< Masalimo 65 >

1 Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide. Nyimbo. Matamando akudikira Inu Mulungu mu Ziyoni; kwa inu malumbiro athu adzakwaniritsidwa.
Dāvida dziesma. Dziedātāju vadonim. Dievs, klusībā iekš Ciānas Tu topi slavēts, un solījumi Tev top maksāti.
2 Inu amene mumamva pemphero, kwa inu anthu onse adzafika.
Tu paklausi lūgšanas, visa miesa nāk pie Tevis.
3 Pamene tinathedwa nzeru ndi machimo, Inu munakhululukira mphulupulu zathu.
Noziegumi mūs ir pārvarējuši, - mūsu pārkāpumus, tos Tu salīdzini!
4 Odala iwo amene inu muwasankha ndi kuwabweretsa pafupi kukhala mʼmabwalo anu! Ife tadzazidwa ndi zinthu zabwino za mʼNyumba mwanu, za mʼNyumba yanu yoyera.
Svētīgs tas, ko Tu izredzi, un kam Tu vaļu dod pie Tevis nākt un dzīvot Tavos pagalmos; mēs tapsim paēdināti no Tava nama labuma Tavā svētā dzīvoklī.
5 Mumatiyankha ife ndi ntchito zodabwitsa zachilungamo, Inu Mulungu Mpulumutsi wathu, chiyembekezo cha mathero onse a dziko lapansi ndi cha nyanja zomwe zili kutali kwambiri,
Paklausi mūs pēc tās taisnības, kas brīnišķas lietas dara, ak Dievs, mūsu Pestītājs, Tu patvērums visām zemes robežām, un tiem, kas tālu pie jūras dzīvo.
6 amene munapanga mapiri ndi mphamvu zanu, mutadziveka nokha ndi mphamvu.
Tu stiprini kalnus ar Savu spēku, Tu apjozies ar varu,
7 Amene munakhalitsa bata nyanja kukokoma kwa mafunde ake, ndi phokoso la anthu a mitundu ina.
Tu klusini jūras kaukšanu, viņas viļņu kaukšanu un ļaužu troksni,
8 Iwo amene akukhala kutali amaopa zizindikiro zozizwitsa zanu; kumene dzuwa limatulukira ndi kumene dzuwa limalowera. Inu mumafuna nyimbo zachimwemwe.
Ka tie, kas dzīvo tanīs robežās, bīstas no Tavām zīmēm. Tu iepriecini visu, kas kust, vakarā un rītā.
9 Inu mumasamalira dziko lapansi ndi kulithirira; Inuyo mumalilemeretsa kwambiri. Mtsinje wa Mulungu ndi wodzaza ndi madzi kuti upereke tirigu kwa anthu, pakuti Inu munakhazikitsa zimenezi.
Tu piemeklē zemi un to dzirdini un to dari ļoti bagātu. Dieva upīte ir ūdens pilna. Tu liec viņu labībai labi izdoties, jo tā Tu zemi apkopi.
10 Mwadzaza nthaka yake ndi madzi ndi kusalaza migula yake, mwayifewetsa ndi mvula yamawawa ndi kudalitsa mbewu zake.
Tu slacini viņas vagas, un liec lietum līt uz viņas arumiem; Tu tos dari mīkstus caur lāsēm, Tu svētī viņas asnus.
11 Inu mumaveka chaka ndi zinthu zochuluka, ndipo ngolo zanu zimasefukira ndi zinthu zochuluka.
Tu pušķo gadu ar Savu labumu, un Tavas pēdas pil no taukumiem.
12 Malo a udzu a mʼchipululu amasefukira; mapiri avekedwa ndi chisangalalo.
Tuksneša ganības pil un pakalni ar prieku ir apjozti.
13 Madambo akutidwa ndi zoweta ndi zigwa zavekedwa ndi tirigu; izo pamodzi zikufuwula ndi kuyimba mwachimwemwe.
Lauki ir apģērbti ar ganāmiem pulkiem, un ielejas ar labību apklātas, ka gavilē un dzied.

< Masalimo 65 >