< Masalimo 82 >

1 Salimo la Asafu. Mulungu akutsogolera msonkhano waukulu; Iye akuweruza pakati pa “milungu.”
Žalm Azafův. Bůh stojí v shromáždění Božím, u prostřed bohů soud čině, a dí:
2 “Mudzateteza osalungama mpaka liti, ndi kukondera anthu oyipa?
Dokudž souditi budete nespravedlivě, a osoby nešlechetných přijímati? (Sélah)
3 Tetezani anthu ofowoka ndi amasiye; mukhazikitse ufulu wa anthu osauka ndi ozunzika.
Zastávejte bídného a sirotka, utištěného a chudého spravedliva vyhlašujte.
4 Landitsani anthu ofowoka ndi osowa; apulumutseni mʼdzanja la anthu oyipa.
Vytrhněte bídného a nuzného, z ruky nešlechetných vytrhněte ho.
5 “Iwo sadziwa kanthu, sazindikira kalikonse. Amayendayenda mu mdima; maziko onse a dziko lapansi agwedezeka.
Ale nevědí nic, nerozumějí nic; ve tmách ustavně chodí, až se proto všickni základové země pohybují.
6 “Ndinati, ‘Inu ndinu Mulungu, nonsenu ndinu ana a Wammwambamwamba.’
Řeklť jsem já byl: Bohové jste, a synové Nejvyššího vy všickni;
7 Koma mudzafa ngati anthu wamba; mudzagwa ngati wolamula wina aliyense.”
A však jako i jiní lidé zemřete, a jako jeden z knížat padnete.
8 Dzukani Inu Mulungu, weruzani dziko lapansi, pakuti mayiko onse ndi cholowa chanu.
Povstaniž, ó Bože, suď zemi; nebo ty dědičně vládneš všemi národy.

< Masalimo 82 >