< Chivumbulutso 18 >
1 Zitatha izi ndinaona mngelo wina akutsika kuchokera kumwamba. Iye anali ndi ulamuliro waukulu, ndipo dziko lapansi linawala ndi ulemerero.
Yaatidi, gita maati de7iya hara kiitanchchoy saloppe wodhdhishin ta be7as. He kiitanchchuwa bonchchoy sa7a poo7isis.
2 Mngeloyo anafuwula ndi mawu amphamvu kuti: “‘Wagwa! Wagwa Babuloni Wamkulu!’ Wasandulika mokhalamo ziwanda ndi kofikako mizimu yonse yoyipa ndi mbalame zonse zonyansa ndi zodetsedwa.
He kiitanchchoy ba qaala dhoqqu oothidi, “Iya kunddasu! Gita Baabilooney kunddasu! Baabilooney tuna ayyaanati aqiya bessi gidasu. Dumma dumma iitabatas keethe gidasu; tuna kafotinne do7ati shemppiya bessi gidasu.
3 Pakuti mayiko onse amwa vinyo ozunguza mutu wazigololo zake. Mafumu a dziko lapansi achita naye chigololo, ndipo amalonda a dziko lapansi analemera kuchokera pa zolakalaka zake zosefukira.”
Hiza, asa zerethi ubbaa ba laymatetha woyniya ushshasu. Sa7aa kawoti iira laymatidosona. I miikkotethaafe denddoyssan biittan de7iya zal77anchchoti durettidosona” yaagis.
4 Ndiponso ndinamva mawu ena kuchokera kumwamba akuti: “‘Anthu anga tulukani, mwa iye,’ mungachimwe naye kuti musadzalandire nawo gawo lililonse la miliri yake;
Hessafe guye, ta saloppe hayssada yaagiya hara qaala si7as. “I nagaraa iira koxonna melanne, iya ekkanaw de7iya seera hintte ekkonna mela, ta deriyaw iippe keyite.
5 pakuti machimo ake awunjikana mpaka kumwamba, ndipo Mulungu wakumbukira milandu yake.
Hiza, I nagaray salo gakkanaw doorettis. Xoossay I naaquwa akeekis.
6 Bwezerani Iye monga momwe iye anakuchitirani. Mubwezereni mowirikiza pa zimene anachita. Mumusakanizire magawo awiri kuchokera mʼchikho chake.
Iya immidayssa mela zaaridi iw immite. Iya oothida oosuwas nam77u kushe iw zaarite. Iya giigisida ushshaa bolla hintte nam77u kushe mathoya ushshaa I xuu7an kunthite.
7 Mumuzunze, kumumvetsa chisoni kwambiri monga mwaulemerero ndi zolakalaka zimene anadzaza mu mtima mwake. Iye anadzikuza nʼkumati, ‘Ndinakhala monga mfumu yayikazi, ine sindine wamasiye ndipo sindidzalira maliro.’
Iya baw bonchchettidayssadanne iw injjetidayssa mela, iyo metoothitenne kayoyite. Iya ba wozanan, ‘Taani kaweeda uttas; ta azini baynna maccas gidikke; taani ubbaka kayottike’ yaagasu.
8 Chifukwa chake miliri yake idzamugonjetsa tsiku limodzi; imfa, kulira maliro ndi njala. Iye adzanyeka ndi moto pakuti wamphamvu ndi Mulungu Ambuye amene wamuweruza.
Hessa gisho, bosha ubbay, harggey, kayoynne koshi iyo issi gallas oykkana. Qassi iya taman xuugettana; ays giikko, I bolla pirddiya Xoossay wolqqaama” yaagis.
9 “Mafumu a dziko lapansi, amene anachita naye chigololo nachita naye pamodzi zosangalatsa moyo uno, akadzaona utsi wa kunyeka kwake, adzalira nakhuza maliro ake.
“Iira laymatidayssatinne I miikkotethan de7ida, alamiya kawoti he katamiya xuugettin keyaa cuya be7ida wode iw waassidi yeekkana.
10 Iwo adzayima kutali nalira chifukwa choopsedwa ndi mazunzo ake. “‘Tsoka! Tsoka mzinda waukulu iwe, Babuloni mzinda wamphamvu! Mu ora limodzi chiwonongeko chako chafika!’
Entti he katamee waaya be7idi yayyida gisho, haakki eqqidi, ‘Ha gita katamee! Wolqqaama katamee! Baabiloonee, nena ayye! Neeni issi saate giddon ne pirdda ekkadasa’ yaagana.
11 “Amalonda a dziko lapansi adzalira nakhuza maliro ake chifukwa palibenso amene akugula katundu wawo,
“Entta markkabiya caanaa hizappe shammiya asi baynna gisho, sa7an de7iya zal77anchchoti he katamaas waassananne kayottana.
12 katundu wagolide, siliva, miyala yamtengo wapamwamba ndi ngale; nsalu zoyera kwambiri zapamwamba ndi zofiira; nsalu zasilika ndi zapepo; mitengo iliyonse yonunkhira ndi zinthu zilizonse zopangidwa ndi mnyanga, kapena matabwa ogulidwa ndi ndalama zambiri kapena mkuwa kapena chitsulo ndi mwala wonyezimira;
Entta worqqaa, biraa, bonchcho shuchchaa, inqo giya al77o shuchchaa, kaalose ma7o, liino ma7o, haare ma7o, zo7o ma7o, dumma dumma sawo mithaa, zaale, al77o mithaa, naase biraata, goole shuchchu,
13 zokometsera zakudya, mure, lubani ndi zofukiza zina, vinyo ndi mafuta a olivi, ufa wosalala ndi tirigu; ngʼombe ndi nkhosa; akavalo ndi ngolo; ndi anthu adzagulitsidwa ukapolo.
qarafa, qimame, ixaane, karbbe, shitto, woyne, zayte, liiqo dhiille, gistte, mehe, dorsse, paraa, para gaare, aylletanne hara asata shammiya oonikka baawa.
