< Masalimo 93 >

1 Yehova akulamulira, wavala ulemerero; Yehova wavala ulemerero ndipo wadzimangirira mphamvu, dziko lonse lakhazikika kolimba; silingasunthidwe.
LEUM GOD El tokosra, El nuknukyang ke wal a ku. Faclu oakwuki ku, Ac fah tiana mukuikui.
2 Mpando wanu waufumu unakhazikika kalekale; Inu ndinu wamuyaya.
Tron lom, LEUM GOD, nuna oakwuki ku oe ke mutawauk me, A kom nuna muta meet liki mutaweyen pacl u.
3 Nyanja zakweza Inu Yehova, nyanja zakweza mawu ake; nyanja zakweza mafunde ake ochita mkokomo.
Yen loal meoa srukak pusralos, O LEUM GOD, Elos srukak pusralos a ngirngir.
4 Yehova ndi wamphamvu kupambana mkokomo wa madzi ambiri, ndi wamphamvu kupambana mafunde a nyanja, Yehova mmwamba ndi wamphamvu.
LEUM GOD El leum fulat inkusrao, El fulat liki ngirngir lun meoa, A ku liki noa in meoa u.
5 Malamulo anu Yehova ndi osasinthika; chiyero chimakongoletsa nyumba yanu mpaka muyaya.
Ma sap lom oan nwe tok, LEUM GOD, A Tempul lom arulana mutal, Ma pahtpat a ma pahtpat.

< Masalimo 93 >