< Masalimo 62 >

1 Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Kutsata mayimbidwe a Yedutuni. Salimo la Davide. Moyo wanga umapeza mpumulo mwa Mulungu yekha; chipulumutso changa chimachokera kwa Iye.
Til Sangmesteren; for Jeduthun; en Psalme af David.
2 Iye yekhayo ndiye thanthwe langa ndi chipulumutso changa; Iye ndi linga langa, choncho sindidzagwedezeka.
Kun for Gud er min Sjæl stille, fra ham kommer min Frelse.
3 Kodi nonsenu mudzalimbana naye munthu mpaka liti? Kodi mudzamugwetsa pansi ngati khoma losalimba, ngati mpanda wogwedezeka?
Kun han er min Klippe og min Frelse, min Befæstning; jeg skal ikke rokkes meget.
4 Iwo akufunitsitsa kumugwetsa kuti achoke pa malo ake apamwamba. Iwo amakondweretsedwa ndi mabodza. Ndi pakamwa pawo amadalitsa koma mʼmitima yawo amatemberera.
Hvor længe storme I imod en Mand, alle tilsammen for at myrde ham, der er som en Væg, der hælder, som en Mur, der har faaet Stød?
5 Peza mpumulo mwa Mulungu yekhayo iwe moyo wanga; chiyembekezo changa chichokera mwa Iye.
Kun om at nedstøde ham fra hans Højhed raadslaa de, de have Behag i Løgn; de velsigne med deres Mund, og de forbande i deres Inderste. (Sela)
6 Iye yekhayo ndiye thanthwe langa ndi chipulumutso changa; Iyeyo ndi linga langa; sindidzagwedezeka.
Kun for Gud vær stille min Sjæl; thi af ham er min Forventning.
7 Chipulumutso changa ndi ulemu wanga zimachokera kwa Mulungu: Iye ndiye thanthwe langa lamphamvu; Mulungu ndiye pothawira panga.
Kun han er min Klippe og min Frelse, min Befæstning; jeg skal ikke rokkes.
8 Dalirani Iye nthawi zonse, inu anthu; khuthulani mitima yanu kwa Iye, pakuti Mulungu ndiye pothawirapo pathu. (Sela)
Hos Gud er min Frelse og min Ære, min Styrkes Klippe, min Tilflugt er i Gud.
9 Anthu wamba ndi mpweya chabe; anthu apamwamba ndi bodza chabe; ngati atayezedwa pa sikelo iwo ndi chabe; iwowo pamodzi ndi mpweya ndi chabe
Forlader eder paa ham til hver Tid, I Folk! udøser eders Hjerte for hans Ansigt; Gud er vor Tilflugt. (Sela)
10 Musadalire kulanda mwachinyengo kapena katundu wobedwa; ngakhale chuma chanu chichuluke, musayike mtima wanu pa icho.
Kun Forfængelighed ere Menneskens Børn, Falskhed ere Menneskene; lægges de i Vægtskaalen, stige de til Vejrs, de ere Forfængelighed til Hobe.
11 Mulungu wayankhula kamodzi, ine ndamvapo zinthu ziwiri; choyamba nʼchakuti Inu Mulungu ndinu wamphamvu,
Forlader eder ikke paa Vold og sætter ikke forfængeligt Haab til røvet Gods; falder Rigdom eder til, da sætter ikke Hjertet dertil!
12 komanso Inu Ambuye, chikondi chanu nʼchosasinthika. Chachiwiri nʼchakuti mumamuchitira munthu molingana ndi ntchito zake.
Een Gang har Gud talt, ja, to Gange, hvad jeg har hørt: At Styrke hører Gud til. Og dig, Herre! hører Miskundhed til; thi du skal betale hver efter hans Gerning.

< Masalimo 62 >