< Masalimo 82 >
1 Salimo la Asafu. Mulungu akutsogolera msonkhano waukulu; Iye akuweruza pakati pa “milungu.”
Mijohañe am-pivorim-panalolahy t’i Andrianañahare; mizaka añivom-pizaka eo.
2 “Mudzateteza osalungama mpaka liti, ndi kukondera anthu oyipa?
Pak’ombia ty mbe izakà’ areo ami’ty tsy hiti’e, hañonjonañe o tsivokatseo? Selà
3 Tetezani anthu ofowoka ndi amasiye; mukhazikitse ufulu wa anthu osauka ndi ozunzika.
Meo tò o rarakeo naho o bode-raeo; tohaño ty zo’ o poie’eo naho o misotrio.
4 Landitsani anthu ofowoka ndi osowa; apulumutseni mʼdzanja la anthu oyipa.
Hahao o mahàtrao naho o malorèo; avotsoro am-pità’ o lo-tserekeo.
5 “Iwo sadziwa kanthu, sazindikira kalikonse. Amayendayenda mu mdima; maziko onse a dziko lapansi agwedezeka.
Tsy mahilala iereo, naho tsy mahafohiñe, mirererere añ’ieñe ao avao; fa naveve iaby o faha’ ty tane toio.
6 “Ndinati, ‘Inu ndinu Mulungu, nonsenu ndinu ana a Wammwambamwamba.’
Nanao ty hoe iraho: Mpizaka nahareo songa anak’ i Andindimoneñey.
7 Koma mudzafa ngati anthu wamba; mudzagwa ngati wolamula wina aliyense.”
Fe hikoromake hoe ondaty avao, hikorovoke manahake ty raike amo roandriañeo.
8 Dzukani Inu Mulungu, weruzani dziko lapansi, pakuti mayiko onse ndi cholowa chanu.
Miongaha, ry Andrianañahare, zakao ty tane toy, fa kila ho lovae’o o fifeheañeo.