< Aroma 3 >

1 Nanga kodi pali ubwino wotani pokhala Myuda, kapena muli ubwino wanjinso mu mdulidwe?
Hanchu, Juda mi ni hah Jentail mingei nêkin imo chungtuorna aom uola? sertan khom imo asena aom?
2 Ubwino wake ndi wambiri mʼnjira zonse! Choyambirira iwo anapatsidwa Mawu a Mulungu kuti awasunge.
Lamtina asena aom ok! Amotontaka chu Pathien chongngei hi Judangei chunga juong mintung ani.
3 Nanga zili bwanji ngati ena analibe chikhulupiriro? Kodi kupanda chikhulupiriro kwawo kukanalepheretsa kukhulupirika kwa Mulungu?
mi senkhatin taksônna dônloi ngei ha inmo an ni rang? an taksôn loina han Pathien taksôn omna hah an minboi thei rang mini?
4 Ayi. Mʼnjira iliyonse ayi! Mulungu akhale woona, ndi munthu aliyense akhale wonama. Monga kwalembedwa kuti, “Kotero kuti inu mwapezeka kuti ndinu wolungama pamene muyankhula ndi kupambana pamene muweruza.”
Nitet mak! mi murdi milak ni riei khomrese ngeia Pathien chu dik tit atih, Pathien lekhabu'n, “Nangma no chong zorân chu thei na chang ngêt rang anâng, roijêkpea no om tika no motor theina rangin,” tia ânziek anghan.
5 Koma ngati kuyipa mtima kwathu kuonetsa poyera kuti Mulungu ndi wolungama, ife tinganene chiyani? Kodi tinganene kuti Mulungu ndi wosalungama pamene aonetsa mkwiyo wake pa ife? (Ine ndikuyankhula monga mmene anthu ena amayankhulira).
Ei dikloina ngei hin Pathien dikna a min lang thei aninte i angin mo ei mindon? Pathien'n mi sepna a pêk inte a minchâi ei ti thei rang mini? (Miriem balama ki ril ani).
6 Ayi. Mʼnjira iliyonse ayi! Ngati zikanakhala zotero, kodi Mulungu akanaweruza bwanji dziko lapansi?
Nitet mak! ha anghan nirese, Pathien'n i angin mo rammuol roi a jêk thei ranga?
7 Wina atanena kuti, “Ngati kunama kwanga kukuonetsa koposa kuti Mulungu ndi woona, ndi kuwonjezera pa ulemerero wake, nanga nʼchifukwa chiyani ndikuweruzidwa kuti ndine wochimwa?”
Aniatachu, adikloi ki nina hin a roiinpuina rang Pathien dik tie ânlang thei uolin te i rangin mo kei khom dikloia bên ka la om ranga?
8 Nʼchifukwa chiyani osanena kuti, monga ena amanena mosasamala kuti, “Tiyeni tichite zoyipa kuti zabwino zionekere?” Anthu onena zoterewa kulangidwa kwawo ndi koyenera.
Mi senkhatin, “Asa ahong suok theina rangin asie lei tho rei u,” a ti, tia min rilsiet anga han ei tho rang mini? ha mingei ha chu theiloi intum ruopiel an ni.
9 Kodi timalize bwanji? Kodi Ayuda ndife oposa anthu ena? Ayi. Mʼnjira iliyonse ayi! Ife tinanena kale kuti Ayuda ndi a mitundu ina omwe ndi ochimwa.
Hanchu, eini Judangei hih Jentailngei nêkin ei sa uol bak mini? nitet mak! Judangei le Jentialngei nunsie suoka om zit ei ni ti ki ril suozoi.
10 Monga kwalembedwa kuti, “Palibe munthu wolungama, inde palibe ndi mmodzi yemwe.
Pathien lekhabu'n, “Tute midik reng ommak ngei, inkhat luo ommak ngei,
11 Palibe ndi mmodzi yemwe amene amazindikira, palibe amene amafunafuna Mulungu.
Tute mivâr reng ommak ngei, tute Pathien a rok reng ommak ngei,
12 Onse apatukira kumbali, onse pamodzi asanduka opandapake. Palibe ndi mmodzi yemwe amene amachita zabwino, palibe ngakhale mmodzi.”
Pathien renga an pêt suo zoia, dikloina tieng an se suozoi, inkhat luo asa sin reng om khâi mak ngei.
13 “Kummero kwawo kuli ngati manda apululu; ndi lilime lawo amayankhula zachinyengo.” “Ululu wa mamba uli pa milomo yawo.”
An rôl chu thân in-ong ania, an meleiin milak an rila, an bâi sûng renga murûl tûr asuoka,
14 “Mʼkamwa mwawo ndi modzaza ndi zotemberera ndi mawu owawa.”
an bâi hah khomâksâmna le chongkhân asipa,
15 “Mapazi awo afulumira kukakhetsa magazi.
an ke hah thisen min suok rangin kal achôi ânranga;
16 Kusakaza ndi chisoni kumaonekera mʼnjira zawo,
an lampui chu inmangna le jâmzalna asipa.
17 ndipo njira ya mtendere sayidziwa.”
