< Masalimo 81 >
1 Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Potsata mayimbidwe a gititi. Salimo la Asafu. Imbani mwachimwemwe kwa Mulungu mphamvu yathu; Fuwulani mokweza kwa Mulungu wa Yakobo!
KOMAIL pereperen kauli on Kot, me kel patail; nijinij on Kot en Iakop!
2 Yambani nyimbo, imbani tambolini imbani pangwe wolira bwino ndi zeze.
Tapia kida kaul en kapin, o wiada tampurin, o laute kajelel ianaki arp!
3 Imbani lipenga la nyanga ya nkhosa yayimuna pa mwezi watsopano, ndi pamene mwezi waoneka wonse, pa tsiku la phwando;
Ni jaunipon kap komail peuk koronete, ni maram, ni ran en im tantuka!
4 ili ndi lamulo kwa Israeli, langizo la Mulungu wa Yakobo.
Pwe iduen tiak en Ijrael kujoned en Kot en Iakop eu.
5 Iye anapereka lamulolo kwa zidzukulu za Yosefe pamene anatuluka kulimbana ndi Igupto, kumene tinamva chiyankhulo chimene sitinachidziwe.
A kotin wiadar kujoned wet on Iojep, ni a lipa jan Akipten. I roner majan pot, me i jaikenta aja:
6 Iye akunena kuti, “Ine ndinachotsa zolemetsa pa mapewa awo; Manja awo anamasulidwa mʼdengu.
I kijaner katoutou kan pon apar a, o pa a jaladokalar jan kopu kan.
7 Pa mavuto anu munayitana ndipo ndinakulanditsani, ndinakuyankhani kuchokera mʼmitambo ya mabingu; ndinakuyesani pa madzi a ku Meriba. (Sela)
Ni om likwirki don ia om apwal, I ap jauaja uk; I kajale dok uk alar, ni anjau me koe lel on nanjapwe, o on jojon uk ni pil en akamai.
8 “Imvani anthu anga, ndipo ndidzakuchenjezani ngati mungathe kumvetsera, Inu Israeli!
Komail nai aramaj akan ron ia, I pan padaki on komail! O Ijrael, ma koe pan peiki on ia!
9 Musadzakhale ndi mulungu wachilendo pakati panu; musadzagwadire mulungu wina.
Jota amen Kot en mi re om, o koe der kaudoki on kot en men wai amen.
10 Ine ndine Yehova Mulungu wanu, amene ndinakutulutsani mʼdziko la Igupto. Yasamani kukamwa kwanu ndipo ndidzakudyetsani.
Nai Ieowa om Kot, me kalua uk jan nan Akipten. Ki pajan au om, i pan kadirela.
11 “Koma anthu anga sanandimvere; Israeli sanandigonjere.
A nai aramaj akan joata kin peiki on nil ai, o Ijrael jota duki on ia.
12 Kotero ndinawasiya ndi mitima yawo yosamverayo kuti atsate zimene ankafuna.
I ari mued on irail ere injen arail ni ar aklapalap, pwe ren kekeid wei ni pein arail lamelam.
13 “Anthu anga akanangondimvera, Israeli akanatsatira njira zanga,
O ma nai aramaj akan pan peiki on ia, o Ijrael pan weweid nan al ai kan,
14 nʼkanafulumira motani kuti ndigonjetse adani awo ndi kutembenuza mkono wanga kulimbana ndi amaliwongo!
I ap pan kaloedi ar imwintiti kan madan, o pa i pan u on me pali on irail akan,
15 Iwo amene amadana ndi Yehova akanakhwinyata pamaso pake, ndipo chilango chawo chinakakhala mpaka kalekale.
O irail me kailonki Ieowa, jota pan kak on irail; o anjaun arail pakadeik pan duedeuta kokolata;
16 Koma inu mukanadyetsedwa tirigu wabwino kwambiri; ndikanakukhutitsani ndi uchi wochokera pa thanthwe.”
O I pan kamana kin irail korn kajelelia, o I pan katunole kin I onik jan nan paip o.