< Masalimo 8 >

1 Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Pa gititi. Salimo la Davide. Inu Yehova Ambuye athu, dzina lanu ndi la lamphamvudi pa dziko lonse lapansi! Inu mwakhazikitsa ulemerero wanu mʼmayiko onse akumwamba.
Kuom Jatend Wer. Kaluwore Gi Gitith. Zaburi Mar Daudi. Yaye Jehova Nyasaye, ma Ruodhwa, mano kaka nyingi nigi duongʼ e piny duto! Iseketo duongʼni maler milamo, moyombo polo.
2 Kuchokera mʼkamwa mwa ana ndi makanda, Inu mwakhazikitsa mphamvu chifukwa cha adani anu, kukhazikitsa bata adani ndi anthu obwezera zoyipa.
Ne isechano mondo nyithindo kod nyithindo mayom omiyi pak, nikech wasiki, mondo jawasigu kod jachul kuor olingʼ kawuoro timni.
3 Pamene ndilingalira za mayiko anu akumwamba, ntchito ya zala zanu, mwezi ndi nyenyezi, zimene mwaziyika pa malo ake,
Kaparo polo mari ma gin tich lweti, kaparo dwe gi sulwe miseketo kargi,
4 munthu ndani kuti Inu mumamukumbukira, ndi mwana wa munthu kuti inu mumacheza naye?
to dhano adhana to en angʼo momiyo ipare, wuod dhano to en angʼo momiyo iketo pachi kuome?
5 Inu munamupanga kukhala wocheperapo kusiyana ndi zolengedwa zakumwamba ndipo mwamuveka ulemerero ndi ulemu.
Ne ichweye mapiny ne malaike kendo isesidhone osimbo mar duongʼ kod luor.
6 Inu munamuyika wolamulira ntchito ya manja anu; munayika zinthu zonse pansi pa mapazi ake;
Isekete jatelo ewi tich lweti duto; iseketo gik moko duto e bwo tiende:
7 nkhosa, mbuzi ndi ngʼombe pamodzi ndi nyama zakuthengo,
Jamni gi kweth duto kod le mager mag bungu,
8 mbalame zamlengalenga ndi nsomba zamʼnyanja zonse zimene zimayenda pansi pa nyanja.
Winy duto mafuyo e kor polo, kod rech manie nam, gi le duto mamol kaluwo yore manie nembe iketo e bwo lochne.
9 Inu Yehova, Ambuye athu, dzina lanu ndi lamphamvudi pa dziko lonse lapansi!
Yaye Jehova Nyasaye, ma Ruodhwa, mano kaka nyingi nigi duongʼ e piny duto!

< Masalimo 8 >