< Chivumbulutso 19 >
1 Zitatha izi, ndinamva chimene chinamveka ngati phokoso la gulu lalikulu mmwamba likufuwula kuti, “Haleluya! Chipulumutso ndi ulemerero ndi mphamvu ndi za Mulungu wathu,
Lani yaa puoli n den gbaadi nani ya niligu n yaba ya fuugu tanpoli po ke bi tua: alleluya! ti Tienu n die mi tindima, ti kpiagidi leni u paaciamu.
2 pakuti chiweruzo chake ndi choona ndi cha chilungamo. Iye waweruza mkazi wadama wotchuka uja amene anayipitsa dziko lonse lapansi ndi zigololo zake. Iye wabwezera pa mkaziyo magazi a atumiki ake.”
Kelima o buudi tiegi, ki go tie moamoani. lani yaa po, o jia ti buudi ki cuo li poconconcianli, wani yua den joagini ki tinga leni o conconma. ki buali o naacenba soama panpaani o nuu nni.
3 Ndipo anafuwulanso kuti, “Haleluya! Utsi wochokera kwa mkazi wadamayo udzakwera kumwamba mpaka muyaya.” (aiōn )
Bi go den kpaani yedi ki yedi: alleluya! u fantañii baa do hali ya yogunu kuli. (aiōn )
4 Akuluakulu 24 aja ndi zamoyo zinayi zija anadzigwetsa pansi kupembedza Mulungu amene anakhala pa mpando waufumu. Ndipo anafuwula kuti, “Ameni, Haleluya!”
Bi piilie n nikpenaadiba leni a bonfuodinaada den gbaani ki kpiagi U Tienu yua n ka libalikalikaanu po ki yedi: Amina alleluya.
5 Kenaka mawu anachoka ku mpando waufumu kuti, “Lemekezani Mulungu wathu inu nonse atumiki ake, inu amene mumamuopa, nonse angʼono ndi akulu!”
U nialu den ñiani libalikalikaanu kani ki yedi: pagi mani ti Tienu, yinba o naacenba, yinba a bila leni a nikpela yaaba n fangi O.
6 Kenaka ndinamva chimene chinamveka ngati gulu lalikulu, ngati mkokomo wamadzi othamanga ndipo ngati kugunda kwakukulu kwa bingu, ndipo anati, “Haleluya! Pakuti Ambuye Mulungu wathu Wamphamvuzonse akulamulira.
Lani n den gbadi ku fuugu ke ku tie nani ya niligu n yaba ya fuugu, ki go tie nani mi ñincianma ya fuugu, leni itatantani ya fuugu yeni, ke ku tua: alleluya! kelima o Diedo, ti Tienu, u paaciamu kuli daano kua o diedima nni.
7 Tiyeni tisangalale ndi kukondwera ndi kumutamanda! Pakuti nthawi ya ukwati wa Mwana Wankhosa yafika, ndipo Mkwatibwi wakonzekeratu.
Tin mangi mani ti pala, ki ya pia li pamancianli ki kpiagi o, kelima ki pebiga potaali yogunu pundi, ke o pocaano bogini ki bobi.
8 Wapatsidwa nsalu yoyera kwambiri, yowala ndi yosada kuti avale.” (Nsalu yoyera kwambiri ikuyimira ntchito zolungama za oyera mtima).
Lani ke bi den puni o, ke wan bobi leni ya tiadi, ke ti pieni ki ñuliti ki ŋani cain kelima len ya tiadi tie bi nigagidiŋanba teginma.
9 Kenaka mngelo anandiwuza kuti, “Lemba kuti, Odala amene ayitanidwa ku phwando la ukwati wa Mwana Wankhosa.” Ndipo anatinso, “Awa ndiwo mawu woona a Mulungu.”
Lani maleki den yedi nni: Diani, li pamanli ye leni ban yini yaaba ki pebiga potaa- jiema po. O go den yedi nni: mi naa maama tie U Tienu n maadi ya moamoani.
10 Pamenepo ndinadzigwetsa pa mapazi ake kumupembedza. Koma anandiwuza kuti, “Usatero ayi, ine ndine mtumiki mnzako ngati iwe yemwe, ndiponso ngati abale ako amene asunga umboni wa Yesu. Pembedza Mulungu. Pakuti umboni wa Yesu ndiye mzimu wa uneneri.”
N den gbaani o taana kani ki baa kpiagi o, ama o den yedi nni da tieni yeni n tie fini leni a kpiiba yaaba n kubi Jesu ya siedi kuli ya tuonsoanbalielo yo, kpiagi U Tienu, kelima Jesu siedi tie mi naa sawali puama ñiali.
