< Masalimo 8 >

1 Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Pa gititi. Salimo la Davide. Inu Yehova Ambuye athu, dzina lanu ndi la lamphamvudi pa dziko lonse lapansi! Inu mwakhazikitsa ulemerero wanu mʼmayiko onse akumwamba.
[Psalm lal David] O LEUM GOD, kom Leum lasr; Fulat lom akilenyuk fin faclu nufon! Kaksakinyom sowak sun kusrao,
2 Kuchokera mʼkamwa mwa ana ndi makanda, Inu mwakhazikitsa mphamvu chifukwa cha adani anu, kukhazikitsa bata adani ndi anthu obwezera zoyipa.
Onkakinyuk sin tulik srisrik ac tulik fusr. Kom oakiya sie pot ku in kosrala mwet lokoalok lom Tuh kom in tulokinya kutena mwet su lain kom.
3 Pamene ndilingalira za mayiko anu akumwamba, ntchito ya zala zanu, mwezi ndi nyenyezi, zimene mwaziyika pa malo ake,
Ke nga ngetak ac liye kusrao su kom orala, Malem ac itu, su kom oakiya in acn selos,
4 munthu ndani kuti Inu mumamukumbukira, ndi mwana wa munthu kuti inu mumacheza naye?
Mea mwet, tuh kom in nunku kacl; Ac mea se mwet uh, tuh kom in saokkin?
5 Inu munamupanga kukhala wocheperapo kusiyana ndi zolengedwa zakumwamba ndipo mwamuveka ulemerero ndi ulemu.
Nwe ouinge, kom oru tuh elos in pusisel kutu srisrik liki kom, Ac sonelosi ke wolana ac sunak.
6 Inu munamuyika wolamulira ntchito ya manja anu; munayika zinthu zonse pansi pa mapazi ake;
Kom oru tuh elos in leum fin orekma nukewa lun poum; Ac filiya ma nukewa ye nialos:
7 nkhosa, mbuzi ndi ngʼombe pamodzi ndi nyama zakuthengo,
Sheep ac cow, oayapa kosro nukewa inimae,
8 mbalame zamlengalenga ndi nsomba zamʼnyanja zonse zimene zimayenda pansi pa nyanja.
Won yen engyeng uh, ac ik in meoa, Ac ma moul nukewa inkof uh.
9 Inu Yehova, Ambuye athu, dzina lanu ndi lamphamvudi pa dziko lonse lapansi!
O LEUM GOD, kom Leum lasr, Fulat lom akilenyuk fin faclu nufon!

< Masalimo 8 >