< Masalimo 78 >

1 Ndakatulo ya Asafu. Inu anthu anga imvani chiphunzitso changa; mvetserani mawu a pakamwa panga.
Kathutkung: Asaph Oe, ka taminaw ka kâlawk hah tarawi awh nateh, ka dei e lawk hah na hnâpakeng awh.
2 Ndidzatsekula pakamwa panga mʼmafanizo, ndidzayankhula zinthu zobisika, zinthu zakalekale
Bangnuenae lahoi ka pahni ka ang vaiteh, ayan e lawkkaru hah ka pâpho han.
3 zimene tinazimva ndi kuzidziwa, zimene makolo athu anatiwuza.
Hothateh, ka thai teh, ka panue tangcoung e mintoenaw ni a dei awh e doeh.
4 Sitidzabisira ana awo, tidzafotokozera mʼbado wotsatira ntchito zotamandika za Yehova, mphamvu zake, ndi zozizwitsa zimene Iye wachita.
A canaw koehoi kâhrawk mahoeh. Ka tho hane senaw koevah, BAWIPA pholennae, a thaonae, hoi hno kângairu a sak e hah ka dei han.
5 Iye anapereka mawu wodzichitira umboni kwa Yakobo ndi kukhazikitsa lamulo mu Israeli, zimene analamulira makolo athu kuphunzitsa ana awo,
Bangtelah tetpawiteh, mintoenaw hah kâ a poe teh, a ca catounnaw koe a panue sak awh nahanlah, Jakop koe lawkpanuesaknae hah acak sak teh, Isarel koe kâlawk hah a poe.
6 kotero kuti mʼbado wotsatira uthe kuzidziwa, ngakhale ana amene sanabadwe, ndi kuti iwo akafotokozere ana awonso.
Kaawm han rae se hoi ka tâcawt han rae camonaw ni, a catounnaw koe a dei awh vaiteh, a panue awh nahanlah,
7 Choncho iwo adzakhulupirira Mulungu ndipo sadzayiwala ntchito zake koma adzasunga malamulo ake.
Cathut dawk a ngaihawi awh nahan hoi Cathut hnosak hah pahnim laipalah kâpoelawknaw a pahnim awh hoeh nahanlah,
8 Iwo asadzakhale monga makolo awo, mʼbado wosamvera ndi wowukira, umene mitima yake inali yosamvera Mulungu, umene mizimu yake inali yosakhulupirika kwa Iye.
Mintoenaw patetlah lungpatanae, taranthawnae, kalan e hno dawk a lung kaawm hoeh e, Cathut hanelah yuemkamcu hoeh e muitha lah ao awh hoeh nahane doeh.
9 Anthu a ku Efereimu, ngakhale ananyamula mauta, anathawabe pa nthawi ya nkhondo;
Ephraim catoun teh tarantuknae a khohna teh licung a patuep ei, tarantuk hnin navah a yawng.
10 iwo sanasunge pangano la Mulungu ndipo anakana kukhala mʼmoyo wotsatira lamulo lake.
Cathut lawkkam tarawi awh hoeh. Kâlawk tarawi e ngai awh hoeh.
11 Anayiwala zimene Iye anachita, zozizwitsa zimene anawaonetsa.
A sak e hoi hno kângairu a sak e hah, a pahnim awh.
12 Iyeyo anachita zodabwitsa makolo athu akuona, mʼdziko la Igupto, mʼchigawo cha Zowani.
A na mintoenaw e mithmu vah, kângairu hno hah Izip ram Zoan tanghling dawk a sak.
13 Anagawa nyanja pakati ndi kudutsitsapo iwowo, Iye anachititsa madzi kuyima chilili ngati khoma.
Talîpui hah a kapek teh ahnimanaw hah a cei sak. Tui hah hnopai patetlah a pâhlawp.
14 Anawatsogolera ndi mtambo masana ndi kuwala kwa moto usiku wonse.
Kanîthun hai tâmai hoi a hrawi teh, tangmin karoitawi hmaiang hoi a hrawi.
