< Masalimo 71 >

1 Mwa Inu Yehova ine ndathawiramo; musalole kuti ndichititsidwe manyazi.
BOEIPA nang dongah ka ying tih, kumhal ah yah m'poh sak boeh.
2 Mundilanditse ndi kundipulumutsa mwa chilungamo chanu, mutchere khutu lanu ndi kundipulumutsa.
Na duengnah neh, kai na huul tih nan hlawt. Te dongah na hna te kai taengla han hooi lamtah, kai n'khang lah.
3 Mukhale thanthwe langa lothawirapo, kumene ine nditha kupita nthawi zonse; lamulani kuti ndipulumuke, pakuti Inu ndinu thanthwe langa ndi linga langa.
Caeh taitu vaengkah ham, kai taengah lungpang khuirhung la ha om lah. Namah te ka thaelpang neh ka rhalvong la na om dongah, kai khang ham khaw na uen.
4 Landitseni Inu Mulungu wanga, kuchoka mʼdzanja la oyipa, kuchoka mʼdzanja la oyipa ndi anthu ankhanza.
Ka Pathen aw, halang kut lamloh, aka phayoe tih aka muen kah kutpha lamloh, kai n'hlawt lah.
5 Pakuti Inu mwakhala chiyembekezo changa, Inu Ambuye Wamphamvuzonse, chilimbikitso changa kuyambira ndili mwana.
Ka Boeipa Yahovah namah tah, ka ngaiuepnah neh, ka camoe lamkah ka pangtungnah ni.
6 Kuyambira pamene ndinabadwa, ndakhala ndikudalira Inu; Inu munanditulutsa mʼmimba mwa amayi anga, ndipo ndidzakupembedzani nthawi zonse.
Bungko khui lamkah nang dongah ka hangdang coeng. Namah loh a nu ko khui lamkah kai nan poh. Namah te kai kah koehnah la na om yoeyah.
7 Ine ndakhala chinthu chodabwitsa kwa anthu ambiri koma Inu ndinu wonditchinjiriza wamphamvu.
Hlang tom taengah mikdairhueng bangla ka om cakhaw namah te ka hlipyingnah sarhi la na om.
8 Pakamwa panga padzaza ndi matamando anu, kulengeza ulemerero wanu tsiku lonse.
Namah kah boeimangnah rhangneh namah koehnah te hnin takuem ka ka ah baetawt.
9 Musanditaye pamene ndakalamba; musandisiye pamene mphamvu zanga zatha.
Ka patong tue vaengah kai m'voei boeh. Ka thadueng a bawt vaengah kai nan hnoo mahpawh.
10 Pakuti adani anga ayankhula motsutsana nane; iwo amene amadikira kuti andiphe amapangana pamodzi.
Ka thunkha rhoek loh kai taengah cal uh tih ka hinglu dawn ham tun caai uh.
11 Iwo amati, “Mulungu wamusiya; mutsatireni ndi kumugwira, pakuti palibe amene adzamupulumutse.”
“Anih he Pathen loh a hnoo coeng dongah hloem uh sih lamtah tu uh sih. Anih aka huul ham khaw hlang a om moenih,” a ti uh.
12 Musakhale kutali ndi ine Inu Mulungu, bwerani msanga, Inu Mulungu wanga; thandizeni.
Pathen aw kai taeng lamkah lakhla tak boeh. Kai bomkung ham ka Pathen nang ha tawn rhoe ha tawn uh laeh.
13 Ondineneza anga awonongeke mwa manyazi, iwo amene akufuna kundipweteka avale chitonzo ndi manyazi.
Ka hinglu aka khingkhoek rhoek te yahpok uh saeh lamtah hmata uh saeh. Kai kah yoethae aka hue rhoe te kokhahnah neh mingthae loh thing uh saeh.
14 Koma ine ndidzakhala ndi chiyembekezo mwa Inu nthawi zonse, ndidzakutamandani mowirikizawirikiza.
Tedae kai loh ka ngaiuep yoeyah vetih namah koehnah te boeih ka khoep ni.
15 Pakamwa panga padzafotokoza za chilungamo chanu, za chipulumutso chanu tsiku lonse, ngakhale sindikudziwa muyeso wake.
Nan khangnah te taenah ham ka ming pawt cakhaw na duengnah te ka ka loh hnin takuem a tae bitni.
16 Ndidzabwera ndi kulengeza za machitidwe amphamvu zanu Inu Ambuye Wamphamvuzonse. Ndidzalengeza chilungamo chanu, chanu chokha.
Ka Boeipa Yahovah kah thayung thamal khuila ka lo vetih, namah bueng dongah ni na duengnah ka thoelh eh.
17 Kuyambira ubwana wanga, Inu Mulungu mwakhala mukundiphunzitsa, ndipo mpaka lero ine ndikulengeza za ntchito zanu zodabwitsa
Pathen aw, ka camoe lamkah kai nan cang puei dongah tahae duela namah kah khobaerhambae te ka doek.
18 Ngakhale pamene ndakalamba ndipo imvi zili mbuu musanditaye Inu Mulungu, mpaka nditalengeza mphamvu zanu kwa mibado yonse yakutsogolo.
Pathen aw, thawnpuei taengah na bantha, hmailong kah aka lo ham boeih taengah na thayung thamal ka doek hlanhil tah patong sampok la ka om cakhaw kai nan hnoo mahpawh.
19 Mphamvu zanu ndi kulungama kwanu zimafika mpaka kumwambamwamba. Ndani wofanana nanu Inu Mulungu, amene mwachita zazikulu?
Tedae Pathen na duengnah loh a sang duela a puet. Pathen loh duelhduelh na saii te, namah bangla ulae aka om?
20 Ngakhale mwandionetsa mavuto ambiri owawa, mudzabwezeretsanso moyo wanga; kuchokera kunsi kwa dziko lapansi, mudzandiukitsanso.
Kai he citcai neh yoethaenah muep nan hmuh khaw nan hmuh sak dae koep nan hing khaw nan hing sak vetih diklai laedil lamkah koep nan lat bal ni.
21 Inu mudzachulukitsa ulemu wanga ndi kunditonthozanso.
Ka lennah nan pueh vetih kai nan hloep bal ni.
22 Ndidzakutamandani ndi zeze chifukwa cha kukhulupirika kwanu Mulungu, ndidzayimba matamando kwa Inu ndi pangwe, Inu Woyera wa Israeli.
Kai khaw ka Pathen namah kah uepomnah te thangpa toembael neh kan uem vetih Israel kah a cim namah te rhotoeng neh ka tingtoeng ni.
23 Milomo yanga idzafuwula ndi chimwemwe pamene ndidzayimba matamando kwa Inu amene mwandiwombola.
Ka hinglu he na lat coeng dongah nang te kan tingtoeng vaengah ka hmui ka lai neh ka tamhoe ni.
24 Lilime langa lidzafotokoza za ntchito zanu zachilungamo tsiku lonse, pakuti iwo amene amafuna kundipweteka achititsidwa manyazi ndi kusokonezedwa.
Kai kah yoethae aka hue rhoek loh yah a poh uh tih a hmai a tal uh coeng dongah ka lai long khaw hnin takuem nang kah duengnah te a thuep ni.

< Masalimo 71 >