< Masalimo 83 >

1 Nyimbo. Salimo la Asafu. Inu Mulungu musakhale chete; musangoti phee, Mulungu musangoti duu.
Ein Lied. Ein Psalm Asafs.
2 Onani adani anu akuchita chiwawa, amene amadana nanu autsa mitu yawo.
Elohim, schaue nicht ruhig zu, / Schweige doch nicht und raste nicht, Gott!
3 Mochenjera iwo akukambirana za chiwembu kutsutsana ndi anthu anu; Iwo akukonzekera kutsutsana ndi omwe mumawakonda.
Denn sieh, deine Feinde toben, / Und deine Hasser erheben das Haupt.
4 Iwo akunena kuti, “Bwerani” akutero, “Tiyeni tiwononge mtundu wonsewu kuti dzina la Israeli lisakumbukikenso.”
Wider dein Volk ersinnen sie listigen Anschlag, / Beraten sich gegen die, die du bewahrst.
5 Ndi mtima umodzi akukonzekera chiwembu; Iwo achita mgwirizano kutsutsana nanu:
"Auf", sagen sie, "laßt uns als Volk sie vernichten, / Daß Israels Name für immer verschwinde!"
6 Matenti a Edomu ndi Aismaeli, Mowabu ndi Ahagiri,
Denn einmütig haben sie sich beraten, / Wider dich einen Bund geschlossen:
7 Agebala, Aamoni ndi Aamaleki, Afilisti, pamodzi ndi anthu a ku Turo.
Edoms Zelte, die Ismaeliter, / Moab und die Hagriter,
8 Ngakhalenso Aasiriya aphatikizana nawo kupereka mphamvu kwa ana a Loti. (Sela)
Gebâl und Ammon und Amalek, / Die Philister samt denen zu Tyrus.
9 Muwachitire zomwe munachitira Amidiyani, monga munachitira Sisera ndi Yabini ku mtsinje wa Kisoni.
Auch Assur hat sich zu ihnen gesellt, / Es leiht seinen Arm den Söhnen Lots. (Sela)
10 Amene anawonongedwa ku Endori ndi kukhala ngati zinyalala.
Tu ihnen so wie Midian, / Wie Sisera, wie Jabin am Bache Kison!
11 Anthu awo otchuka muwachite zomwe munachita Orebu ndi Zeebu ana a mafumu muwachite zomwe munachita Zeba ndi Zalimuna,
Sie wurden bei Endor vertilgt, / Wurden Dünger auf Ackerland.
12 amene anati, “Tiyeni tilande dziko la msipu la Mulungu.”
Ihre Edlen mache wie Oreb und Seeb, / wie Sébach und Zalmúnna all ihre Fürsten,
13 Muwasandutse fumbi lowuluka, Inu Mulungu wanga, ngati mankhusu owuluka ndi mphepo.
Weil sie gesprochen: "Wir wollen für uns / Einnehmen die Auen Gottes."
14 Monga moto umatentha nkhalango, kapena malawi a moto kuyatsa phiri,
Mein Gott, mache sie wie Laub, / Wie Stoppeln, die der Wind wegtreibt,
15 kotero muwathamangitse ndi mphepo yamkuntho, ndi kuwachititsa mantha ndi namondwe.
Wie Feuer, das einen Wald verbrennt, / Wie die Flamme, die Berge entzündet!
16 Muphimbe nkhope zawo ndi manyazi kuti adzafunefune dzina lanu Yehova.
Verfolge sie so mit deinem Sturm, / Und mit deiner Windsbraut schrecke sie!
17 Achite manyazi ndi mantha nthawi zonse; awonongeke mwa manyazi.
Mach ihr Antlitz voll Schmach, / Damit sie nach deinem Namen fragen, o Jahwe!
18 Adziwe kuti Inu amene dzina lanu ndi Yehova, ndinu nokha Wammwambamwamba pa dziko lonse lapansi.
Sie sollen zuschanden werden, erschrecken für immer, / Erröten vor Scham und vergehen! Dann laß sie erkennen, daß du, des Name Jahwe heißt, / Allein der Höchste bist auf der ganzen Erde.

< Masalimo 83 >