< Masalimo 9 >

1 Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Monga mwa mayimbidwe a nyimbo ya “Imfa ya Mwana.” Salimo la Davide. Ine ndidzakutamandani, Inu Yehova, ndi mtima wanga wonse; ndidzafotokoza za zodabwitsa zanu zonse.
Rengeko an-kaliforan-troke irehe r’Iehovà; ho talilieko iaby o halatsa’oo.
2 Ndidzakondwa ndi kusangalala mwa inu; Ndidzayimba nyimbo zamatamando pa dzina lanu, Inu Wammwambamwamba.
Hifaleako naho hirebehako, ho saboeko i tahina’oy, ry Andindimoneñe.
3 Adani anga amathawa, iwo amapunthwa ndi kuwonongedwa pamaso panu.
Ie mimpoly o rafelahikoo, le mikorovoke vaho mibaibay añ’atrefa’o ey.
4 Pakuti Inu mwatsimikiza za kulungama kwanga ndi mlandu wanga; Inu mwakhala pa mpando wanu waufumu, kuweruza mwachilungamo.
Fa nitohañe’o i naseseko mahitiy, ihe miambesatse am-piambesa’o eo, mizaka an-kavantañañe.
5 Mwadzudzula mitundu ya anthu ndipo mwawononga anthu oyipa; Inu mwafafaniza dzina lawo kwamuyaya.
Nendaha’o o kilakila ‘ndatio, rinotsa’o o lo-tserekeo; finaopao’o kitro katroke ty añara’ iareo.
6 Chiwonongeko chosatha chagwera adani, mwafafaniza mizinda yawo; ngakhale chikumbutso chawo chawonongedwa.
O ry rafelahio, fa nampigadoñeñe an-koak’ao kitro katroke; fa nombota’o o rovao, fa momoke ty fitiahiañe iareo.
7 Yehova akulamulira kwamuyaya; wakhazikitsa mpando wake waufumu woweruzira.
Toe am-piambesa’e eo nainai’e t’Iehovà, fa nihentseña’e ho an-jaka i fiambesa’ey;
8 Iye adzaweruza dziko mwachilungamo; adzalamulira mitundu ya anthu mosakondera.
an-katò ty fizaka’e ty voatse toy, ho zakae’e an-kahiti’e ondatio.
9 Yehova ndiye kothawirako kwa opsinjika mtima, linga pa nthawi ya mavuto.
Kijoly abo te amo forekekeñeo t’Iehovà, fitsolohañe an-tsan-kasotriañe;
10 Iwo amene amadziwa dzina lanu adzadalira Inu, pakuti Inu Yehova, simunawatayepo amene amafunafuna inu.
Hiantok’ azo o mahafohiñe ty tahina’oo, amy te tsy aforintse’o ze mipay Azo, ry Iehovà,
11 Imbani nyimbo zamatamando kwa Yehova, ali pa mpando waufumu mu Ziyoni; lengezani pakati pa mitundu ya anthu zimene wachita.
Misaboa am’ Iehovà ry mpimoneñe e Tsiône ao! tseizo am’ ondatio o fitoloña’eo!
12 Pakuti Iye amene amabwezera chilango akupha anzawo wakumbukira; Iye salekerera kulira kwa ozunzika.
Toe ihaoñe’ i Mpamale Fatey; tsy haliño’e ty fikoiaha’ o mpisotrio.
13 Inu Yehova, onani momwe adani anga akundizunzira! Chitireni chifundo ndipo ndichotseni pa zipata za imfa,
Isoho iraho, ry Iehovà! Vazohò ty haoreako am-pità’ o malaiñe ahio; Ihe Mpañonjoñe ahy boak’ an- dalam-bein-kavilasy ao,
14 kuti ndilengeze za matamando anu pa zipata za ana aakazi a Ziyoni, kuti pamenepo ndikondwere ndi chipulumutso chanu.
ho talilieko iaby ty enge’o amo lalam-bei’ i anak-ampela’ i Tsiôneio, hirebehako o fandrombaha’oo.
15 Mitundu ya anthu yagwa mʼdzenje limene yakumba; mapazi awo akodwa mu ukonde umene anawubisa.
Nijoroboñe amy koboñe hinali’iereoy o fifeheañeo; finandri’ ty harato naeta’iareo o fandia’iareoo.
16 Yehova amadziwika ndi chilungamo chake; oyipa akodwa ndi ntchito za manja awo. Higayoni. (Sela)
Fa nampandrendre-batañe t’Iehovà fa nametsake zaka: tsepaheñ’ amo satan-taña’eo avao ty lo-tsereke. [mahantseñantseñe, Selà]
17 Oyipa amabwerera ku manda, mitundu yonse imene imayiwala Mulungu. (Sheol h7585)
Himpoly mb’an-tsikeokoek’ ao o tsivokatseo, ze kilakila’ ondaty mandikok’ an’Andrianañahare. (Sheol h7585)
18 Koma osowa sadzayiwalika nthawi zonse, kapena chiyembekezo cha ozunzika kutayika nthawi zonse.
Fe tsy ho haliño nainai’e o rarakeo vaho tsy ho modo kitro añ’afe’e ty fisalalà’ o mpisotrio.
19 Dzukani Inu Yehova, musalole munthu kuti apambane; mitundu yonse iweruzidwe pamaso panu.
Miongaha ry Iehovà, ko anga’o handrekets’ ondatio; Ho zakaeñe am-pivazohoa’o eo o fifeheañeo!
20 Akantheni ndi mantha aakulu, Inu Yehova; mitundu idziwe kuti iwo ndi anthu wamba. (Sela)
Apoho am’ iareo ty fangebahebahañe, ry Iehovà ampahafohino o kilakila’ndatio t’ie ondaty avao! Selà

< Masalimo 9 >