< Masalimo 1 >

1 Wodala munthu amene satsatira uphungu wa anthu ochimwa, kapena kuyima mʼnjira ya anthu oyipa, kapena kukhala mʼmagulu a anthu onyoza.
Blahoslavený ten muž, kterýž nechodí po radě bezbožných, a na cestě hříšníků nestojí, a na stolici posměvačů nesedá.
2 Koma chikondwerero chake chili mʼmalamulo a Yehova ndipo mʼmalamulo akewo amalingaliramo usana ndi usiku.
Ale v zákoně Hospodinově jest líbost jeho, a v zákoně jeho přemýšlí dnem i nocí.
3 Iye ali ngati mtengo wodzalidwa mʼmbali mwa mitsinje ya madzi, umene umabereka zipatso zake pa nyengo yake ndipo masamba ake safota. Chilichonse chimene amachita amapindula nacho.
Nebo bude jako strom štípený při tekutých vodách, kterýž ovoce své vydává časem svým, jehožto list nevadne, a cožkoli činiti bude, šťastně mu se povede.
4 Sizitero ndi anthu oyipa! Iwo ali ngati mungu umene umawuluzidwa ndi mphepo.
Ne takť budou bezbožní, ale jako plevy, kteréž rozmítá vítr.
5 Kotero anthu oyipa sadzatha kuyima pa chiweruzo, kapena anthu ochimwa mu msonkhano wa anthu olungama.
A protož neostojí bezbožní na soudu, ani hříšníci v shromáždění spravedlivých.
6 Pakuti Yehova amayangʼanira mayendedwe a anthu olungama, koma mayendedwe a anthu oyipa adzawonongeka.
Neboť zná Hospodin cestu spravedlivých, ale cesta bezbožných zahyne.

< Masalimo 1 >