< Masalimo 97 >
1 Yehova akulamulira, dziko lapansi lisangalale; magombe akutali akondwere.
HERREN är nu konung! Därför fröjde sig jorden; havsländerna glädje sig, så många som de äro.
2 Mitambo ndi mdima waukulu zamuzungulira; chilungamo ndi kuweruza molungama ndiwo maziko a mpando wake waufumu.
Moln och töcken omgiva honom, rättfärdighet och rätt äro hans trons fäste.
3 Moto umapita patsogolo pake ndi kunyeketsa amaliwongo kumbali zonse.
Eld går framför honom och förbränner hans ovänner runt omkring.
4 Zingʼaningʼani zake zimawalitsa dziko lonse; dziko lapansi limaona ndipo limanjenjemera.
Hans ljungeldar lysa upp jordens krets; jorden ser det och bävar.
5 Mapiri amasungunuka ngati phula pamaso pa Yehova, pamaso pa Ambuye a dziko lonse lapansi.
Bergen smälta såsom vax för HERREN, för hela jordens Herre.
6 Mayiko akumwamba amalengeza za chilungamo chake, ndipo mitundu yonse ya anthu imaona ulemerero wake.
Himlarna förkunna hans rättfärdighet, och alla folk se hans ära.
7 Onse amene amalambira mafano osema amachititsidwa manyazi, iwo amene amanyadira mafano; mulambireni, inu milungu yonse!
Alla de skola komma på skam, som dyrka beläten, de som berömma sig av avgudar. Alla gudar skola tillbedja honom.
8 Ziyoni akumva ndipo akukondwera, midzi ya Yuda ikusangalala chifukwa cha maweruzo anu Yehova.
Sion hör det och gläder sig, och Juda döttrar fröjda sig för dina domars skull, HERRE.
9 Pakuti Inu Yehova ndi Wammwambamwamba pa dziko lonse lapansi; ndinu wokwezeka kupambana milungu yonse.
Ty du, HERRE, är den Högste över hela jorden; du är högt upphöjd över alla gudar.
10 Iwo amene amakonda Yehova adane ndi zoyipa pakuti Iye amayangʼanira miyoyo ya amene amamukhulupirira ndipo amawapulumutsa mʼdzanja la anthu oyipa
I som älsken HERREN, haten det onda. Han bevarar sina frommas själar, ur de ogudaktigas hand räddar han dem.
11 Kuwala kumafika pa anthu olungama, ndi chimwemwe kwa olungama mtima.
Ljus är utsått för den rättfärdige och glädje för de rättsinniga.
12 Kondwerani mwa Yehova Inu olungama ndipo tamandani dzina lake loyera.
Glädjens, I rättfärdige, i HERREN, och prisen hans heliga namn.