< Masalimo 70 >

1 Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide. Pempho. Fulumirani Mulungu kundipulumutsa; Yehova bwerani msanga kudzandithandiza.
Til Sangmesteren; af David; “til Ihukommelse”.
2 Iwo amene akufunafuna moyo wanga achititsidwe manyazi ndi kusokonezedwa; onse amene akukhumba chiwonongeko changa abwezedwe mopanda ulemu.
Gud! kom at fri mig; Herre! skynd dig at hjælpe mig!
3 Onse amene akunena kwa ine kuti, “Aha, aha,” abwerere chifukwa cha manyazi awo.
Lad dem blues og blive beskæmmede, som søge efter mit Liv; lad dem vige tilbage og blive til Skamme, som have Lyst til min Ulykke.
4 Koma onse amene akufunafuna Inu akondwere ndi kusangalala mwa Inu; iwo amene amakonda chipulumutso chanu nthawi zonse anene kuti, “Mulungu akuzike!”
Lad dem vende tilbage for deres Skændsels Skyld, de, som sige: Ha, ha!
5 Koma ine ndine wosauka ndi wosowa; bwerani msanga kwa ine Inu Mulungu. Inu ndinu thandizo langa ndi momboli wanga; Inu Yehova musachedwe.
Lad dem frydes og glædes i dig, alle de, som søge dig; lad dem, som elske din Frelse, altid sige: Gud være storlig lovet! Men jeg er elendig og fattig; Gud! skynd dig til mig; du er min Hjælp, og den, som udfrier mig; Herre! tøv ikke!

< Masalimo 70 >