15 Iye anangʼamba miyala mʼchipululu ndi kuwapatsa madzi ochuluka ngati a mʼnyanja zambiri;
Kahrawngum vah, lungsong a bawng teh, talîpui tui patetlah moikapap e tui a pânei.
16 Anatulutsa mitsinje kuchokera mʼmingʼalu ya miyala ndi kuyenda madzi ngati mitsinje.
Lungsong thung hoi tui a tâco sak teh, palangpui patetlah a lawng sak.
17 Komabe iwowo anapitiriza kumuchimwira Iye, kuwukira Wammwambamwamba mʼchipululu.
Hatei, ama taranlahoi hoehoe a yon awh teh, kahrawngum vah Lathueng Poung taranlahoi taran a thaw awh.
18 Ananyoza Mulungu mwadala pomuwumiriza kuti awapatse chakudya chimene anachilakalaka.
Ca han a ngai poung awh e hah a hei awh teh, a lungthin hoi Cathut hah a tanouk awh.
19 Iwo anayankhula motsutsana naye ponena kuti, “Kodi Mulungu angatipatse chakudya mʼchipululu?
Bokheiyah, Cathut taranlahoi a dei awh e teh, kahrawngum vah Cathut ni rawca na poe thai awh han na maw, telah ati awh.
20 Iye atamenya thanthwe madzi anatuluka, ndipo mitsinje inadzaza ndi madzi. Koma iye angatipatsenso ife chakudya? Kodi angapereke nyama kwa anthu akewa?”
Khenhaw! tui a tâco teh, tuiko muen ka kawi lah a lawng nahan lah lungsongpui hah a hem. Rawca hai a poe thai namaw. A taminaw hah moi a poe thai han na ou, telah ati awh.
21 Yehova atawamva anakwiya kwambiri; moto wake unayaka kutsutsana ndi Yakobo, ndipo mkwiyo wake unauka kutsutsana ndi Israeli,
Hatdawkvah, BAWIPA ni hote lawk hah a thai teh a lungkhuek. Hat toteh, Jakop taranlahoi hmaito a tâco teh, Isarel taranlahoi a lungkhuek.
22 pakuti iwo sanakhulupirire Mulungu kapena kudalira chipulumutso chake.
Bangkongtetpawiteh, Cathut hah yuem awh hoeh. A rungngangnae hai kâuep awh hoeh.
23 Komabe Iye anapereka lamulo kwa mitambo mmwamba ndi kutsekula makomo a mayiko akumwamba;
Hottelah nahlangva, lathueng lae tâmai hah kâ a poe teh, kalvan longkha hah a paawng pouh.
24 anagwetsa mana kuti anthu adye, anawapatsa tirigu wakumwamba.
Ca hane mana hah ahnimouh lathueng a rak sak teh, kalvanlae rawca hah a poe.
25 Anthu anadya buledi wa angelo, Iye anawatumizira chakudya chonse chimene akanatha kudya.
Taminaw ni thaonae rawca hah a ca awh teh, kaboumlah ca hane a patawn.
26 Anamasula mphepo ya kummwera kuchokera kumwamba, ndi kutsogolera mphepo ya kummwera mwa mphamvu zake.
Kanîtholae kahlî hah kalvan a tho sak teh, a hnotithainae lahoi a cum lae kahlî hah a tho sak.
27 Iye anawagwetsera nyama ngati fumbi, mbalame zowuluka ngati mchenga wa mʼmbali mwa nyanja.
Vaiphu patetlah moi hah a rak sak teh, rathei ka tawn e tavanaw hah tuirai e sadi yit touh apap awh.
28 Anazibweretsa kwa iwo mʼkati mwa misasa yawo, kuzungulira matenti awo onse.
A roenae tengpam petkâkalup lah a bo pouh.
