< Masalimo 83 >
1 Nyimbo. Salimo la Asafu. Inu Mulungu musakhale chete; musangoti phee, Mulungu musangoti duu.
Uma canção. Um salmo de Asaph. God, não fique calado. Não fique calado, e não fique quieto, Deus.
2 Onani adani anu akuchita chiwawa, amene amadana nanu autsa mitu yawo.
Pois, eis que seus inimigos estão agitados. Aqueles que odeiam você levantaram a cabeça.
3 Mochenjera iwo akukambirana za chiwembu kutsutsana ndi anthu anu; Iwo akukonzekera kutsutsana ndi omwe mumawakonda.
Eles conspiram com astúcia contra seu povo. Eles conspiram contra os seus queridos.
4 Iwo akunena kuti, “Bwerani” akutero, “Tiyeni tiwononge mtundu wonsewu kuti dzina la Israeli lisakumbukikenso.”
“Venha”, dizem eles, “vamos destruí-los como nação”, que o nome de Israel não seja mais lembrado”.
5 Ndi mtima umodzi akukonzekera chiwembu; Iwo achita mgwirizano kutsutsana nanu:
Pois eles têm conspirado juntos com uma só mente. Eles formam uma aliança contra você.
6 Matenti a Edomu ndi Aismaeli, Mowabu ndi Ahagiri,
As tendas da Edom e dos ismaelitas; Moab, e os Hagrites;
7 Agebala, Aamoni ndi Aamaleki, Afilisti, pamodzi ndi anthu a ku Turo.
Gebal, Ammon, e Amalek; Philistia com os habitantes de Tyre;
8 Ngakhalenso Aasiriya aphatikizana nawo kupereka mphamvu kwa ana a Loti. (Sela)
Assyria também está unido a eles. Eles têm ajudado as crianças de Lot. (Selah)
9 Muwachitire zomwe munachitira Amidiyani, monga munachitira Sisera ndi Yabini ku mtsinje wa Kisoni.
Do a eles como você fez com a Midian, quanto a Sisera, quanto a Jabin, no rio Kishon;
10 Amene anawonongedwa ku Endori ndi kukhala ngati zinyalala.
que pereceu em Endor, que se tornou como esterco para a terra.
11 Anthu awo otchuka muwachite zomwe munachita Orebu ndi Zeebu ana a mafumu muwachite zomwe munachita Zeba ndi Zalimuna,
Make seus nobres como Oreb e Zeeb, sim, todos os seus príncipes como Zebah e Zalmunna,
12 amene anati, “Tiyeni tilande dziko la msipu la Mulungu.”
que disse: “Vamos tomar posse das terras de pasto de Deus”.
13 Muwasandutse fumbi lowuluka, Inu Mulungu wanga, ngati mankhusu owuluka ndi mphepo.
Meu Deus, faça-os como se fossem ervas daninhas, como o palhiço antes do vento.
14 Monga moto umatentha nkhalango, kapena malawi a moto kuyatsa phiri,
Como o fogo que queima a floresta, como a chama que incendeia as montanhas,
15 kotero muwathamangitse ndi mphepo yamkuntho, ndi kuwachititsa mantha ndi namondwe.
so persegui-los com sua tempestade, e aterrorizá-los com sua tempestade.
16 Muphimbe nkhope zawo ndi manyazi kuti adzafunefune dzina lanu Yehova.
Fill seus rostos com confusão, que eles possam procurar seu nome, Yahweh.
17 Achite manyazi ndi mantha nthawi zonse; awonongeke mwa manyazi.
Let eles ficarão desapontados e consternados para sempre. Sim, que sejam confundidos e pereçam;
18 Adziwe kuti Inu amene dzina lanu ndi Yehova, ndinu nokha Wammwambamwamba pa dziko lonse lapansi.
para que eles saibam que você sozinho, cujo nome é Yahweh, são as Altíssimas em toda a Terra.