< Masalimo 70 >

1 Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide. Pempho. Fulumirani Mulungu kundipulumutsa; Yehova bwerani msanga kudzandithandiza.
[Psalm lal David, Soko On in Asor] Moliyula, O God! LEUM GOD, kasreyu inge!
2 Iwo amene akufunafuna moyo wanga achititsidwe manyazi ndi kusokonezedwa; onse amene akukhumba chiwonongeko changa abwezedwe mopanda ulemu.
Lela tuh elos su srike in uniyuwi In fohsak ac kutangyukla. Lela tuh elos su pwarkin keok luk In folokinyukla ac aklusrongtenyeyuk.
3 Onse amene akunena kwa ine kuti, “Aha, aha,” abwerere chifukwa cha manyazi awo.
Lela tuh elos su isrunyu, In mwekinla ke kutangyukla elos.
4 Koma onse amene akufunafuna Inu akondwere ndi kusangalala mwa Inu; iwo amene amakonda chipulumutso chanu nthawi zonse anene kuti, “Mulungu akuzike!”
Lela tuh elos nukewa su suk kom, Elos in engan ac insewowo. Lela elos nukewa su sang kulo ke molela lom In fahk pacl e nukewa, “God El fulatlana!”
5 Koma ine ndine wosauka ndi wosowa; bwerani msanga kwa ine Inu Mulungu. Inu ndinu thandizo langa ndi momboli wanga; Inu Yehova musachedwe.
Nga munas ac sukasrup; Aksaye nu yuruk, O God! Kom kasreyu ac moliyula. O LEUM GOD, aksaye in kasreyu!

< Masalimo 70 >