29 Iwo anadya mpaka anatsala nazo zochuluka pakuti Iye anawapatsa zimene anazilakalaka.
Hateh, a ca awh teh king a boum awh. Bangkongtetpawiteh, a ngai awh e patetlah a poe.
30 Koma iwowo anasiya kudya chakudya anachilakalakacho, chakudya chili mʼkamwa mwawobe,
Hatei, a ngai awh e rawca a hmawt awh hoehnahlan, a ca awh lahun navah,
31 mkwiyo wa Mulungu unawayakira; Iye anapha amphamvu onse pakati pawo, kugwetsa anyamata abwino kwambiri mu Israeli.
Cathut lungkhueknae teh ahnimouh koe a pha. A tami tha kaawmnaw hah a thei teh, Isarel thoundounnaw hah koung a rawp sak.
32 Ngakhale zinali chomwechi, iwo anapitirira kuchimwa; ngakhale anaona zozizwitsa zakezo iwowo sanakhulupirirebe.
Hottelah nahlangva, hoehoe a yon awh teh, hno kalen a sak awh e hai bout yuem awh hoeh.
33 Kotero Mulungu anachepetsa masiku awo kuti azimirire ngati mpweya. Iye anachepetsa zaka zawo kuti zithere mʼmasautso.
Hatdawkvah, hringyung hnin hah ayawmyin lah a coung sak awh teh, lungpuennae hoi a kum teh a baw sak awh.
34 Mulungu atawapha, iwo amamufunafuna Iyeyo; iwo ankatembenukiranso kwa Iye mwachangu.
Ahnimanaw hah a thei awh teh, a ma tawng hanelah a ban awh teh, atangcalah Cathut heh a tawng awh.
35 Ankakumbukira kuti Mulungu ndiye Thanthwe lawo, kuti Mulungu Wammwambamwamba ndiye Mpulumutsi wawo.
Cathut teh amamae lungsongpui doeh tie a panue awh teh, Lathueng Poung Cathut teh na karatangkung doeh tie a panue awh.
36 Komabe ankamuthyasika ndi pakamwa pawo, kumunamiza ndi malilime awo;
Hateiteh, ama teh a pahni hoi a pholen teh, lai hoi laithoe a dei awh.
37 Mitima yawo sinali yokhazikika pa Iye, iwo sanakhulupirike ku pangano lake.
Bangkongtetpawiteh, ahnimae lungthin teh a hmalah lan hoeh, a lawkkam dawk yuemkamcu awh hoeh.
38 Komabe Iye anali wachifundo; anakhululukira mphulupulu zawo ndipo sanawawononge. Nthawi ndi nthawi Iye anabweza mkwiyo wake ndipo sanawutse ukali wake wonse.
Hatei, ama teh lungmanae hoi akawi teh, a payonnae heh a ngaithoum teh, koung raphoe hoeh. Bokheiyah, avai moikapap lungkhueknae a roum sak teh, a lungphuennae kaman sak ngai hoeh.
39 Iye anakumbukira kuti iwo anali anthu chabe, mphepo yopita imene sibwereranso.
Bangkongtetpawiteh, takthai lah ao awh teh, bout ban hoeh hanelah, kâha a poe e tie hah pahnim awh hoeh.
40 Nthawi zambiri iwo ankamuwukira Iye mʼchipululu ndi kumumvetsa chisoni mʼdziko lopanda kanthu!
Thingyeiyawn vah vai nâyittouh maw a lungkhuek sak awh teh, ramke vah avai nâyittouh maw a lungmathoe sak awh toe.
41 Kawirikawiri iwo ankamuyesa Mulungu; ankamuputa Woyera wa Israeli.
Bokheiyah, atuhoitu Cathut a tanouk awh teh, Isarelnaw e Tami Kathoung hah a taran awh.
42 Sanakumbukire mphamvu zake, tsiku limene Iye anawawombola kwa ozunza,
A thaonae pâkuem ngai awh hoeh, a tarannaw koehoi a rungngang ei nakunghai, pâkuem ngai awh hoeh.
