< Masalimo 67 >

1 Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Pa zoyimbira za zingwe. Salimo. Yehova atikomere mtima ndi kutidalitsa, achititse kuti nkhope yake itiwalire.
Przedniejszemu śpiewakowi na Neginot psalm ku śpiewaniu. Boże! zmiłuj się nad nami, a błogosław nam, rozświeć oblicze twoje nad nami. (Sela)
2 Kuti njira zanu zidziwike pa dziko lapansi, chipulumutso chanu pakati pa mitundu yonse.
Aby tak poznali na ziemi drogę twoję, a po wszystkich narodach zbawienie twoje.
3 Mitundu ya anthu ikutamandeni Inu Mulungu; mitundu yonse ya anthu ikutamandeni.
Tedy cię będą wysławiały narody o Boże! Będą cię wysławiać wszyscy ludzie!
4 Mitundu yonse ya anthu isangalale ndi kuyimba mwachimwemwe, pakuti inu mumaweruza mitundu ya anthu mwachilungamo ndi kutsogolera mitundu ya anthu a dziko lapansi.
Radować się będą i wykrzykać narody; bo ty będziesz sądził ludzi w sprawiedliwości, a narody będziesz sprawował na ziemi. (Sela)
5 Mitundu ya anthu ikutamandeni Inu Mulungu; mitundu yonse ya anthu ikutamandeni.
Będą cię wysławiać narody, o Boże! Będą cię wysławiać wszyscy ludzie.
6 Nthaka yabereka zokolola zake; tidalitseni Mulungu wathu.
Ziemia także wyda urodzaj swój; niech nam błogosławi Bóg, Bóg nasz.
7 Mulungu atidalitse kuti pamenepo malekezero onse a dziko lapansi apembedze Iyeyo.
Niech nam błogosławi Bóg, a niech się go boją wszystkie kraje ziemi.

< Masalimo 67 >