< Masalimo 67 >
1 Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Pa zoyimbira za zingwe. Salimo. Yehova atikomere mtima ndi kutidalitsa, achititse kuti nkhope yake itiwalire.
KOT en kotin maki on kit, o kotin kapaia kin kit. A kotin kamaraine kin kit, jilan i.
2 Kuti njira zanu zidziwike pa dziko lapansi, chipulumutso chanu pakati pa mitundu yonse.
Pwe japwilim a al akan me janjaleda nin jappa o ren men liki kan a maur.
3 Mitundu ya anthu ikutamandeni Inu Mulungu; mitundu yonse ya anthu ikutamandeni.
Main Kot, wei kan pan kapina komui, wei kan karoj pan kapina komui.
4 Mitundu yonse ya anthu isangalale ndi kuyimba mwachimwemwe, pakuti inu mumaweruza mitundu ya anthu mwachilungamo ndi kutsogolera mitundu ya anthu a dziko lapansi.
Wei kan pan peren kida o nijinij, pwe kom kin kotin kapun on wei kan ni tiak pun, o kom kotin kaunda aramaj akan nin jappa.
5 Mitundu ya anthu ikutamandeni Inu Mulungu; mitundu yonse ya anthu ikutamandeni.
Main Kot, wei kan pan kapina komui, wei kan karoj pan kapina komui.
6 Nthaka yabereka zokolola zake; tidalitseni Mulungu wathu.
Jap o kin kapwaiada a tuka kan. Kot pan kotin kapai kit ada, at Kot.
7 Mulungu atidalitse kuti pamenepo malekezero onse a dziko lapansi apembedze Iyeyo.
Kot pan kotin kapai kit ada, o toun jappa karoj pan majak i!