< Masalimo 87 >

1 Salimo la Ana a Kora. Iye wakhazikitsa maziko ake pa phiri loyera;
Kora mma dwom. Awurade ato ne fapem wɔ bepɔ kronkron no so;
2 Yehova amakonda zipata za Ziyoni kupambana malo onse okhalamo a Yakobo.
Awurade dɔ Sion apono no sene Yakob atenaeɛ nyinaa.
3 Za ulemerero wako zimakambidwa, Iwe mzinda wa Mulungu: (Sela)
Wɔka wo ho animuonyamsɛm Ao Onyankopɔn kuropɔn:
4 “Ndidzanena za Rahabe ndi Babuloni pakati pa iwo amene amandidziwa. Dzikonso la Filisitiya, Turo pamodzi ndi Kusi, ndipo ndidzati, ‘Uyu anabadwira mʼZiyoni.’”
“Mede Rahab ne Babilonia bɛka wɔn a wɔyɛ ɔsetie ma me no ho, Filistia, Tiro ne Kus nso mɛka sɛ, ‘Wɔwoo yeinom wɔ Sion.’”
5 Ndithudi, za Ziyoni adzanena kuti, “Uyu ndi uyo anabadwira mwa iye, ndipo Wammwambamwamba adzakhazikitsa iyeyo.”
Ampa ara wɔbɛka wɔ Sion ho sɛ, “Wɔwoo yei ne ɔno wɔ ne mu, na Ɔsorosoroni no ankasa de no bɛtim hɔ.”
6 Yehova adzalemba mʼbuku la kawundula wa anthu a mitundu ina: “Uyu anabadwira mʼZiyoni.” (Sela)
Awurade bɛtwerɛ wɔ nnipa dintwerɛ nwoma no mu sɛ, “Wɔwoo yei wɔ Sion.”
7 Oyimba ndi ovina omwe adzati, “Akasupe anga onse ali mwa iwe.”
Na wɔbɛto dwom sɛ, “Me nhini nyinaa wɔ wo mu.”

< Masalimo 87 >