< Masalimo 62 >

1 Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Kutsata mayimbidwe a Yedutuni. Salimo la Davide. Moyo wanga umapeza mpumulo mwa Mulungu yekha; chipulumutso changa chimachokera kwa Iye.
I Andrianañahare avao ty fitamà’ ty fiaiko am-pitsiñañe, boak’ ama’e ty fandrombahañe ahy.
2 Iye yekhayo ndiye thanthwe langa ndi chipulumutso changa; Iye ndi linga langa, choncho sindidzagwedezeka.
Ie avao ro lamilamiko naho ty fandrombahañe ahy; i haboam-pipalirakoy; tsy hasiotsiotse iraho.
3 Kodi nonsenu mudzalimbana naye munthu mpaka liti? Kodi mudzamugwetsa pansi ngati khoma losalimba, ngati mpanda wogwedezeka?
Pak’ombia ty ho boroboñafe’ areo t’indaty?­ Hanjevoa’areo iaby hoe t’ie rindriñe mitondritse, ndra kijoly migavengaveñe.
4 Iwo akufunitsitsa kumugwetsa kuti achoke pa malo ake apamwamba. Iwo amakondweretsedwa ndi mabodza. Ndi pakamwa pawo amadalitsa koma mʼmitima yawo amatemberera.
Ty hamotsahañe aze ami’ty haabo’e avao ro fikililia’ iareo: mpitea volam-bande; mitata am-palie, f’ie mamatse añ’ova ao Selà
5 Peza mpumulo mwa Mulungu yekhayo iwe moyo wanga; chiyembekezo changa chichokera mwa Iye.
I Andrianañahare avao ty liñisa’o ampitsiñañe, ty fiaiko toy; boak’ ama’e ty fisalalàko.
6 Iye yekhayo ndiye thanthwe langa ndi chipulumutso changa; Iyeyo ndi linga langa; sindidzagwedezeka.
Ie avao ro lamilamiko naho fandrombahañe ahy; ty kijoliko abo; tsy hasiotse iraho.
7 Chipulumutso changa ndi ulemu wanga zimachokera kwa Mulungu: Iye ndiye thanthwe langa lamphamvu; Mulungu ndiye pothawira panga.
I Andrianañahare ty ampipohañe ty fandrombahañe ahy, naho ty engeko; ty lamilamin-kaozarako; fipalirako t’i Andrianañahare.
8 Dalirani Iye nthawi zonse, inu anthu; khuthulani mitima yanu kwa Iye, pakuti Mulungu ndiye pothawirapo pathu. (Sela)
Miatoa ama’e nainai’e, ondatio, adoaño añatrefa’e ty arofo’ areo; fitsolohan-tika t’i Andrianañahare. Selà
9 Anthu wamba ndi mpweya chabe; anthu apamwamba ndi bodza chabe; ngati atayezedwa pa sikelo iwo ndi chabe; iwowo pamodzi ndi mpweya ndi chabe
Toe hakoahañe avao o ana’ i Dameo, lañitse o ana’ ondatio; ie atraok’ am-pilanjàñe eo, le maivañe te ami’ty kofòke.
10 Musadalire kulanda mwachinyengo kapena katundu wobedwa; ngakhale chuma chanu chichuluke, musayike mtima wanu pa icho.
Ko iatoa’o ty fikatramoañe, naho ko manao fañirian-kafoake am-pikamerañe. Ndra te mionjoñe o varao ko ampirampian’ arofo.
11 Mulungu wayankhula kamodzi, ine ndamvapo zinthu ziwiri; choyamba nʼchakuti Inu Mulungu ndinu wamphamvu,
Nitsara indraike t’i Andrianañahare, tsinanoko indroe ty hoe: An’Andrianañahare o haozarañeo,
12 komanso Inu Ambuye, chikondi chanu nʼchosasinthika. Chachiwiri nʼchakuti mumamuchitira munthu molingana ndi ntchito zake.
vaho ama’o, ry Talè, ty fiferenaiñañe, songa tambeze’o mañeva o fitoloña’eo t’i ondaty.

< Masalimo 62 >