< Masalimo 67 >

1 Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Pa zoyimbira za zingwe. Salimo. Yehova atikomere mtima ndi kutidalitsa, achititse kuti nkhope yake itiwalire.
Přednějšímu z kantorů na neginot, žalm k zpívání. Bože, smiluj se nad námi, a požehnej nám, zasvěť oblíčej svůj nad námi, (Sélah)
2 Kuti njira zanu zidziwike pa dziko lapansi, chipulumutso chanu pakati pa mitundu yonse.
Tak aby poznali na zemi cestu tvou, mezi všemi národy spasení tvé.
3 Mitundu ya anthu ikutamandeni Inu Mulungu; mitundu yonse ya anthu ikutamandeni.
I budou tě oslavovati národové, ó Bože, oslavovati tě budou všickni lidé.
4 Mitundu yonse ya anthu isangalale ndi kuyimba mwachimwemwe, pakuti inu mumaweruza mitundu ya anthu mwachilungamo ndi kutsogolera mitundu ya anthu a dziko lapansi.
Veseliti se a prozpěvovati budou národové; nebo ty souditi budeš lidi v pravosti, a národy spravovati budeš na zemi. (Sélah)
5 Mitundu ya anthu ikutamandeni Inu Mulungu; mitundu yonse ya anthu ikutamandeni.
I budou tě oslavovati národové, ó Bože, oslavovati tě budou všickni lidé.
6 Nthaka yabereka zokolola zake; tidalitseni Mulungu wathu.
Země také vydá úrodu svou. Požehnání svého uděliž nám Bůh, Bůh náš;
7 Mulungu atidalitse kuti pamenepo malekezero onse a dziko lapansi apembedze Iyeyo.
Požehnej nás Bůh, a bojtež se jeho všecky končiny země.

< Masalimo 67 >