< Masalimo 82 >
1 Salimo la Asafu. Mulungu akutsogolera msonkhano waukulu; Iye akuweruza pakati pa “milungu.”
Asafa dziesma. Dievs stāv Savā draudzē, Viņš tura tiesu starp tiem dieviem.
2 “Mudzateteza osalungama mpaka liti, ndi kukondera anthu oyipa?
Cik ilgi jūs gribat netaisni tiesāt un uzlūkot bezdievīgo ļaužu vaigu? (Sela)
3 Tetezani anthu ofowoka ndi amasiye; mukhazikitse ufulu wa anthu osauka ndi ozunzika.
Izdodiet tiesu nabagam un bāriņam, taisnojiet bēdīgo un nabagu.
4 Landitsani anthu ofowoka ndi osowa; apulumutseni mʼdzanja la anthu oyipa.
Izglābiet nabagu un bēdīgo, izraujiet viņu no bezdievīgo rokas.
5 “Iwo sadziwa kanthu, sazindikira kalikonse. Amayendayenda mu mdima; maziko onse a dziko lapansi agwedezeka.
Bet tie to neatzīst un nesaprot, tie staigā tumsībā; par to zemes pamatiem jāšaubās.
6 “Ndinati, ‘Inu ndinu Mulungu, nonsenu ndinu ana a Wammwambamwamba.’
Gan Es esmu sacījis: jūs esat dievi, un visi tā Visuaugstākā bērni.
7 Koma mudzafa ngati anthu wamba; mudzagwa ngati wolamula wina aliyense.”
Bet jūs nomirsiet kā cilvēki un iesiet bojā tāpat kā citi lieli kungi.
8 Dzukani Inu Mulungu, weruzani dziko lapansi, pakuti mayiko onse ndi cholowa chanu.
Celies, ak Dievs, tiesā pasauli, jo Tev būs par mantību visas tautas.