< Masalimo 70 >

1 Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide. Pempho. Fulumirani Mulungu kundipulumutsa; Yehova bwerani msanga kudzandithandiza.
Грэбеште, Думнезеуле, де мэ избэвеште! Грэбеште де-мь ажутэ, Доамне!
2 Iwo amene akufunafuna moyo wanga achititsidwe manyazi ndi kusokonezedwa; onse amene akukhumba chiwonongeko changa abwezedwe mopanda ulemu.
Сэ рэмынэ де рушине ши ынфрунтаць чей че вор сэ-мь я вяца! Сэ дя ынапой ши сэ рошяскэ чей че-мь дореск пеиря!
3 Onse amene akunena kwa ine kuti, “Aha, aha,” abwerere chifukwa cha manyazi awo.
Сэ се ынтоаркэ ынапой де рушине чей че зик: „Аха! Аха!”
4 Koma onse amene akufunafuna Inu akondwere ndi kusangalala mwa Inu; iwo amene amakonda chipulumutso chanu nthawi zonse anene kuti, “Mulungu akuzike!”
Тоць чей че Те каутэ сэ се веселяскэ ши сэ се букуре ын Тине! Чей че юбеск мынтуиря Та сэ зикэ неынчетат: „Прямэрит сэ фие Думнезеу!”
5 Koma ine ndine wosauka ndi wosowa; bwerani msanga kwa ine Inu Mulungu. Inu ndinu thandizo langa ndi momboli wanga; Inu Yehova musachedwe.
Еу сунт сэрак ши липсит: грэбеште сэ-мь ажуць, Думнезеуле! Ту ешть Ажуторул ши Избэвиторул меу: Доамне, ну зэбови!

< Masalimo 70 >