< Masalimo 67 >

1 Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Pa zoyimbira za zingwe. Salimo. Yehova atikomere mtima ndi kutidalitsa, achititse kuti nkhope yake itiwalire.
Til Sangmesteren; med Strengeleg; en Psalme, en Sang.
2 Kuti njira zanu zidziwike pa dziko lapansi, chipulumutso chanu pakati pa mitundu yonse.
Gud være os naadig og velsigne os; han lade sit Ansigt lyse for os (Sela)
3 Mitundu ya anthu ikutamandeni Inu Mulungu; mitundu yonse ya anthu ikutamandeni.
at man maa kende din Vej paa Jorden, din Frelse iblandt alle Hedninger!
4 Mitundu yonse ya anthu isangalale ndi kuyimba mwachimwemwe, pakuti inu mumaweruza mitundu ya anthu mwachilungamo ndi kutsogolera mitundu ya anthu a dziko lapansi.
Dig skulle Folkestammerne prise, o Gud! dig skulle Folkestammerne prise alle tilsammen.
5 Mitundu ya anthu ikutamandeni Inu Mulungu; mitundu yonse ya anthu ikutamandeni.
Folkeslag skulle glæde sig og synge med Fryd; thi du dømmer Folkestammer med Ret, og Folkeslag paa Jorden dem fører du. (Sela)
6 Nthaka yabereka zokolola zake; tidalitseni Mulungu wathu.
Dig skulle Folkestammerne prise, o Gud! dig skulle Folkestammerne prise alle tilsammen.
7 Mulungu atidalitse kuti pamenepo malekezero onse a dziko lapansi apembedze Iyeyo.
Landet har givet sin Grøde; Gud, vor Gud, vil velsigne os. Gud vil velsigne os, og alle Jordens Grænser skulle frygte ham.

< Masalimo 67 >