamu, osati kwa iwo okha amene amatsatira Malamulo komanso kwa iwo amene ali ndi chikhulupiriro cha Abrahamu. Iye ndiye kholo la ife tonse.
Masikin, chongkhâm hah Abraham jâisuonngei murdi rangin balam a jôm ngei mang niloiin ama taksôn anga iempungei rang khomin Pathien manboipêk a nitie min langna rangin iemna sikin ani Abraham kôma chong a lei khâm hah, ama hah ratha tienga ei rênga ei pa ani.
17 Monga kwalembedwa kuti, “Ine ndakusandutsa kukhala kholo la mitundu yambiri.” Iye ndiye kholo lathu pamaso pa Mulungu, amene anamukhulupirira, Mulungu amene amapereka moyo kwa akufa ndipo amapereka moyo kwa zinthu zopanda moyo.
Pathien lekhabu'n, “Nam tamtak pa'n nang ki minchang zoi” a tia, inkhâmna hah Pathien tieng chu asa ani. Hi chongkhâm hih Abraham'n ai iem Pathien mithi ngei minringnôkpu le neinun a omloi ngei min ompu kôm renga ai mu ani.
18 Ngakhale zinali zosayembekezeka, Abrahamu anakhulupirira ndi chiyembekezo kuti adzakhala kholo la mitundu yambiri. Izi ndi monga zinanenedwa kwa iye kuti, “Ndi mmene adzakhalire ana ako ndi zidzukulu zako.”
Abraham han sabei rang aboi tet nûk khomin ala sabei ngit sikin, “Nam tamtak ngei pa,” a hongchang zoi ani. Pathien chongin, “Na jâisuonngei ârsi dôr la nîng an tih,” ati anghan.
19 Iye sanafowoke mʼchikhulupiriro. Anadziwa choonadi cha thupi lake kuti linali lakufa popeza anali ndi zaka pafupifupi 100 ndiponso mimba ya Sara inali yowuma.
Kum raza mi ani zoia a taksa mindon nân chu mithi angdôr ani zoia, Sarah khom aching ani ti a riet chien pum khomin a taksônna chu duoi uol mak.
20 Komabe iye sanagwedezeke chifukwa chosakhulupirira pa zokhudzana ndi lonjezo la Mulungu. Iye analimbikitsidwa mʼchikhulupiriro chake ndi kupereka ulemerero kwa Mulungu.
Taksônna insamin Pathien chongkhâm hah mindon kârminlak maka, a taksônna a rât uol uola Pathien a chôiminsânga.
21 Anatsimikiza mu mtima mwake kuti Mulungu anali ndi mphamvu yochita chomwe analonjeza.
Pathien'n a chongkhâm tuonmintung thei ngêt a tih, ti a riet minthâr sikin.
22 Nʼchifukwa chake “chinamuchititsa kukhala wolungama.”
Masika han kêng, “A taksônna sika thei minchang ani,” ti ani.
23 Mawu akuti, “chinatengedwa kwa iye” sanalembedwe chifukwa cha iye yekha,
Hi chong, “midika pom ani,” ti hih ama chungroi misîrna rang manga miziek ni maka.
24 komanso chifukwa ife amene Mulungu adzatiyesa olungama, ife amene tikhulupirira mwa Iye amene anamuukitsa kwa akufa, Yesu Ambuye athu.
Eini, ei Pumapa Jisua thina renga kaithoipu iemngei sika dikna intum sai ngei rang khomin miziek ani.
25 Iye anaperekedwa kuti aphedwe chifukwa cha machimo athu ndipo anaukitsidwa ndi kukhala ndi moyo kuti tilungamitsidwe.
Jisua hah ei sietnangei sikin thatin a oma Pathien makunga dikna intum theina rangin kaithoiin a om nôk ani.