< Masalimo 71 >

1 Mwa Inu Yehova ine ndathawiramo; musalole kuti ndichititsidwe manyazi.
Mu ngeyo, a Yave, ndisuamina kadi tala ti ndifua tsoni kadi khumbu yimosi!
2 Mundilanditse ndi kundipulumutsa mwa chilungamo chanu, mutchere khutu lanu ndi kundipulumutsa.
Wukhudi ayi wuphukisa mu busonga buaku balula dikutu diaku kuidi minu ayi phukisa.
3 Mukhale thanthwe langa lothawirapo, kumene ine nditha kupita nthawi zonse; lamulani kuti ndipulumuke, pakuti Inu ndinu thanthwe langa ndi linga langa.
Ba ditadi diama diodi di kutsuekanga; momo ndilenda kuenda mu zithangu zioso vana lutumunu mu kuphukisa bila widi ditadi diama ayi tinunu kiama ki ngolo.
4 Landitseni Inu Mulungu wanga, kuchoka mʼdzanja la oyipa, kuchoka mʼdzanja la oyipa ndi anthu ankhanza.
Wukhudi Nzambi ama mu mioko mi batu bambimbi; mu mioko mi batu bamvanganga mambimbi ayi mu batu badi tsita.
5 Pakuti Inu mwakhala chiyembekezo changa, Inu Ambuye Wamphamvuzonse, chilimbikitso changa kuyambira ndili mwana.
Bila ngeyo wuba diana diama, a Yave, ngeyo wumvanganga moso wuzodidi. Diana diama tona mu bumuana buama.
6 Kuyambira pamene ndinabadwa, ndakhala ndikudalira Inu; Inu munanditulutsa mʼmimba mwa amayi anga, ndipo ndidzakupembedzani nthawi zonse.
Tona ndibutuka, mu ngeyo ndieti singimina; ngeyo wuthotula tona mu vumu ki ngudi ama; Ngeyo ndiela zitisanga mu zithangu zioso.
7 Ine ndakhala chinthu chodabwitsa kwa anthu ambiri koma Inu ndinu wonditchinjiriza wamphamvu.
Ndieka banga diambu di siminina kuidi bawombo, vayi ngeyo suamunu kiama kingolo.
8 Pakamwa panga padzaza ndi matamando anu, kulengeza ulemerero wanu tsiku lonse.
Munu ama widi wuwala mu nzitusu aku wunyamikisa kiezila kiaku mu lumbu kimvimba.
9 Musanditaye pamene ndakalamba; musandisiye pamene mphamvu zanga zatha.
Kadi kundoza mu thangu ndieka nunu; kadi kundiekula mu thangu zingolo ziama zilembu suki!
10 Pakuti adani anga ayankhula motsutsana nane; iwo amene amadikira kuti andiphe amapangana pamodzi.
Bila bambeni ziama zilembo thubidila bobo balembo tombi kuphonda, balembo wizana va kimosi,
11 Iwo amati, “Mulungu wamusiya; mutsatireni ndi kumugwira, pakuti palibe amene adzamupulumutse.”
balembo tubi: “Nzambi wunyekudi, nlandakananu, bila kuisi ko mutu wufueti ku nkula.”
12 Musakhale kutali ndi ine Inu Mulungu, bwerani msanga, Inu Mulungu wanga; thandizeni.
Kadi ba thama ayi minu, a Nzambi, yiza nsualu Nzambi ama mu kutsadisa!
13 Ondineneza anga awonongeke mwa manyazi, iwo amene akufuna kundipweteka avale chitonzo ndi manyazi.
Bika mimfundi miama mibungana mu tsoni; bika bobo bantomba kuphanga phasi baba ba lenzo ayi dio kombolo.
14 Koma ine ndidzakhala ndi chiyembekezo mwa Inu nthawi zonse, ndidzakutamandani mowirikizawirikiza.
Vayi kuidi minu, ndiela tulanga kaka diana mu zithangu zioso buela kuzitisanga ngolo.
15 Pakamwa panga padzafotokoza za chilungamo chanu, za chipulumutso chanu tsiku lonse, ngakhale sindikudziwa muyeso wake.
Munu ama wela yolukila busonga buaku ayi phulusu aku mu lumbu kimvimba, bila ndikadi zaba tezo biawu.
16 Ndidzabwera ndi kulengeza za machitidwe amphamvu zanu Inu Ambuye Wamphamvuzonse. Ndidzalengeza chilungamo chanu, chanu chokha.
Ndiela kuiza ayi yamikisa mavanga maku ma lulendo; a Yave, mutu wumvanganga makazodidi ndiela yamikisa busonga buaku; busonga buaku kaka.
17 Kuyambira ubwana wanga, Inu Mulungu mwakhala mukundiphunzitsa, ndipo mpaka lero ine ndikulengeza za ntchito zanu zodabwitsa
Tona mu bumuana buama, a Nzambi, ngeyo wundonga ayi ye lumbu kiaki yayi ndinyamikisanga matsiminanga maku.
18 Ngakhale pamene ndakalamba ndipo imvi zili mbuu musanditaye Inu Mulungu, mpaka nditalengeza mphamvu zanu kwa mibado yonse yakutsogolo.
Bobuawu, bu ndiela nuna ayi zitsuki ziphembi kadi ku ndiekula, a Nzambi. Muingi nditubila lulendo luaku kuidi tsungi yinkuiza, zingolo ziaku kuidi babo bela kuiza.
19 Mphamvu zanu ndi kulungama kwanu zimafika mpaka kumwambamwamba. Ndani wofanana nanu Inu Mulungu, amene mwachita zazikulu?
Busonga buaku buntula nate ku diyilu, a Nzambi. Ngeyo wuvanga mambu manneni; nani a Nzambi widi banga ngeyo e?
20 Ngakhale mwandionetsa mavuto ambiri owawa, mudzabwezeretsanso moyo wanga; kuchokera kunsi kwa dziko lapansi, mudzandiukitsanso.
Ngeyo wumbonisa ziphasi ziwombo ayi zindudi; wela buela kuphutudila luzingu; tona ku tsi ntoto, ngeyo wela buela kuthotula.
21 Inu mudzachulukitsa ulemu wanga ndi kunditonthozanso.
Wela buela wokisa nzitusu ama, ayi buela ku khindisa diaka.
22 Ndidzakutamandani ndi zeze chifukwa cha kukhulupirika kwanu Mulungu, ndidzayimba matamando kwa Inu ndi pangwe, Inu Woyera wa Israeli.
Ndiela kuzitisa mu ngitala mu diambu di kikhuikizi kiaku, a Nzambi ama; ndiela kuyimbidila minzitusu mu Lila. Ngeyo nlongo wu Iseli.
23 Milomo yanga idzafuwula ndi chimwemwe pamene ndidzayimba matamando kwa Inu amene mwandiwombola.
Bididi biama biela yimbila mu diambu di khini mu thangu ndiela kuyimbidila minzitusu, minu mutu wowo wukula.
24 Lilime langa lidzafotokoza za ntchito zanu zachilungamo tsiku lonse, pakuti iwo amene amafuna kundipweteka achititsidwa manyazi ndi kusokonezedwa.
Ludimi luama luela yolukila mavanga maku masonga mu lumbu kimvimba, Bila bobo bantomba kumbonisa phasi bela fua tsoni ayi bela ba dio kombolo.

< Masalimo 71 >