< Masalimo 7 >

1 Sigioni wa Davide, amene anayimbira Yehova zokhudza Kusi, wa fuko la Benjamini. Inu Yehova Mulungu wanga, Ine ndikuthawira kwa Inu; pulumutseni ndi kundilanditsa kwa onse amene akundithamangitsa,
En Sjiggajon af David, som han sang for HERREN i anledning af Benjaminiten Kusj's Ord.
2 mwina angandikadzule ngati mkango, ndi kundingʼamba popanda wondipulumutsa.
HERRE min Gud, jeg lider paa dig, frels mig og fri mig fra hver min Forfølger,
3 Inu Yehova Mulungu wanga, ngati ndachita izi ndipo ndapezeka wolakwa,
at han ej som en Løve skal rive mig sønder, bortrive, uden at nogen befrier.
4 ngati ndachita zoyipa kwa iye amene ndili naye pa mtendere, kapena popanda chifukwa ndalanda mdani wanga,
HERRE min Gud, har jeg handlet saa, er der Uret i mine Hænder,
5 pamenepo lolani adani anga andithamangitse ndi kundipitirira, lolani kuti moyo wanga aupondereze pansi ndipo mundigoneke pa fumbi. (Sela)
har jeg voldet dem ondt, der holdt Fred med mig, uden Aarsag gjort mine Fjender Men,
6 Nyamukani Yehova, mu mkwiyo wanu; nyamukani kutsutsana ndi mkwiyo wa adani anga. Dzukani Mulungu wanga, lamulirani chilungamo chanu.
saa forfølge og indhente Fjenden min Sjæl, han træde mit Liv til Jorden og kaste min Ære i Støvet. (Sela)
7 Lolani gulu la anthu a mitundu ina lisonkhane mokuzungulirani. Alamulireni muli kumwambako;
HERRE, staa op i din Vrede, rejs dig imod mine Fjenders Fnysen, vaagn op, min Gud, du sætte Retten!
8 Yehova aweruzeni anthu a mitundu inayo. Ndiweruzeni Yehova, monga mwa chilungamo changa, monga mwa moyo wanga wangwiro, Inu Wammwambamwamba.
Lad Folkeflokken samles om dig, tag Sæde over den hist i det høje!
9 Inu Mulungu wolungama, amene mumasanthula maganizo ndi mitima, thetsani chiwawa cha anthu oyipa ndipo wolungama akhale motetezedwa.
HERREN dømmer Folkeslag. Mig dømme du, HERRE, efter min Retfærd og Uskyld!
10 Chishango changa ndi Mulungu Wammwambamwamba, amene amapulumutsa olungama mtima.
Paa gudløses Ondskab gøre du Ende, støt den retfærdige, du, som prøver Hjerter og Nyrer, retfærdige Gud.
11 Mulungu amaweruza molungama, Mulungu amene amaonetsa ukali wake tsiku ndi tsiku.
Mit Skjold er hos Gud, han frelser de oprigtige af Hjertet;
12 Ngati munthu satembenuka, Mulungu adzanola lupanga lake, Iye adzawerama ndi kukoka uta.
retfærdig som Dommer er Gud, en Gud, der hver Dag vredes.
13 Mulungu wakonza zida zake zoopsa; Iye wakonzekera mivi yake yoyaka moto.
Visselig hvæsser han atter sit Sværd, han spænder sin Bue og sigter;
14 Taonani, munthu woyipa amalingalira zoyipa zokhazokha nthawi zonse. Zochita zake ndi zosokoneza ndi zovutitsa anthu ena.
men mod sig selv har han rettet de dræbende Vaaben, gjort sine Pile til brændende Pile.
15 Iye amene akumba dzenje ndi kulizamitsa amagwera mʼdzenje limene wakumbalo.
Se, han undfanger Tomhed, svanger med Ulykke føder han Blændværk;
16 Mavuto amene amayambitsa amamubwerera mwini; chiwawa chake chimatsikira pa mutu wake womwe.
han grov en Grube, han huled den ud, men faldt i den Grav, han gjorde.
17 Ine ndidzayamika Yehova chifukwa cha chilungamo chake; ndipo ndidzayimba nyimbo zamatamando pa dzina la Yehova Wammwambamwamba.
Ulykken falder ned paa hans Hoved, hans Uret rammer hans egen Isse. Jeg vil takke HERREN for hans Retfærd, lovsynge HERREN den Højestes Navn.

< Masalimo 7 >