< Masalimo 98 >
1 Salimo. Imbirani Yehova nyimbo yatsopano, pakuti Iyeyo wachita zinthu zodabwitsa; dzanja lake lamanja ndi mkono wake woyera zamuchitira chipulumutso.
Um salmo. Cante para Yahweh uma nova canção, pois ele tem feito coisas maravilhosas! Sua mão direita e seu braço sagrado trabalharam a salvação para ele.
2 Yehova waonetsa chipulumutso chake ndipo waulula chilungamo chake kwa anthu a mitundu ina.
Yahweh deu a conhecer sua salvação. Ele demonstrou abertamente sua retidão aos olhos das nações.
3 Iye wakumbukira chikondi chake ndi kukhulupirika kwake pa Aisraeli; malekezero onse a dziko lapansi aona chipulumutso cha Mulungu wathu.
Ele se lembrou de sua bondade amorosa e de sua fidelidade para com a casa de Israel. Todos os confins da Terra viram a salvação de nosso Deus.
4 Fuwulani mwachimwemwe kwa Yehova, dziko lonse lapansi, muyimbireni nyimbo mofuwula ndi mokondwera.
Make um alegre barulho para Yahweh, toda a terra! Explodir e cantar por alegria, sim, cantar louvores!
5 Imbirani Yehova nyimbo ndi zeze, ndi zeze ndi mawu a kuyimba,
Cante louvores a Javé com a harpa, com a harpa e a voz da melodia.
6 ndi malipenga ndi kuliza kwa nyanga ya nkhosa yayimuna fuwulani mwachimwemwe pamaso pa Yehova Mfumu.
Com trombetas e som da buzina do carneiro, fazer um barulho alegre diante do Rei, Yahweh.
7 Nyanja ikokome pamodzi ndi zonse zili mʼmenemo, dziko lonse ndi onse amene amakhala mʼmenemo.
Deixe o mar bramir com sua plenitude; o mundo, e aqueles que nele habitam.
8 Mitsinje iwombe mʼmanja mwawo, mapiri ayimbe pamodzi mwachimwemwe;
Let os rios batem palmas. Deixem as montanhas cantarem juntas por alegria.
9 izo ziyimbe pamaso pa Yehova, pakuti Iye akubwera kudzaweruza dziko lapansi. Adzaweruza dziko lonse mwachilungamo, ndi mitundu ya anthu mosakondera.
Let eles cantam antes de Yahweh, pois ele vem para julgar a terra. Ele julgará o mundo com retidão, e os povos com equidade.