< Masalimo 87 >

1 Salimo la Ana a Kora. Iye wakhazikitsa maziko ake pa phiri loyera;
Ein Psalmlied der Söhne Korahs. / Er hat es gegründet auf heiligen Bergen.
2 Yehova amakonda zipata za Ziyoni kupambana malo onse okhalamo a Yakobo.
Zions Tore liebt Jahwe mehr / Als alle Wohnungen Jakobs.
3 Za ulemerero wako zimakambidwa, Iwe mzinda wa Mulungu: (Sela)
Herrliches ist über dich verheißen, / O du Stadt Elohims. (Sela)
4 “Ndidzanena za Rahabe ndi Babuloni pakati pa iwo amene amandidziwa. Dzikonso la Filisitiya, Turo pamodzi ndi Kusi, ndipo ndidzati, ‘Uyu anabadwira mʼZiyoni.’”
"Ich nenne Rahab und Babel als meine Bekenner. / Ja, von Philistäa und Tyrus samt Kusch sag ich: / ['Diese sind dort geborn.'"
5 Ndithudi, za Ziyoni adzanena kuti, “Uyu ndi uyo anabadwira mwa iye, ndipo Wammwambamwamba adzakhazikitsa iyeyo.”
Aber von Zion wird's heißen: / "Jeder ist da geboren, / Und er selbst, der Höchste, erhält es."
6 Yehova adzalemba mʼbuku la kawundula wa anthu a mitundu ina: “Uyu anabadwira mʼZiyoni.” (Sela)
Jahwe wird verzeichnen die Völker: / "Diese sind dort geboren!" (Sela)
7 Oyimba ndi ovina omwe adzati, “Akasupe anga onse ali mwa iwe.”
Und singend und tanzend ruft man laut: / "All meine Quellen sind in dir!"

< Masalimo 87 >