43 tsiku limene Iyeyo anaonetsa poyera zizindikiro zozizwitsa zake mu Igupto, zozizwitsa zake mʼchigawo cha Zowani.
Izip ram hoi Zoan yawn dawk kângairu hno a sak e hoi.
44 Iye anasandutsa mitsinje yawo kukhala magazi; Iwo sanathe kumwa madzi ochokera mʼmitsinje yawo.
Ahnimae palang hah thipaling lah a coung sak teh, ahnimae tuikhunaw hai nei thai hoeh hanlah thipaling lah koung a coung sak.
45 Iye anawatumizira magulu a ntchentche zimene zinawawononga, ndiponso achule amene anawasakaza.
Ahnimouh ka kei e bitseinaw hoi, ahnimouh karaphoekung ekkanaw hah a tha pouh.
46 Iye anapereka mbewu zawo kwa ziwala, zokolola zawo kwa dzombe.
Ahnimae a pawhiknaw hah, ahri ni ca hanelah a poe teh, a tawksak awh e a pawhik hah samtongnaw a poe pouh.
47 Iye anawononga mphesa zawo ndi matalala ndiponso mitengo yawo yankhuyu ndi chisanu.
Ahnimae misurnaw teh roun ni koung a raphoe pouh teh, thailahei kungnaw hai tadamtui ni koung a thei pouh.
48 Iye anapereka ngʼombe zawo ku matalala, zoweta zawo ku zingʼaningʼani.
Ahnimae saringnaw hai roun ni dêi hanelah a poe pouh teh, saringnaw hah kei ni a ka pouh.
49 Anakhuthula moto wa ukali wake pa iwo, anawapsera mtima nawakwiyira nʼkuwabweretsera masautso. Zimenezi zinali ngati gulu la angelo osakaza.
Takitho e a lungkhueknae hah ahnimouh lathueng a rabawk teh, lungkhueknae, lungpoutnae, hoi runae hah ahnimouh koe thoenae kaphawtkung kalvan tami totouh a tha pouh.
50 Analolera kukwiya, sanawapulumutse ku imfa koma anawapereka ku mliri.
A lungkhueknae hanlah lamthung a sak, a hringnae hah duenae hlak pasai laipalah, lacik mathout hah letlang a poe.
51 Anakantha ana oyamba kubadwa a Igupto, zipatso zoyamba kucha za mphamvu zawo mʼmatenti a Hamu
Izip vah camin pueng hoi Ham e rim a thaonae hmaloe poung e hoi koung a raphoe.
52 Koma Iye anatulutsa anthu ake ngati ziweto; anawatsogolera ngati nkhosa kudutsa mʼchipululu.
Hatei, a taminaw teh tu patetlah a hrawi teh, saringnaw patetlah kahrawngum vah a hrawi.
53 Anawatsogolera bwinobwino kotero kuti analibe mantha koma nyanja inamiza adani awo.
Karoumcalah a hrawi teh, taki hane banghai awm hoeh. A tarannaw teh talîpui ni koung a ramuk.
54 Kotero anawafikitsa ku malire a dziko lake loyera, ku dziko lamapiri limene dzanja lake lamanja linawatengera.
Hahoi, ramri kathoung, aranglae kut hoi a tawn e, mon totouh a hrawi.
55 Iye anathamangitsa mitundu ya anthu patsogolo pawo ndipo anapereka mayiko awo kwa Aisraeli kuti akhale awo; Iye anakhazikitsa mafuko a Israeli mʼnyumba zawo.
Ahnimae hmalah, alouke miphunnaw hah a pâlei pouh. A pang awh hane râw hah a bangnue pouh teh, alouklouk lah hmuen a poe.
56 Koma iwo anayesa Mulungu ndi kuwukira Wammwambamwamba; sanasunge malamulo ake.
Hat nahlangva, Lathueng Poung Cathut hah a tanouk awh teh, a lungkhuek sak awh teh, a panuesaknae lawk hah tarawi awh hoeh.
