< Masalimo 92 >

1 Salimo. Nyimbo ya pa tsiku la Sabata. Nʼkwabwino kutamanda Yehova ndi kuyimbira nyimbo dzina lanu, Inu Wammwambamwamba,
Dziesma svētdienā dziedama. Laba lieta ir, To Kungu slavēt un dziedāt Tavam Vārdam, Tu Visuaugstākais,
2 Kulengeza chikondi chanu mmawa, ndi kukhulupirika kwanu nthawi ya usiku,
Rītos izteikt Tavu žēlastību un naktīs Tavu uzticību,
3 kuyimbira nyimbo choyimbira cha zingwe khumi ndi mayimbidwe abwino a zeze.
Uz tām desmit stīgām un uz stabulēm, ar spēlēšanu uz koklēm.
4 Pakuti Inu mumandisangalatsa ndi ntchito zanu, Inu Yehova; Ine ndikuyimba mwachimwemwe pa ntchito ya manja anu.
Jo, Kungs, Tu mani iepriecini ar Saviem darbiem; es gavilēju par to, ko Tava roka dara.
5 Ndi yayikuludi ntchito yanu Yehova, maganizo anu ndi ozamadi!
Ak Kungs, cik lieli ir Tavi darbi, cik ļoti dziļas Tavas domas!
6 Munthu wopanda nzeru sadziwa, zitsiru sizizindikira,
Nejēga to neatzīst, un ģeķis to nesaprot.
7 kuti ngakhale anthu oyipa aphuka ngati udzu ndipo anthu onse ochita zoyipa apindula, adzawonongedwa kwamuyaya.
Gan bezdievīgie zaļo kā zāle, un visi ļauna darītāji zeļ; tomēr tie top izdeldēti mūžīgi mūžam.
8 Koma Inu Yehova, ndinu wokwezedwa kwamuyaya.
Bet Tu, Kungs, esi tas augstākais mūžīgi.
9 Zoonadi adani anu Yehova, zoonadi adani anu adzawonongeka; onse ochita zoyipa adzabalalitsidwa.
Jo redzi, Tavi ienaidnieki, ak Kungs, redzi, Tavi ienaidnieki iet bojā, visi ļaundarītāji top izkaisīti.
10 Inu mwakweza nyanga yanga ngati nyanga ya njati; mafuta abwino akhuthulidwa pamutu wanga.
Bet Tu paaugstini manu ragu kā vērša ragu; es esmu apliets ar jaunu eļļu.
11 Maso anga aona kugonjetsedwa kwa olimbana nane, makutu anga amva za kugwa kwa amaliwongo anga oyipa.
Un manas acis uzlūko ar prieku manus nicinātājus, manas ausis iepriecinājās par tiem, kas ļaunā prātā pret mani ceļas.
12 Anthu olungama adzaphuka ngati mtengo wa mgwalangwa, adzakula ngati mkungudza wa ku Lebanoni;
Taisnais zaļo kā palma koks, viņš aug kā ciedru koks uz Lībanus.
13 odzalidwa mʼnyumba ya Yehova, adzakula bwino mʼmabwalo a Mulungu wathu.
Kas Tā Kunga namā ir stādīti, tie zaļo mūsu Dieva pagalmos.
14 Iwo adzaberekabe zipatso mu ukalamba wawo, adzakhala anthete ndi obiriwira,
Vēl pašā vecumā tie nes augļus, tie ir auglīgi un zaļi,
15 kulengeza kuti, “Yehova ndi wolungama; Iye ndiye Thanthwe langa, ndipo mwa Iye mulibe choyipa.”
Un stāsta, ka Tas Kungs, mans patvērums, ir taisns, un netaisnības nav pie Viņa.

< Masalimo 92 >