< Masalimo 66 >

1 Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo. Fuwulani kwa Mulungu ndi chimwemwe, dziko lonse lapansi!
Ipukkawyo iti panagdaydayawyo iti Dios, iti entero a daga;
2 Imbani ulemerero wa dzina lake; kumutamanda kwake kukhale kwaulemerero.
Ikantayo iti dayag ti naganna; pagbalinenyo a nadayag ti pammadayaw kenkuana.
3 Nenani kwa Mulungu, “Ntchito zanu ndi zoopsa ndithu! Mphamvu yanu ndi yayikulu kwambiri kotero kuti adani anu amawerama pamaso panu.
Ibagayo iti Dios, “Anian a nakakaskasdaaw dagiti aramidmo! Babaen iti nabileg a pannakabalinmo, agtulnog kenka dagiti kabusormo.
4 Dziko lonse lapansi limaweramira inu; limayimba matamando kwa Inu; limayimba matamando pa dzina lanu.” (Sela)
Idaydayaw ken kantaandaka ti entero a daga; agkantada iti pagdaydayaw iti naganmo.” (Selah)
5 Bwerani mudzaone zimene Mulungu wachita, ntchito zanu ndi zoopsa ndithu pakati pa anthu.
Umayyo kitaen dagiti aramid ti Dios; nakakaskasdaaw iti inaramidna kadagiti annak ti tao.
6 Iye anasandutsa nyanja kukhala malo owuma, iwo anawoloka pa madzi ndi mapazi. Bwerani, tiyeni tikondwere mwa Iye.
Pinagbalinna a namaga a daga iti baybay; pinagnada a binallasiw ti karayan; nagrag-otayo sadiay kenkuana.
7 Iye amalamulira ndi mphamvu zake mpaka muyaya, maso ake amayangʼanira anthu a mitundu ina. Anthu owukira asadzitukumule.
Agturturay isuna iti agnanayon babaen iti pannakabalinna; mat-matmatanna dagiti nasion; saan a palubosan nga itag-ay dagiti kabusor dagiti bagbagida. (Selah)
8 Tamandani Mulungu wathu, inu mitundu ya anthu, mulole kuti mawu a matamando ake amveke;
Dayawenyo ti Dios, dakayo a tattao, ipangngegyo kadagiti tattao ti panagdayawyo kenkuana.
9 Iye watchinjiriza miyoyo yathu ndi kusunga mapazi athu kuti angaterereke.
Inaywanannatayo tapno agtalinaedtayo a sibibiag, ken saanna nga itulok a maikaglis dagiti sakatayo.
10 Pakuti Inu Mulungu munatiyesa; munatiyenga ngati siliva.
Ta sika, O Dios, sinuotnakami; sinuotnakami a kas iti pirak.
11 Inu mwatilowetsa mʼndende ndi kutisenzetsa zolemera pa misana yathu.
Impalubosmo a masiloankami; inikkam iti nakaro a dadagsen dagiti siketmi.
12 Inu munalola kuti anthu akwere pa mitu yathu; ife tinadutsa mʼmoto ndi mʼmadzi, koma Inu munatibweretsa ku malo a zinthu zochuluka.
Impalubosmo nga ibadde-baddekdakami dagiti tattao; limmasatkami kadagiti apuy ken danum, ngem impannakami iti nalawa a lugar.
13 Ine ndidzabwera ku Nyumba yanu ndi nsembe zopsereza ndi kukwaniritsa malumbiro anga.
Umayak iti balaymo nga addaan iti daton a maipuor; bayadak dagiti sapatak kenka
14 Malumbiro amene milomo yanga inalonjeza ndi pakamwa panga panayankhula pamene ndinali pa mavuto.
nga inkari dagiti bibigko ken inbalikas ti ngiwatko idi tiempo ti pannakariribukko.
15 Ndidzapereka nsembe nyama zonenepa kwa Inu ndi chopereka cha nkhosa zazimuna; ndidzapereka ngʼombe zamphongo ndi mbuzi. (Sela)
Idatagko kenka dagiti maipuor a daton a nalulukmeg nga ayup ken kadagiti nabanglo nga ayamuom dagiti kalakian a karnero; Agidatonak kadagiti bulog a baka ken kalding. (Selah)
16 Bwerani ndipo mudzamve inu nonse amene mumaopa Mulungu. Ndidzakuwuzani zimene Iyeyo wandichitira.
Umayyo denggen, dakayo amin a managbuteng iti Dios, ken ipablaakko ti inaramidna iti kararuak.
17 Ndinafuwula kwa Iye ndi pakamwa panga, matamando ake anali pa lilime panga.
Nagsangitak kenkuana, ken indaydayaw iti dilak isuna.
18 Ndikanasekerera tchimo mu mtima mwanga Ambuye sakanamvera;
No saanko nga inkankano dagiti basolko, saannak koma a dinengngeg ti Apo.
19 koma ndithu Mulungu wamvetsera ndipo watchera khutu ku mawu a kupempha kwanga.
Ngem pudno a nangngeg ti Dios, ken impangagna ti timek ti kararagko.
20 Matamando akhale kwa Mulungu amene sanakane pemphero langa kapena kuletsa chikondi chake pa ine!
Idaydayawko ti Dios, a saan a timmallikod iti kararagko wenno iti kinapudnona iti tulagna kaniak.

< Masalimo 66 >