< Masalimo 7 >

1 Sigioni wa Davide, amene anayimbira Yehova zokhudza Kusi, wa fuko la Benjamini. Inu Yehova Mulungu wanga, Ine ndikuthawira kwa Inu; pulumutseni ndi kundilanditsa kwa onse amene akundithamangitsa,
Ry Iehovà Andrianañahareko, Ihe ro fitsolohako, avotsoro amo mañoridañe ahikoo, le hahao;
2 mwina angandikadzule ngati mkango, ndi kundingʼamba popanda wondipulumutsa.
Tsy mone ho ritaritae’e hoe liona ty fiaiko, hirofodrofota’e tsy amam-pañolotse.
3 Inu Yehova Mulungu wanga, ngati ndachita izi ndipo ndapezeka wolakwa,
Ry Iehovà Andrianañahareko, naho nanoeko zao: lehe an-tañako ty hatsivokarañe,
4 ngati ndachita zoyipa kwa iye amene ndili naye pa mtendere, kapena popanda chifukwa ndalanda mdani wanga,
naho vinaleko haratiañe ty rañeko; (hera) nivoloseko tsy amam-poto’e ty nañembets’ ahy;
5 pamenepo lolani adani anga andithamangitse ndi kundipitirira, lolani kuti moyo wanga aupondereze pansi ndipo mundigoneke pa fumbi. (Sela)
Le ho hotrohe’ ty rafelahiko, hiambotraha’e; ho lialià’e an-tane ty haveloko, vaho hado’e an-debok’ ao ty engeko. Selà
6 Nyamukani Yehova, mu mkwiyo wanu; nyamukani kutsutsana ndi mkwiyo wa adani anga. Dzukani Mulungu wanga, lamulirani chilungamo chanu.
Miongaha, ry Iehovà, an-kaviñera’o, miavota ty amo fitrotrofiaha’ o rafelahikoo. mivañona ty amako amy zaka kinoi’oy.
7 Lolani gulu la anthu a mitundu ina lisonkhane mokuzungulirani. Alamulireni muli kumwambako;
Hiarikatok’ ama’o ty fivori’ ondatio, vaho mibaliha hifehea’o boak’añ’abo ey.
8 Yehova aweruzeni anthu a mitundu inayo. Ndiweruzeni Yehova, monga mwa chilungamo changa, monga mwa moyo wanga wangwiro, Inu Wammwambamwamba.
Ry Iehovà Mpizaka o kilakila ‘ndatio; zakao iraho ry Iehovà, ty amy havantañako naho ty havañonako an-trok’ ao.
9 Inu Mulungu wolungama, amene mumasanthula maganizo ndi mitima, thetsani chiwawa cha anthu oyipa ndipo wolungama akhale motetezedwa.
Hijihetse ty haratia’ o lo-tserekeo naho hajado’o o vañoñeo, fa mpitsòke arofo naho ova t’i Andrianañahare vantañe.
10 Chishango changa ndi Mulungu Wammwambamwamba, amene amapulumutsa olungama mtima.
Aman’Añahare ao ty fikalako Ie mpandrombake o vañon-trokeo.
11 Mulungu amaweruza molungama, Mulungu amene amaonetsa ukali wake tsiku ndi tsiku.
Mpizaka to t’i Andrianañahare, Eka, torifike boak’ andro t’i Andrianañahare;
12 Ngati munthu satembenuka, Mulungu adzanola lupanga lake, Iye adzawerama ndi kukoka uta.
Aa naho tsy mimpoly t’indaty: le ho sioña’e i fibara’ey; fa navoho’e ty fale’e vaho nihajarie’e;
13 Mulungu wakonza zida zake zoopsa; Iye wakonzekera mivi yake yoyaka moto.
Fa nihentseñe’e fialiañe mahafate, ampibelabelae’ afo o ana-pàle’eo.
14 Taonani, munthu woyipa amalingalira zoyipa zokhazokha nthawi zonse. Zochita zake ndi zosokoneza ndi zovutitsa anthu ena.
Hehe t’ie tsongoen-tsihavokarañe, ie nampiareñe kilily vaho hiterake i remborake;
15 Iye amene akumba dzenje ndi kulizamitsa amagwera mʼdzenje limene wakumbalo.
Nihaly kobon-dre naho nampigorabahe’e, vaho tafajorobo amy hinali’ey.
16 Mavuto amene amayambitsa amamubwerera mwini; chiwawa chake chimatsikira pa mutu wake womwe.
Toe hibalik’ an-doha’e avao ty fikitroha’e raty, vaho hivotrak’ an-kevo’e eo i nandovia’ey.
17 Ine ndidzayamika Yehova chifukwa cha chilungamo chake; ndipo ndidzayimba nyimbo zamatamando pa dzina la Yehova Wammwambamwamba.
Andriañeko t’Iehovà ty amy havantaña’ey, ho bangoeko an-tsabo ty tahina’ Iehovà Andindimoneñe.

< Masalimo 7 >