< Masalimo 99 >
1 Yehova akulamulira, mitundu ya anthu injenjemere; Iye wakhala pa mpando wake waufumu, pakati pa akerubi, dziko lapansi ligwedezeke.
HERREN är nu konung! Därför darra folken. Han som tronar på keruberna! Därför skälver jorden.
2 Mʼziyoni wamkulu ndi Yehova; Iye ndi wokwezeka pamwamba pa mitundu yonse ya anthu.
HERREN är stor i Sion, och upphöjd är han över alla folk.
3 Anthu atamande dzina lanu lalikulu ndi loopsa kwambiri, Iye ndi woyera.
Därför prisar man ditt namn, det stora och fruktansvärda. Helig är han.
4 Mfumu yamphamvu, iyo imakonda chilungamo Inu mwakhazikitsa khalidwe losakondera; mwachita zolungama ndi zoyenera mwa Yakobo.
Och konungen i sin makt älskar vad rätt är. Ja, du håller rättvisa vid makt, rätt och rättfärdighet övar du i Jakob.
5 Kwezani Yehova Mulungu wathu ndipo mulambireni pa mapazi ake; Iye ndi woyera.
Upphöjen HERREN, vår Gud, och tillbedjen vid hans fotapall. Helig är han.
6 Mose ndi Aaroni anali ena mwa ansembe ake, Samueli anali pamodzi ndi iwo amene anayitana pa dzina lake; iwo anayitana Yehova ndipo Iyeyo anawayankha.
Mose och Aron voro bland hans präster, och Samuel bland dem som åkallade hans namn; de ropade till HERREN, och han svarade dem.
7 Iye anayankhula nawo kuchokera mʼchipilala cha mtambo; iwo anasunga malamulo ake ndi zophunzitsa zomwe anawapatsa.
I molnstoden talade han då till dem; de höllo hans vittnesbörd och den lag som han gav dem.
8 Inu Yehova Mulungu wathu, munawayankha iwo; Inu kwa Israeli munali Mulungu wokhululuka, ngakhale munawalanga pa zochita zawo zoyipa.
Ja, HERRE, vår Gud, du svarade dem; du var mot dem en förlåtande Gud -- och en hämnare över deras gärningar.
9 Kwezani Yehova Mulungu wathu ndipo mumulambire pa phiri lake loyera, pakuti Yehova Mulungu wathu ndi woyera.
Upphöjen HERREN, vår Gud, och tillbedjen inför hans heliga berg. Ty helig är HERREN, vår Gud.