11 Ndinaona kumwamba kutatsekuka ndipo patsogolo panga panali kavalo woyera, amene anakwerapo dzina lake linali Wokhulupirika ndiponso Woona. Poweruza ndi kuchita nkhondo, amachita molungama.
Lani n den la ke tanpoli luodi, ke o tanpieno se, ke yua n den jagi o, yii o dugika leni o moamoandaano o bujiali tiegi, ki go tiendi bu toabu mo leni mi teginma.
12 Maso ake anali ngati malawi amoto, ndipo pamutu pake panali zipewa zaufumu zambiri. Anali ndi dzina lolembedwa, lodziwika ndi Iye yekha, osati wina aliyense.
O nuni tie nani mi fantama yeni, o den ciibi mu badifogilimu boncianla, o den pia li yeli ke li diani, yali ke oba kuli ki bani li, kali wani o ba.
13 Iye anavala mkanjo woviyika mʼmagazi, ndipo dzina lake ndi Mawu a Mulungu.
O den yie mi soama n yayadi ya tiayiekaagu po, o yeli tie U Tienu maama.
14 Magulu ankhondo akumwamba ankamutsatira atakwera pa akavalo oyera, ndipo iwowo atavala nsalu zoyera kwambiri ndi zosada.
Tanpoli toagola den ŋua o, ki jagi yi tanpieni, ki laa len ya tiapiendi ke ti ŋani cain.
15 Mʼkamwa mwake munatuluka lupanga lakuthwa limene anati akaphe nalo mitundu ya anthu. Iye adzalamulira ndi ndodo yachitsulo. Iye anaponda choponderamo mphesa cha ukali wa Mulungu Wamphamvuzonse.
Ya jugisiega n mani den ña o ñoabu nni, ki pua i nibuoli, o baa kpaaba ki muubi ti kuli badi gbianu. leni U Tienu u paaciamu kuli daano pabiencianli nni ke o ba ŋmaadi duven ŋanbikaanu.
16 Pa chovala ndi pa ntchafu pake panalembedwa dzina ili: MFUMU YA MAFUMU NDI MBUYE WA AMBUYE.
O den pia li yeli ke li diani o tiayekaagu leni o panli po: bi badiba Bado, leni bi diediba Diedo.
17 Ndipo ndinaona mngelo atayimirira pa dzuwa amene anafuwula ndi mawu okweza kwa mbalame zonse zowuluka mlengalenga kuti, “Bwerani, sonkhanani pamodzi ku phwando lalikulu la Mulungu.
N go den laa maleki, ke o se o yienu nni lani o den kpaani leni o nialu ciamu ki yedi ya bonyugiditi n yugi tanpoli nni kuli: cua mani ki taani U Tienu badijecianma kani.
18 Kuti mudye mnofu wa mafumu, wa akulu a ankhondo, ndi wa anthu amphamvu, wa akavalo ndi okwerapo awo, ndi wa anthu onse, mfulu ndi akapolo, angʼono ndi aakulu.”
Ki je bi badiba gbanandi, i taami leni bi tandanba gbanandi, i yonbi leni yaaba n die bi yula, a bila leni a nikpela kuli gbanandi.
19 Kenaka ndinaona chirombo chija ndi mafumu a dziko lapansi ndi magulu ankhondo atasonkhana pamodzi kuti achite nkhondo ndi wokwera pa kavalo ndi ankhondo ake.
N go den laa ki fuayanga leni bi badiba leni bi toagola, ke bi kuli taani ki baa tuogi bu toabu leni yua n jagi o tanpieno po leni O toagoli.
20 Koma chirombocho chinagwidwa pamodzi ndi mneneri wonyenga uja amene anachita zizindikiro zodabwitsa pamaso pake. Ndi zizindikirozi anasocheretsa amene analembedwa chizindikiro cha chirombocho napembedza fano lake. Onse awiri anaponyedwa amoyo mʼnyanja yamoto yasulufule wotentha. (Limnē Pyr )
O den cuo ki foayanga, wani leni o sawalipua tuofaadaano, yua n den tiendi mi bancianma ki nintuali ki boandi yaaba n den ga ki fuayanga maalima ki go gbaani ki kpiagi o nannanli O den luni banni bonbilie kuli ke bi fo ku fantanbuogu nni, li cidibili n co nani. (Limnē Pyr )
21 Ena onse anaphedwa ndi lupanga lija linatuluka mʼkamwa mwa wokwera pa kavalo uja, ndipo mbalame zonse zinadya mokwanira mnofu wa anthu akufawo.
Yua n den jagi o taamo po den kpa yaaba n sieni leni ya jugisiega n den ñia o ñoabu nni, ke ti bonyugiditi dini bi gbanandi ki guo.