< Masalimo 82 >

1 Salimo la Asafu. Mulungu akutsogolera msonkhano waukulu; Iye akuweruza pakati pa “milungu.”
Psalam. Asafov. Bog ustaje u skupštini “bogova”, usred “bogova” sud održava.
2 “Mudzateteza osalungama mpaka liti, ndi kukondera anthu oyipa?
“Dokle ćete sudit' krivo, ić' na ruku bezbožnima?
3 Tetezani anthu ofowoka ndi amasiye; mukhazikitse ufulu wa anthu osauka ndi ozunzika.
Štitite slaba i sirotu, vratite pravicu jadniku i siromahu!
4 Landitsani anthu ofowoka ndi osowa; apulumutseni mʼdzanja la anthu oyipa.
Izbavite potlačenog i ubogog: istrgnite ga iz ruku bezbožnih!”
5 “Iwo sadziwa kanthu, sazindikira kalikonse. Amayendayenda mu mdima; maziko onse a dziko lapansi agwedezeka.
Ne shvaćaju nit' razumiju, po mraku hodaju: poljuljani su svi temelji zemlje.
6 “Ndinati, ‘Inu ndinu Mulungu, nonsenu ndinu ana a Wammwambamwamba.’
Rekoh doduše: “Vi ste bogovi i svi ste sinovi Višnjega!
7 Koma mudzafa ngati anthu wamba; mudzagwa ngati wolamula wina aliyense.”
Ali ćete k'o svi ljudi umrijeti, past ćete kao svatko od velikih!”
8 Dzukani Inu Mulungu, weruzani dziko lapansi, pakuti mayiko onse ndi cholowa chanu.
Ustani, Bože, i sudi zemlju, jer si s pravom gospodar svih naroda.

< Masalimo 82 >