Inngêina lampui reng riet mak ngei,
18 “Saopa Mulungu ndi pangʼono pomwe.”
an mitmua Pathien china reng om riek mak,” tia inziek anghan.
19 Tsopano tikudziwa kuti chilichonse Malamulo amanena, amanena kwa amene amalamulidwa ndi Malamulowo, ndi cholinga chakuti aliyense asowe chonena, ndipo dziko lonse lidzayimbidwa mlandu ndi Mulungu.
Balam chongngei chu Balam nuoia omngei chunga mang rang ani ti ei riet, tutên ite an ti theiloina rangin le rammuol pumpui hi Pathien roijêkna nuoia aom theina rangin.
20 Chifukwa chake palibe mmodzi amene adzayesedwa wolungama pamaso pake chifukwa chosunga Malamulo, kuti ife timazindikira tchimo kupyolera mu Malamulo.
Masikin Balam jôm mindik sikin tute Pathien makunga dik intum theiruo nimak Balam chu miriem sietna inrietna mang kêng ani.
21 Koma tsopano chilungamo chochokera kwa Mulungu, osati chochokera ku Malamulo, chaonetsedwa. Ichi ndi chimene Malamulo ndi Aneneri amachitira umboni.
Atûn chu Pathien'n miriemngei dik a mintum lam a juong minlang zoi. Balamin ite atho rang ommak, Moses Balam le Dêipungeiin rietpuipu lei ni senla ngei khoma.
22 Timakhala olungama pamaso pa Mulungu pamene takhulupirira Yesu Khristu. Mulungu amachitira zimenezi anthu onse amene akhulupirira Khristu. Palibe kusiyana pakati pa Myuda ndi a mitundu ina,
Jisua Khrista an taksônna sikin Pathien'n mi thei a min chang ani, tukhom a iem murdi chu inteina reng ommak.
23 pakuti onse anachimwa naperewera pa ulemerero wa Mulungu
Mi murdi'n nunsie an tho zita, Pathien sanminjôkna hah an chang thei khâiloi ani.
24 ndipo onse alungamitsidwa mwaulere mwa chisomo chake chifukwa cha Khristu Yesu amene anawawombola.
Nikhomsenla, Khrista Jisua râtanna jârin Pathien'n a moroina sik vaiin ke mi a manboiin thei a min chang zoi.
25 Mulungu anamupereka Iyeyu kuti pokhetsa magazi ake, akhale nsembe yokhululukira machimo. Mulungu anachita zimenezi kufuna kuonetsa chilungamo chake. Chifukwa cha kuleza mtima kwake, sanalange anthu chifukwa cha machimo amene anachita kale.
Pathien'n ama hah ngâihoiin a pêka, ma anghan a thisena ama an taksônna sika mi murdi nunsie ngâidam anni narangin, mîn dik an chang theina rangin Pathien'n a tho ani. Zora lei vunsai han chu tuongdierin miriemngei nunsienangei chu riet khâiloiin a min vun ani. Pathien'n ama lelê midik ani tie le Jisua iem ngei murdi dik an chang ti minthârna rangin atûn lâihin mi dik a minchang lam hah a juong minlang ani hi.
26 Iye anachita izi kuti aonetse chilungamo chake lero lino. Anthu azindikire kuti Iye ndi wolungama ndipo amalungamitsa aliyense amene akhulupirira Yesu.
27 Nanga tsono pamenepa munthu anganyadenso? Kunyadatu kwachotsedwa. Chifukwa cha Malamulo? Kodi Malamulo samafuna ntchito za munthu? Ayi, koma mwachikhulupiriro.
Hanchu song rang mo ei dôn? dôn makme, itho sikin mo? balam jôm sika mini? nimak, iemna sika kêng ani.
28 Ife tikunenabe kuti munthu amalungamitsidwa mwachikhulupiriro osati mwakusunga Malamulo.
Masika han miriem hi Balam jôm sika Pathien kôm adik a chang niloiin, taksônna sikin kêng mîn dik an chang tiin kin min mong ani.
29 Kodi Mulungu ndi Mulungu wa Ayuda okha? Kodi si Mulungu wa a mitundu inanso? Inde wa a mitundu inanso,
Pathien chu Judangei ta rang uol mini? Jentailngei ta khom ani loi mini? O, ani sa.
30 popeza ndi Mulungu mmodzi yemweyo amene adzalungamitsa mwachikhulupiriro ochita mdulidwe ndi osachita mdulidwe kudzera mʼchikhulupiriro chomwecho.
Pathien chu inkhat ania, Juda sertanngei chu an taksônna sikin thei min chang ngei a ta, sertanloi Jentailngei khom an taksônna sik nanâk han thei min chang ngei atih.
31 Kodi tsono ife, tikutaya Malamulo pamene tikunena kuti pafunika chikhulupiriro? Ayi. Mʼnjira iliyonse ayi! Komatu ife tikukwaniritsadi Malamulo.
Hanchu taksônna ei misîr uol sikin Balam hah mangmunboia ei dar rak rang tina mini? Ni uol mak, Balam hah ei mindet ani.

< Aroma 3 >