< Masalimo 66 >
1 Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo. Fuwulani kwa Mulungu ndi chimwemwe, dziko lonse lapansi!
Dunu huluane! Godema hahawane nodone wele sia: ma!
2 Imbani ulemerero wa dzina lake; kumutamanda kwake kukhale kwaulemerero.
Ea Hadigi Dio amoma gesami hea: ma! Amola hadigiwane Ema nodone sia: ma!
3 Nenani kwa Mulungu, “Ntchito zanu ndi zoopsa ndithu! Mphamvu yanu ndi yayikulu kwambiri kotero kuti adani anu amawerama pamaso panu.
Godema amane sia: ma, “Dia hamobe liligi da noga: idafa gala. Dia da bagadedafaba: le, Dima ha lai dunu da beda: ga, Dia midadi begudusa.
4 Dziko lonse lapansi limaweramira inu; limayimba matamando kwa Inu; limayimba matamando pa dzina lanu.” (Sela)
Osobo bagade fifi asi gala dunu huluanedafa da Dima nodone sia: ne gadolala. Ilia da Dima nodone gesami hea: sa. Ilia da Dia Dio gaguia gadole gesami hea: sa.
5 Bwerani mudzaone zimene Mulungu wachita, ntchito zanu ndi zoopsa ndithu pakati pa anthu.
Gode Ea hamobe amo ba: la misa! Ea dunu fi amo ganodini Ea noga: idafa hamobe amo ba: la misa.
6 Iye anasandutsa nyanja kukhala malo owuma, iwo anawoloka pa madzi ndi mapazi. Bwerani, tiyeni tikondwere mwa Iye.
E da hano wayabo bagade afadenene, bu hafoga: i soge hamoi. Ninia aowalali da Yodane Hano amo emoga degei. Amogawi, ninia da Ea hamoi amo ba: lalu bagade nodoi.
7 Iye amalamulira ndi mphamvu zake mpaka muyaya, maso ake amayangʼanira anthu a mitundu ina. Anthu owukira asadzitukumule.
E da Ea gasaga fifi asi gala ouligilala. E da fifi asi gala huluane Ea siga ba: lala. Ema lelesu dunu ilia da Ema mae lelema: ma!
8 Tamandani Mulungu wathu, inu mitundu ya anthu, mulole kuti mawu a matamando ake amveke;
Osobo bagade fifi asi gala huluane! Ninia Godema nodona: di! Dunu huluane da dilia Ema nodobe nabimu da defea!
9 Iye watchinjiriza miyoyo yathu ndi kusunga mapazi athu kuti angaterereke.
E da nini gebewane esaloma: ne ouligi. Amola nini mae dafama: ne ouligi.
10 Pakuti Inu Mulungu munatiyesa; munatiyenga ngati siliva.
Gode! Silifa da laluga gobele, noga: i amola wadela: i afafama: ne adoba: be agoane, Di da nini adoba: i.
11 Inu mwatilowetsa mʼndende ndi kutisenzetsa zolemera pa misana yathu.
Di da nini saniga sa: ima: ne adodigi. Di da ninia baligi da: iya dioi liligi ligisi.
12 Inu munalola kuti anthu akwere pa mitu yathu; ife tinadutsa mʼmoto ndi mʼmadzi, koma Inu munatibweretsa ku malo a zinthu zochuluka.
Di da ninima ha lai dunu ninima hasalasima: ne yolesi. Ninia da lalu gelabodili amola hano heda: i degele asi. Be wali Di da ninia gado sogebi amoga oule misi dagoi.
13 Ine ndidzabwera ku Nyumba yanu ndi nsembe zopsereza ndi kukwaniritsa malumbiro anga.
Na da Dima gobei gobele salasu liligi amo Dia diasuga gaguli misunu. Na da Dima ilegei liligi amo Dima imunusa: olemu.
14 Malumbiro amene milomo yanga inalonjeza ndi pakamwa panga panayankhula pamene ndinali pa mavuto.
Na da nama bidi hamosu doaga: loba, na da adi Dima imunusa: sia: i liligi, amo Dima imunu.
15 Ndidzapereka nsembe nyama zonenepa kwa Inu ndi chopereka cha nkhosa zazimuna; ndidzapereka ngʼombe zamphongo ndi mbuzi. (Sela)
Na da sibi amo oloda da: iya gobele sanasimusa: imunu. Na da bulamagau gawali amola goudi gobele salimu. Amola gobele salasu mobi da muagado heda: mu.
16 Bwerani ndipo mudzamve inu nonse amene mumaopa Mulungu. Ndidzakuwuzani zimene Iyeyo wandichitira.
Godema nodone dawa: su dunu huluane! Naba misa! Amola na da Ea nama hamobe amo huluane dilima olelemu.
17 Ndinafuwula kwa Iye ndi pakamwa panga, matamando ake anali pa lilime panga.
Na da Ema na fidima: ne dini i. Na da gesami hea: su Ema nodone sia: i.
18 Ndikanasekerera tchimo mu mtima mwanga Ambuye sakanamvera;
Na da na wadela: i hou banenesisa ganiaba, Hina Gode da na sia: ne gadobe hame naba: loba.
19 koma ndithu Mulungu wamvetsera ndipo watchera khutu ku mawu a kupempha kwanga.
Be Gode da dafawane na sia: ne gadobe nabi.
20 Matamando akhale kwa Mulungu amene sanakane pemphero langa kapena kuletsa chikondi chake pa ine!
Na da Godema nodosa. Bai E da na sia: ne gadosu hame higa: i. Amola E da nama mae fisili Ea asigidafa hou hame gagulaligi.