< Masalimo 64 >

1 Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide. Ndimvereni Mulungu pomwe ndikunena madandawulo anga; tetezani moyo wanga ku chiopsezo cha mdani.
Davidin Psalmi, edelläveisaajalle. Kuule, Jumala, ääntäni, minun valituksessani: varjele elämäni vihollisen pelvosta.
2 Ndibiseni ku chiwembu cha anthu oyipa, ku gulu laphokoso la anthu ochita zoyipa.
Peitä minua pahain neuvosta, väärintekiäin metelistä,
3 Iwo amanola malilime awo ngati malupanga, amaponya mawu awo olasa ngati mivi.
Jotka kielensä hiovat niinkuin miekan: he ampuvat myrkyllisillä sanoillansa niinkuin nuolilla;
4 Iwo amaponya mivi yawo ali pa malo wobisala kwa munthu wosalakwa; amamulasa modzidzimutsa ndi mopanda mantha.
Että he salaisesti ampuisivat viatointa: he ampuvat häntä äkisti ilman pelvota.
5 Iwo amalimbikitsana wina ndi mnzake pa chikonzero chawo choyipa, amayankhula zobisa misampha yawo; ndipo amati, “Adzayiona ndani?”
He vahvistavat itsensä pahoissa juonissansa ja puhuvat, kuinka he paulat virittäisivät, ja sanovat: kuka taitaa ne nähdä?
6 Iwo amakonzekera zosalungama ndipo amati, “Takonza ndondomeko yabwino kwambiri!” Ndithu maganizo ndi mtima wa munthu ndi zachinyengo.
He ajattelevat vääryyttä, ja täyttävät sen minkä he ajatelleet ovat; viekkaat ihmiset ja salakavalat sydämet.
7 Koma Mulungu adzawalasa ndi mivi; mwadzidzidzi adzakanthidwa.
Mutta Jumala ampuu heitä; äkillinen nuoli on heidän rangaistuksensa.
8 Iye adzatembenuza milomo yawoyo kuwatsutsa ndi kuwasandutsa bwinja; onse amene adzawaona adzagwedeza mitu yawo mowanyoza.
Heidän oma kielensä pitää heitä langettaman, että jokainen, joka heidät näkee, pakenee heitä.
9 Anthu onse adzachita mantha; adzalengeza ntchito za Mulungu ndi kulingalira mozama zomwe Iye wazichita.
Ja kaikkein ihmisten pitää pelkäämän, ja Jumalan työtä ilmoittaman, ja hänen työnsä ymmärtämän.
10 Lolani wolungama akondwere mwa Yehova ndi kubisala mwa Iye, owongoka mtima onse atamande Iye!
Vanhurskaat pitää Herrassa riemuitseman, ja häneen uskaltaman; ja kaikki vaat sydämet kerskatkoon siitä.

< Masalimo 64 >