< Masalimo 87 >
1 Salimo la Ana a Kora. Iye wakhazikitsa maziko ake pa phiri loyera;
[Psalm Lun Tulik Natul Korah] LEUM GOD El musaela siti sel fineol mutal.
2 Yehova amakonda zipata za Ziyoni kupambana malo onse okhalamo a Yakobo.
El lungse siti Jerusalem Yohk liki kutena acn saya in Israel.
3 Za ulemerero wako zimakambidwa, Iwe mzinda wa Mulungu: (Sela)
Porongo, O kowos su mwet in siti lun God, Ke ma wolana ma El fahk keiwos:
4 “Ndidzanena za Rahabe ndi Babuloni pakati pa iwo amene amandidziwa. Dzikonso la Filisitiya, Turo pamodzi ndi Kusi, ndipo ndidzati, ‘Uyu anabadwira mʼZiyoni.’”
“Nga ac fah oakla acn Egypt ac Babylonia Ke nga takunla inen mutunfacl su akosyu; Mwet Philistia, Tyre, ac Ethiopia Nga ac fah oakalos pac inmasrlon mwet su muta Jerusalem.”
5 Ndithudi, za Ziyoni adzanena kuti, “Uyu ndi uyo anabadwira mwa iye, ndipo Wammwambamwamba adzakhazikitsa iyeyo.”
Ac mwet uh fah fahk Tuh mutanfahl nukewa elos mwet Zion, Ac El su Kulana fah oru tuh Zion in ku.
6 Yehova adzalemba mʼbuku la kawundula wa anthu a mitundu ina: “Uyu anabadwira mʼZiyoni.” (Sela)
LEUM GOD El ac simusla inen mwet inge, Ac oakalosyang nukewa nu ke mwet Jerusalem.
7 Oyimba ndi ovina omwe adzati, “Akasupe anga onse ali mwa iwe.”
Elos ac fah onsrosro ac fahk, “Mwe insewowo lasr nukewa tuku Zion me.”