< Masalimo 67 >

1 Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Pa zoyimbira za zingwe. Salimo. Yehova atikomere mtima ndi kutidalitsa, achititse kuti nkhope yake itiwalire.
Psalmi ja veisu, edelläveisaajalle, kanteleilla. Jumala olkoon meille armollinen, ja siunatkoon meitä! hän valistakoon kasvonsa aina meidän päällemme, (Sela)
2 Kuti njira zanu zidziwike pa dziko lapansi, chipulumutso chanu pakati pa mitundu yonse.
Että me maan päällä tuntisimme sinun ties, ja kaikkein pakanain seassa sinun autuutes.
3 Mitundu ya anthu ikutamandeni Inu Mulungu; mitundu yonse ya anthu ikutamandeni.
Sinua, Jumala, kansat kiittäköön: sinua kaikki kansat kiittäköön.
4 Mitundu yonse ya anthu isangalale ndi kuyimba mwachimwemwe, pakuti inu mumaweruza mitundu ya anthu mwachilungamo ndi kutsogolera mitundu ya anthu a dziko lapansi.
Kansat iloitkaan ja riemuitkaan, ettäs kansat oikein tuomitset, ja hallitset kansat maan päällä, (Sela)
5 Mitundu ya anthu ikutamandeni Inu Mulungu; mitundu yonse ya anthu ikutamandeni.
Sinua, Jumala, kansat kiittäköön: sinua kaikki kansat kiittäköön.
6 Nthaka yabereka zokolola zake; tidalitseni Mulungu wathu.
Maa antaa hedelmänsä; siunatkoon meitä Jumala, meidän Jumalamme.
7 Mulungu atidalitse kuti pamenepo malekezero onse a dziko lapansi apembedze Iyeyo.
Siunatkoon meitä Jumala, ja kaikki maailma peljätköön häntä.

< Masalimo 67 >