57 Anakhala okanika ndi osakhulupirika monga makolo awo, anapotoka monga uta wosakhulupirika.
A na mintoenaw patetlah a kamlang awh teh, yuemkamcu hoeh lah a kâroe awh. Dumyennae licung patetlah a kâkamei awh.
58 Anakwiyitsa Iyeyo ndi malo awo opembedzera mafano; anawutsa nsanje yake ndi mafano awo.
Bangkongtetpawiteh, ahnimae hmuerasangnaw ni a lungkhuek sak teh, a sak awh e meikaphawknaw ni dipma sinnae a tâco sak.
59 Pamene Mulungu anamva zimenezi, anakwiya kwambiri; Iye anakana Israeli kwathunthu.
Hetheh Cathut ni a thai toteh, puenghoi a lungkhuek teh, Isarel hah puenghoi a panuet.
60 Anasiya nyumba ya ku Silo, tenti imene Iyeyo anayimanga pakati pa anthu.
Hatdawkvah, taminaw koe a ta e Shiloh rim koe totouh a ceitakhai.
61 Anatumiza mphamvu zake ku ukapolo, ulemerero wake mʼmanja mwa adani.
A thaonae teh san lah a coung sak teh, a lentoenae teh a tarannaw kut dawk a poe.
62 Anapereka anthu ake ku lupanga; anakwiya kwambiri ndi cholowa chake.
A taminaw tahloi a kâhmo sak teh, râw lah a coe e naw koe a lungkhuek.
63 Moto unanyeketsa anyamata awo, ndipo anamwali awo analibe nyimbo za ukwati;
A thoundounnaw teh hmai ni a kak awh teh, a tanglanaw ni vâ kâhmo awh hoeh.
64 ansembe awo anaphedwa ndi lupanga, ndipo amayi awo amasiye sanathe kulira.
A vaihmanaw teh tahloi hoi a thei awh eiteh, lahmainaw ni khui awh hoeh.
65 Kenaka Ambuye anakhala ngati akudzuka kutulo, ngati munthu wamphamvu wofuwula chifukwa cha vinyo.
BAWIPA teh ka ip e patetlah a kâhlaw teh, misurtui kecu dawk ka hram e athakaawme tami patetlah a hram.
66 Iye anathamangitsa adani ake; anawachititsa manyazi ku nthawi zonse.
A taran hah a pâlei teh, a yungyoe min mathoenae hah a poe.
67 Kenaka Iye anakana matenti a Yosefe, sanasankhe fuko la Efereimu;
Hothloilah Joseph rim hah a pahnawt teh, Ephraim miphun hah rawi ngai hoeh.
68 Koma anasankha fuko la Yuda, phiri la Ziyoni limene analikonda.
Ama koehoi Judah miphun, Zion mon ka pahren e heh a rawi.
69 Iye anamanga malo ake opatulika ngati zitunda, dziko limene analikhazikitsa kwamuyaya.
A hmuen kathoung hah karasang e patetlah a sak teh, talai patetlah a yungyoe acak sak.
70 Anasankha Davide mtumiki wake ndi kumuchotsa pakati pa makola ankhosa;
A san Devit hai a rawi teh tutakha thung hoi a la.
71 kuchokera koyangʼanira nkhosa anamubweretsa kuti akhale mʼbusa wa anthu ake, Yakobo, wa Israeli cholowa chake.
Tumanu, a canaw ouk a hrawi e patetlah, a tami Jakop hoi a coe e râw Isarelnaw khenyawnkung hanelah a la.
72 Ndipo Davide anawaweta ndi mtima wolungama; ndi manja aluso anawatsogolera.
Hothloilah, a lungthin ahawi e patetlah, a khetyawt teh, a thoumnae kut hoi a hrawi awh.

< Masalimo 78 >