< Masalimo 70 >

1 Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide. Pempho. Fulumirani Mulungu kundipulumutsa; Yehova bwerani msanga kudzandithandiza.
[For the Chief Musician. By David. A reminder.] Hurry, God, to deliver me. Come quickly to help me, LORD.
2 Iwo amene akufunafuna moyo wanga achititsidwe manyazi ndi kusokonezedwa; onse amene akukhumba chiwonongeko changa abwezedwe mopanda ulemu.
Let them be put to shame and confounded who seek my soul. Let those who desire my ruin be turned back in disgrace.
3 Onse amene akunena kwa ine kuti, “Aha, aha,” abwerere chifukwa cha manyazi awo.
Let them be turned back because of their shame who say to me, "Aha. Aha."
4 Koma onse amene akufunafuna Inu akondwere ndi kusangalala mwa Inu; iwo amene amakonda chipulumutso chanu nthawi zonse anene kuti, “Mulungu akuzike!”
Let all those who seek you rejoice and be glad in you. Let those who love your salvation continually say, "Let God be exalted."
5 Koma ine ndine wosauka ndi wosowa; bwerani msanga kwa ine Inu Mulungu. Inu ndinu thandizo langa ndi momboli wanga; Inu Yehova musachedwe.
But I am poor and needy. Come to me quickly, God. You are my help and my deliverer. LORD, do not delay.

< Masalimo 70 >