< Masalimo 61 >
1 Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide. Loyimbidwa ndi zipangizo za zingwe. Imvani kulira kwanga, Inu Mulungu; mvetserani pemphero langa.
För sångmästaren, till strängaspel; av David. Hör, o Gud, mitt rop, akta på min bön.
2 Kuchokera ku malekezero a dziko lapansi ine ndimayitana Inu ndimayitana pomwe mtima wanga ukufowoka; tsogolereni ku thanthwe lalitali kuposa ineyo.
Från jordens ända ropar jag till dig, ty mitt hjärta försmäktar; för mig upp på en klippa, som är mig alltför hög.
3 Pakuti Inu mwakhala pothawirapo panga, nsanja yolimba polimbana ndi adani anga.
Ty du är min tillflykt, ett starkt torn mot fienden.
4 Ine ndikulakalaka kukhala mʼtenti yanu kwamuyaya ndi kupeza chitetezo mu mthunzi wa mapiko anu.
Låt mig bo i din hydda evinnerligen; under dina vingars beskärm tager jag min tillflykt. (Sela)
5 Pakuti Inu Mulungu mwamva malumbiro anga; mwandipatsa cholowa cha iwo amene amaopa dzina lanu.
Ty du, o Gud, hör mina löften, åt dem som frukta ditt namn giver du en arvedel.
6 Wonjezerani masiku a moyo wa mfumu, zaka zake kwa mibado yochuluka.
Du förökar konungens dagar; hans år skola vara från släkte till släkte.
7 Iye akhale pa mpando waufumu pamaso pa Mulungu kwamuyaya; ikani chikondi chanu ndi kukhulupirika kwanu kuti zimuteteze.
Må han sitta på sin tron inför Gud evinnerligen; låt nåd och trofasthet bevara honom.
8 Kotero ndidzayimba matamando kwamuyaya pa dzina lanu ndi kukwaniritsa malumbiro anga tsiku ndi tsiku.
Då skall jag lovsjunga ditt namn till evig tid, i det jag får infria mina löften dag efter dag.