< Masalimo 8 >
1 Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Pa gititi. Salimo la Davide. Inu Yehova Ambuye athu, dzina lanu ndi la lamphamvudi pa dziko lonse lapansi! Inu mwakhazikitsa ulemerero wanu mʼmayiko onse akumwamba.
Kumqondisi wokuhlabela. Ngendlela yegithithi. Ihubo likaDavida. Oh Thixo, Thixo wethu, ibizo lakho libabazeka kangaka emhlabeni wonke! Uyibekile inkazimulo yakho ngaphezulu emazulwini.
2 Kuchokera mʼkamwa mwa ana ndi makanda, Inu mwakhazikitsa mphamvu chifukwa cha adani anu, kukhazikitsa bata adani ndi anthu obwezera zoyipa.
Ukumisile ukudunyiswa yizindebe zabantwana lensane ngenxa yezitha zakho, ukuze uthulise isitha lomphindiseli.
3 Pamene ndilingalira za mayiko anu akumwamba, ntchito ya zala zanu, mwezi ndi nyenyezi, zimene mwaziyika pa malo ake,
Nxa nginakana ngamazulu akho, umsebenzi weminwe yakho, inyanga lezinkanyezi ozibeke endaweni yazo,
4 munthu ndani kuti Inu mumamukumbukira, ndi mwana wa munthu kuti inu mumacheza naye?
uyini umuntu osungaze uzihluphe ngaye na, indodana yomuntu ukuba uyinanze?
5 Inu munamupanga kukhala wocheperapo kusiyana ndi zolengedwa zakumwamba ndipo mwamuveka ulemerero ndi ulemu.
Wamenza waba mncinyazana kulezingilosi, wamethesa umqhele wodumo lobukhosi.
6 Inu munamuyika wolamulira ntchito ya manja anu; munayika zinthu zonse pansi pa mapazi ake;
Wamenza umbusi phezu kwemisebenzi yezandla zakho; wabeka zonke izinto ngaphansi kwezinyawo zakhe:
7 nkhosa, mbuzi ndi ngʼombe pamodzi ndi nyama zakuthengo,
yonke imihlambi yezimvu leyenkomo lezinyamazana zeganga,
8 mbalame zamlengalenga ndi nsomba zamʼnyanja zonse zimene zimayenda pansi pa nyanja.
izinyoni zasemkhathini lenhlanzi zolwandle, konke okuntsheza emanzini olwandle.
9 Inu Yehova, Ambuye athu, dzina lanu ndi lamphamvudi pa dziko lonse lapansi!
Oh Thixo, Thixo wethu, ibizo lakho libabazeka kangaka emhlabeni wonke!