< Masalimo 95 >
1 Bwerani, tiyeni timuyimbire Yehova mwachimwemwe, tiyeni tifuwule kwa Thanthwe la chipulumutso chathu
KOMAIL kodo, pwe kitail pan kapina Ieowa o nijinij on paip en maur atail.
2 Tiyeni tibwere pamaso pake ndi chiyamiko ndipo mupembedzeni Iyeyo ndi zida zoyimbira ndi nyimbo.
Kitail pan kola tuki on i kapin. Kitail en nijinijki on I pjalm!
3 Pakuti Yehova ndi Mulungu wamkulu, mfumu yayikulu pamwamba pa milungu yonse.
Pwe Ieowa Kot lapalap amen, o Nanmarki lapalap amen pon anin kot akan karoj.
4 Mʼmanja mwake muli maziko ozama a dziko lapansi, ndipo msonga za mapiri ndi zake.
Pan jappa mi ni lim a, o pon komon nana me japwilim a.
5 Nyanja ndi yake, pakuti anayilenga ndi Iye, ndipo manja ake anawumba mtunda wowuma.
Madau me japwilim a, pwe i me kotin wiadar, o lim a kan wiadar waja madekon.
6 Bwerani, tiyeni tiwerame pomulambira, tiyeni tigwade pamaso pa Yehova Mlengi wathu;
Komail kodo, kitail pan kaudok, o dairukedi, o kelepuki mon Ieowa, me kotin wia kitail dar.
7 pakuti Iye ndiye Mulungu wathu ndipo ife ndife anthu a pabusa pake, ndi nkhosa za mʼdzanja lake. Lero ngati inu mumva mawu ake,
Pwe i atail Kot, a kitail aramaj en japwilim a wajan kamana o pwin en lim a. Ran wet, ma komail pan ron kapitie,
8 musawumitse mitima yanu monga momwe munachitira pa Meriba, monga munachitira tsiku lija pa Masa mʼchipululu.
Komail der kapitakaila monion omail, duen a wiauier Meripa o ni ran en Maja nan jap tan.
9 Kumene makolo anu anandiyesa ndi kundiputa, ngakhale anaona zimene Ine ndinazichita.
Ni jam omail akan jonejon ia o kajau ia da, pwe re kilaner ai dodok kan.
10 Kwa zaka makumi anayi ndinali wokwiya ndi mʼbado umenewo; ndipo ndinati, “Iwo ndi anthu amene mitima yawo imasochera ndipo sanadziwe njira zanga.”
Par paeijok I juede kilar di wet, o I indada: Monion en jon en aramaj duen met kin wukiwuk jili, o re jota men aja duen al ai kan.
11 Choncho ndili chikwiyire, ndinalumbira kuti, “Iwowa sadzalowa ku malo anga a mpumulo.”
I ap kaula ni ai makar: Irail jota pan konodi ai kamol.