14 “Iwo adzanena kuti, ‘Chipatso chimene unachilakalaka chakuchokera. Chuma chako chonse ndi ulemerero zatha, sizidzapezekanso.’
“Zal77anchchoti maccaseekko, ‘Neeni amottida lo77obaa ubbay neeppe dhays. Ne aqoynne alleeqettidabaa ubbay neeppe haakkis. Neeni zaarada entta ubbaa demmaka’ yaagidosona.
15 Amalonda amene anagulitsa zinthu izi napeza chuma kuchokera kwa iye adzayima patali potero ataopsedwa ndi mazunzo ake. Adzalira ndi kukhuza maliro
He kataman zal77idi durettida zal77anchchoti I metuwa babbidi iippe haakkidi eqqana. Entti yeekkananne kayottana.
16 ndipo adzalira mokuwa kuti, “‘Tsoka! Tsoka! Mzinda waukulu, iwe wovala nsalu zoyera kwambiri, zapepo ndi zofiira, ndi wonyezimira ndi golide, miyala yamtengo wapamwamba ndi ngale!
Qassi, ‘Liino ma7o, kaalose ma7onne zo7o ma7o ma77ada, worqqan, bonchcho shuchchaninne inqo giya al77o shuchchan alleeqettida, he gita katamees ayye!
17 Chuma chambiri choterechi chafika powonongeka mu ora limodzi!’ “Oyendetsa sitima ndi onse oyenda pa sitima ya pamadzi, ogwira ntchito mʼsitima ndi onse amene amadalira nyanja pamoyo wa tsiku ndi tsiku adzayima patali potero.
Hayssa mela gita shalo ubbay issi saate giddon dhays’ yaagidosona. Markkabiya laaggiya ubbay, markkabiyan biya ubbay, markkabiya bolla oothiya ubbaynne abban zal77iya ubbay haakki eqqidosona.
18 Akadzaona utsi wa kunyeka kwake, adzakuwa kuti, ‘Kodi panalinso mzinda wina ngati mzinda waukuluwu?’
He katamiya xuugettin keyaa cuya be7ida wode, “Ha gita katamiw daaniya hara katami de7ishshaa?” yaagidosona.
19 Adzathira fumbi pamitu pawo ndipo adzalira nakhuza maliro kuti, “Tsoka! Tsoka mzinda waukulu iwe, kumene onse anali ndi sitima pa nyanja analemera kudzera mʼchuma chake! Mu ora limodzi wawonongedwa.
Entti bantta huu7en baana qolidi, waassidosonanne kayottidosona. “Abbaa bolla markkabeti de7iya ubbay, I shaluwan durettida ubbay, he katamiya issi saaten dhayida gisho, ayye! Ayye!
20 “Kondwerani chifukwa cha iye inu kumwamba! Kondwerani oyera mtima ndi atumwi ndi aneneri! Mulungu wamuweruza iye monga momwe anakuchitirani inu.”
Saluwaw, I dhayuwan ufaytta! Geeshshato, hawaareto, nabeto, Xoossay hintte gisho I bolla pirddida gisho ufayttite.” yaagidosona.
21 Kenaka mngelo wamphamvu ananyamula mwala waukulu ngati mphero yayikulu nawuponya mʼnyanja nanena kuti, “Mwa mphamvu chonchi mzinda waukulu wa Babuloni udzaponyedwa pansi, sudzapezekanso.
Yaatin, mino kiitanchchoy woxa daaniya gita shuchchu denthidi abban holishe, “Gita katamiya Baabilooney wolqqan holettada hayssada kunddana; iya hachchife guye ubbaka benttuku.
22 Mwa iwe simudzamvekanso liwu la woyimba zeze, ndi akatswiri a zoyimbayimba, oyimba zitoliro, ndi lipenga. Mwa iwe simudzapezekanso mʼmisiri wina aliyense. Mwa iwe simudzapezekanso phokoso la mphero.
Diithi diixeyssatinne yexeyssati, suusul77enne moyze punneyssati, hizappe guye ne giddon ubbaka si7ettokona. Ay kochcha zal77e zal77iya asikka ne giddon benttenna. Woxa girssi hizappe guye ne giddon si7ettenna.
23 Kuwala kwa nyale sikudzawunikanso mwa inu. Mawu a mkwati ndi mkwatibwi sadzamvekanso mwa iwe. Amalonda anu anali akuluakulu a dziko lapansi. Mitundu yonse inasokonezedwa ndi zamatsenga zako.
xomppe poo7oy zaaridi ne giddon poo7enna. Machcho ekkeysinne azina geliyari qaali hizappe guye ne giddon si7ettenna. Ne zal77anchchoti biitta ubban erettida wolqqaamata. Ne bitan kawotethata ubbaa cimmadasa” yaagis.
24 Mwa iye munapezeka magazi a aneneri ndi a oyera mtima, ndi onse amene anaphedwa pa dziko lapansi.”
Nabeta suuthay, geeshshata suuthaynne biitta bolla hayqqida asa ubbaa suuthay I giddon benttida gisho Baabilooney pirddettasu.